39
EDENI W A S ATA NA Tiyeni tiwerame. Wokondedwa Mulungu, ndife oyamikira kwa Inu usikuuno chifukwa cha mwayi wopambana uwu, kuti tabweranso mu Dzina la Ambuye Yesu, kuti tidzakomane naye mdani wathu, mdani Wanu, kuno ku bwalo la nkhondo; ndi Mawu, kuti timuthamangitsire iye kutali achoke pakati pa anthu Anu; kuti iwo akhoze kuwona, usikuuno, Ambuye, Kuwala kwa Uthenga. Ine ndikupemphera kuti Inu muwadzoze maso athu ndi mankhwala opaka mmaso, kuti iwo akakhoze kutsegulidwira kwa Choonadi; kuti ife tikachoke pano, tikunena mkati mwa mitima yathu, “Kodi mitima yathu siinatenthe mkati mwathu pamene Iye amalankhula nafe pa njira ija?” Muwachiritse odwala ndi osautsika. Muwalimbikitse okhumudwa. Mukwezere mmwamba manja ofooka amene nthawi ina anali ogwera pansi. Mutilole ife tiziyang’ana ku Kudza kwa Ambuye Yesu, kumene ife tikukhulupirira kuti kwayandikira. Ife tikupempha izi mu Dzina la Yesu. Ameni. Mukhale pansi. 2 Ine ndiyesera kuti ndichite mwachidule usikuuno, chifukwa ine ndikudziwa kuti ambiri abwera kuchokera ku zigawo zosiyanasiyana za dzikoli, ku…adzera msonkhano; kapena munatsalira, ena a inu, ndipo muyenera kuti muzibwerera, mwinamwake mitunda yaitali kuti mubwerere. Ndipo ine ndikukuthokozani inu. Mmawa uno ine ndimafuna kuti ndimumve M’bale Neville, inemwini. Ndipo ine ndamumvapo iye nthawi zambiri, ndipo ine sindinakhalepo ndi nthawi imene ndinamumvapo iye imene ndinakhala osamuyamikira iye. Koma mmawa uno, uthenga wogwirizana ndi nthawi uja, ine ndikudziwa ine ndinali ndi kutsogolera kwa Ambuye kuti ndimvetsere kwa iwo mmawa uno. Zabwino kwambiri! Ndipo ine ndawona chifukwa chimene anthu inu mumakonda kumabwera ndi kudzamumvetsera iye, inunso. Ndipo iye nthawizonse azikuchitirani inu zabwino, ine ndikutsimikiza, mukamamumvetsera iye. 3 Ine ndinali kuyesera kuti ndimalizitse zina za zolankhulana zanga lero; mmawa uno ndi madzulo ano. Ine ndikadali nawobe ambiri, mbiri, ambiri oti azipita. Ndipo ine… 4 Monga, ine ndikukhulupirira, anali Yatero amene anamuuza Mose nthawi ina, anati, “Iwe zakuchulukira basi.” Kotero, ife tiri ndi abale ambiri pano pa mavuto anuwo. Ndipo mmodzi aliyense wa iwo ndi wololedwa, ndipo ndi zinthu zabwino zimene ziyenera kusamaliridwa. Ndipo ine ndingafune abusa athu, kapena M’bale Mann, ndi atumiki ena a Chikhulupiriro chathu pano. Inu mukhoza kupita kwa iwowo. Iwo akhoza

CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

Embed Size (px)

Citation preview

Page 1: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA

Tiyeni tiwerame. Wokondedwa Mulungu, ndife oyamikirakwa Inu usikuuno chifukwa cha mwayi wopambana uwu,

kuti tabweranso mu Dzina la Ambuye Yesu, kuti tidzakomanenaye mdani wathu, mdani Wanu, kuno ku bwalo la nkhondo; ndiMawu, kuti timuthamangitsire iye kutali achoke pakati pa anthuAnu; kuti iwo akhoze kuwona, usikuuno, Ambuye, Kuwala kwaUthenga. Ine ndikupemphera kuti Inumuwadzozemaso athu ndimankhwala opaka mmaso, kuti iwo akakhoze kutsegulidwirakwa Choonadi; kuti ife tikachoke pano, tikunena mkati mwamitima yathu, “Kodi mitima yathu siinatenthe mkati mwathupamene Iye amalankhula nafe pa njira ija?” Muwachiritseodwala ndi osautsika. Muwalimbikitse okhumudwa. Mukwezeremmwamba manja ofooka amene nthawi ina anali ogwera pansi.Mutilole ife tiziyang’ana ku Kudza kwa Ambuye Yesu, kumeneife tikukhulupirira kuti kwayandikira. Ife tikupempha izi muDzina la Yesu. Ameni.

Mukhale pansi.2 Ine ndiyesera kuti ndichite mwachidule usikuuno, chifukwaine ndikudziwa kuti ambiri abwera kuchokera ku zigawozosiyanasiyana za dzikoli, ku…adzera msonkhano; kapenamunatsalira, ena a inu, ndipo muyenera kuti muzibwerera,mwinamwake mitunda yaitali kuti mubwerere. Ndipo inendikukuthokozani inu. Mmawa uno ine ndimafuna kutindimumve M’bale Neville, inemwini. Ndipo ine ndamumvapoiye nthawi zambiri, ndipo ine sindinakhalepo ndi nthawiimene ndinamumvapo iye imene ndinakhala osamuyamikiraiye. Koma mmawa uno, uthenga wogwirizana ndi nthawiuja, ine ndikudziwa ine ndinali ndi kutsogolera kwa Ambuyekuti ndimvetsere kwa iwo mmawa uno. Zabwino kwambiri!Ndipo ine ndawona chifukwa chimene anthu inu mumakondakumabwera ndi kudzamumvetsera iye, inunso. Ndipo iyenthawizonse azikuchitirani inu zabwino, ine ndikutsimikiza,mukamamumvetsera iye.3 Ine ndinali kuyesera kuti ndimalizitse zina za zolankhulanazanga lero; mmawa uno ndi madzulo ano. Ine ndikadali nawobeambiri, mbiri, ambiri oti azipita. Ndipo ine…4 Monga, ine ndikukhulupirira, anali Yatero amene anamuuzaMose nthawi ina, anati, “Iwe zakuchulukira basi.” Kotero, ifetiri ndi abale ambiri pano pa mavuto anuwo. Ndipo mmodzialiyense wa iwo ndi wololedwa, ndipo ndi zinthu zabwinozimene ziyenera kusamaliridwa. Ndipo ine ndingafune abusaathu, kapena M’bale Mann, ndi atumiki ena a Chikhulupirirochathu pano. Inu mukhoza kupita kwa iwowo. Iwo akhoza

Page 2: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

2 MAWU OLANKHULIDWA

kukakuuzani inu ndendende basi chinthu choti mukachite;anthu ena, ana awo; kukwatirana, kapena zinthu zimene zirizolakwika. Ndipo amuna awa akhoza kukuthandizani inuchimodzimodzi basi monga—monga wina aliyenseyo, chifukwaiwowo ndi antchito aKhristu. Ndipomuzipita kwa iwowo, ndipoine ndikutsimikiza iwo aka—iwo akakupatsani inu thandizolimene inu mukulisowa. Ine sindingathe kupita kwa onse aiwo. Alipo ochuluka basi, paliponse pamene iwe ungapite.Iwo akumangochulukira chulukira mokwerera kwerera, inumukuona. Ndipo—ndipo iwe umafuna kuti ufikire kwa winaaliyense wa iwowo, koma iwe sungathe kuchita zimenezo. Komaine ndikumapemphera mosalekeza kuti Mulungu, mwanjira ina,akuthandizeni inu izo mwabwino bwino.5 Tsopano, usikuuno, ife tikufuna kuti tipite ku Lemba, ndikukawerenga gawo la Lemba kuchokera mu Genesis, mutuwa 3; ndipo tizilozera mmbuyo pang’ono kwa zinthu zinazomwe ife takhala tikuzikamba, mu nthawi za mmbuyomu,ndipo tiwona ngati Ambuye Yesu ati atipatse ife zowonjezerapang’ono pa zomwe titadziwe pamene ife tikhale tikutuluka. Inendikupemphera—ndikupemphera kuti Iye atero.

Tsopano serpenti anali wochenjera kwambiri kuposazamoyo zonse za kuthengo zimene YEHOVA Mulunguanazipanga. Ndipo iye anati kwa mkaziyo, Eya,Mulungu wanena kuti, Inu musamadye za mtengouliwonse wa m’mundamu?Ndipo mkaziyo anati kwa serpenti, Ife tikhoza kudya

chipatso cha mmitengo ya mmundamu:Koma chipatso cha mtengo umene uli pakati pa

munda, Mulungu wanena kuti, Inu musadzadyeumenewo, komanso musadzawukhudze iwo, kuwopakuti inu mungafe.Ndipo serpenti anati kwamkaziyo, Inu kufa simudzafa

ayi:Pakuti Mulungu akudziwa kuti tsiku limene inu

mudzadya umenewo, ndiye maso anu adzatseguka,ndipo inu mudzakhala ngati milungu, odziwa zabwinondi zoipa.Ndipo pamenemkaziyo anawona kuti mtengowo unali

wabwino kuwudya, ndi kuti unali wokoma mmaso,ndi mtengo wokhumbirika wompangitsa wina kukhalawanzeru, iye anatenga chipatso chake, ndipo anadya,ndipo anakampatsansomwamunawake limodzi ndi iye;ndipo iye anadyanso.Ndipo maso a onse awiri anatseguka, ndipo iwo

anadziwa kuti anali amaliseche; ndipo anasokamasamba a mkuyu, ndipo anadzipangira okhamatewera.

Page 3: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 3

6 Ambuye awonjezere ma…madalitso Ake pa kuwerengakwa Mawu Ake. Tsopano ine ndikufuna kuti nditenge phunzirousikuuno, kuchokera pamenepo, ndi kulitcha: Edeni Wa Satana.Kanthu kakang’ono kakhambi kwambiri kuti ukanene, ka,Edeni Wa Satana. Izo zikukhala ngati zikugwirizana, ndi usikuwina wa Lamlungu, ine ndikukhulupirira, pamene ine ndinalikulakhula ndi inu kuno zaSefa YaMunthuWoganiza, ndi kulawakwa munthu woyera.7 Ndipo nthawizina kulankhula kwa khambi ukukumatibweretsa ife kwa chinachake; zimatipangitsa ife kutitiziwerenga, ndi kukuika iwe powerenga Mawu. Ndipo ndichimene ine ndimafuna mpingo wanga wonse kuti uzichita.“Munthu sadzakhala moyo ndi mkate wokha, koma ndiMawu onse otuluka kuchokera mkamwa mwa Mulungu.”Kotero, muziwerenga Mawu; muziwaphunzira Iwo. Ndipomuziwaphunzira Iwo ndi maso a Mulungu, kuti muzilipatsaluntha lanu kumvetsetsa kwa mmene ife tiyenera kukhalira mutsiku la lero.8 Tsopano ndabwera kuno, usikuuno, kuti ndidzangolankhulandi inu, kudzanena kuti, “Chabwino, ine ndikhoza kuchita izikapena izo,…”9 Ine ndimakonda kulankhulana ndi anthu, mochulukamongammene ine ndikufunira ngakhale kupita kunyumba ndi winaaliyense wa inu usikuuno. Ine…Mulungu akudziwa kuti izo ndizoona. Ine ndingakonde nditapita kunyumba ndi wina aliyensewa inu, ndi—ndi kukadya—kukadya kadzutsa ndi inu mmawa,ndi—ndi—ndi kupita kutchire ndi kukasaka agologolo ndi inumawa madzulo, mwawona. Ine—ine ndingakonde nditachitazimenezo, koma ine—ine sindingathe kuchita zimenezo. Ndipoine ndimafuna nditapita kunyumba ndi kukangokhala pansindi kumalankhula ndi inu; kukakhala pa khonde utathamsonkhano, ndi kukalankhula nanu kwakanthawi, kulankhulananu inu zamoyowanu ndi zokhudzaMulungu. Ine ndingakondenditamachita zimenezo. Amuna ndi akazi muno; Mulunguakudziwa kuti ine ndimafuna nditamachita zimenezo, komaine sindingathe kuchita izo. Mwawona, pamangokhala basizoterozo—pamangokhala kukoka koteroko ndi kupanikizika.10 Ndipo—ndipo mu m’badwo wamanjenje uno umene ife tirinkukhalamo…Ndipo ndine munthu wa manjenje, inemwini.Lero ine ndikhoza kukhazikitsamalingaliro anga pa chinachake,“Ine ndiyenera basi kuti ndichite chimenecho,” ndipo mawazidzakhala mamailosi miliyoni kwa ine; chinachake chaduliramkati ndipo chachita ichi ndi icho. Ndipo iwe umakhala ndinthawi, yoyesera kuti uziike nzeru zako pamodzi.11 Koma chopambana changa chachikulu ndi kulalikiraUthenga kudzera mu Mpingo, ndi kuchita zonse zimene inendingathe kuti ndikabweretse ulemu kwa Yesu Khristu mu

Page 4: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

4 MAWU OLANKHULIDWA

tsiku lino, pamene ine ndikadali pano pa dziko lapansi,ndi nthawi yomwe ndatsala nayo pa dziko lapansi. Inendabwera ku—kuti ndidzayesere kunena chinachake kwainu chimene chingakuthandizeni inu; chinachake. Inendinakawerenga pamene ndinapita kunyumba mmawawu.“Kodi ine ndingakanene chiyani usikuuno, Ambuye, chimenechingakawathandize anthu amenewo?”12 Ndikumvetsera uthenga wamphamvu uja mmawa uno pa…M’bale Neville anatibweretsera ife, wa…ine ndinaganiza iwounali wopambana kwambiri, momwe iye ananenera pamenepo,“Adokotala amayeza matenda; koma munthu amene amabwerandimbale yodzaza ndimasingano, iye amabaya jakiseni.” Koteroine ndinaganiza izo zinali zenizeni—kulongosola kokongolakwenikweni kwakung’ono. Ine ndinaganizira za zimenezo,“mankhwala, nthendayo ikapezeka.” Kotero chimenecho ndichinthu chabwino kwambiri.13 Ine ndikufuna kuti ndilankhule ndi inu chinachake, kutindibweretse chinachake choti chiwunikire kwa inu lonjezola Mulungu la m’badwo uno. Mukuona? Chinachake, osatichinachake chimene winawake anali mu tsiku linalake,koma chinachake…ndipo pamene…Zinthu zimenezo ndizabwino; ife tonse timalozera kwa zinthu zimenezo. Komaine ndaganiza kuti ndiyesere kubweretsa chinachake kumalingaliro anu, pogwiritsa ntchito Malemba awa amenendawalemba apa, chimene chingakuunikireni inu, kutimuzidziwa, kukakupangani inu kukhala msirikali wabwinokomuthengo limene inu mukumenyamo pakali pano; kutimuphunzire njomba za mdani, kuti inu mukathe kuphererachirichonsecho chisanafike kwa inu, mwawona. Ndicho chinthuchenichenicho, ndikuti muphunzire kupewa—zibagela kutizisakufikeni inu, mochulukammene inumungathere.14 Tsopano, tiyeni ife tiyang’ane tsopano kwa chopambanaichi…kwa maminiti pang’ono, tsiku lalikulu, lochimwitsitsa ililimene ife tiri nkukhalamo tsopano. Ine sindikukhulupirirakuti linayamba lakhalapo tsiku limene ine ndinayambandaliwerengapo mu mbiriyakale…Pakhala pali masikuopambana akuzunzidwa, pamene ana a Mulungu ankaphedwapa mbali zonse zonse. Koma kuwona chinyengo cha mdani,ife sitinayambe takhalapo ndi tsiku ngati ili limene ife tirinkukhalamo tsopano. Ilo ndi tsiku lothyathyalika kwambiri,lachinyengo. Ndipo pamene ine ndiwona zimenezo, izozimabweretsa izi, kuti, Mkhristu ayenera kukhala mochulukakwambiri pa mapazi ake lero kuposa momwe iye anayambawakhalirapo mum’badwo uliwonsewo.15 Tsopano, tikabwerera mu masiku a kuzunza, kwa Roma,mpaka kudzafika kwa Mpingo; Mkhristu akalakwitsa, iyeamapita ku bwalo ndipo amakadyetsedwa kwamikango, kapenachinachake monga choncho, pamene iwo amupeza kuti iye

Page 5: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 5

ndi Mkhristu chifukwa cha umboni wakewo. Koma moyowake umapulumutsidwa, chifukwa iye anali wokhulupiriraweniweni, wosaipitsidwa mwa Mulungu, ndipo mokondweraamasindikiza umboni wake ndi magazi ake. Pamene mitsemphaimakhwefuka, kapena mabowo mu thupi lakelo, ndipo magazinkumawukhamo, iye ankakhoza kukuwa mokweza mawu,ndi chikhulupiriro chenicheni chomvera, ndikuti, “Mulandiremzimu wanga, Ambuye Yesu!”16 Koma, tsopano, kuthyathyalika kwa mdierekezi tsopano,kukuwapangitsa anthu kumakhulupirira kuti iwowo ndiMkhristu pamene iwo asali. Chinthu chake ndi chimenecho.Inu simukusowa kuti muzisindikiza…Ili—ili ndi tsikulothyathyalika kwambiri kuposa limene ilo lingakhale, kusiyanandi pamene iwe unkachita kusindikiza moyo—moyo wako ndiumboni wako. Mdierekezi watchera msampha wothyathyalikauliwonse umene iye angathe, kuti…Iyeyo ndi wonyenga.Ndipo Yesu anatiuza ife, mu Mateyu 24, momwe tsiku ililikanadzakhalira limene ife tiri nkukhalamo, tsiku lonyengakwambiri limene silinayambe lakhalapo, “zapafupi kwambirimwakuti zikanati zidzawanyenge Osankhidwa kumene aMulungu ngati kukanakhala kotheka kuti iye awanyenge.”17 Tsopano tiyeni ife tifanizitse Malemba ena, kapenamauneneri amene analankhulidwa mu Baibulo, za lero, ndipotifanizitse izo ndi tsiku limene ife tiri nkukhalamo pakali pano.18 Mu Timoteo Wachiwiri 3, ife timaphunzira izi, kutimneneri ananena, kuti, “Zidzachitika mu masiku ano, kutianthu adzakhala ammutu, amaganizo-odzikweza, okondazokondweretsa kuposa kukonda Mulungu.” Mufanizitsezimenezo tsopano, kwa mphindi chabe. Ife sikuti…Ifetingochitamwachidule izo, chifukwa ife tiribe nthawi yochulukachomwecho kuti tidutse mu izo zonse monga mmene ifetiyenera kuzitengera izo; koma basi kuti tingowunikirapo izo,kuti inu mukathe kuwona pamene inu mukafike kwanu ndikukawerenga izo. “Ammutu, amaganizo-odzikweza, okondazokondweretsa kuposa kukonda Mulungu; osayanjanitsika,otsutsa mwabodza, osadzigwira, ndi onyoza iwo amene aliabwino.” “Tsopano Mzimu unalankhula mwachimvekere kutizinthu izi zikanadzakhala mu masiku otsiriza.” Amenewo ndimasiku ano, uneneri ukulankhula kwa iwo.19 Tsopano ife tiwerenge, aponso, mu Chivumbulutso…14, Chivumbulutso 3:14, kani, M’badwo wa Mpingo waLaodikaya, za momwe mpingo uti udzakhalire mu tsikulotsiriza lino. Ndipo iwo udzakhala, Iwo amati, “Iwo udzakhalangati mkazi wamasiye ndipo sumadzasowa kanthu. Iwo—iwo unali wolemera, ndi wochulukidwa nacho chuma, ndipoosadziwa izo kuti iwo unali wosauka, womvetsa chisoni,watsoka, wakhungu, ndi wamaliseche, ndipo sumadziwa izo.”A…Tsopano, kumbukirani, Iye akulankhula ndi mpingo wa

Page 6: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

6 MAWU OLANKHULIDWA

m’badwo uno, “womvetsa chisoni, wakhungu, wamaliseche,ndipo osadziwa izo.” Ndime yomalizira iyo, Mawu omaliziraawo, ndi amene akuzipanga izo kukhala zokhudza kwambiri.Iwo amaganiza kuti ndi odzazidwa bwino ndi Mzimu, iwo onsendi okonzeka. M’badwo wa Mpingo wa Laodikaya ndi M’badwowa Mpingo wa Pentekoste, chifukwa iwo ndi m’badwo wampingo wotsirizira. Luther anali ndi uthenga wake;Wesley analindi uthengawake; ndipo Pentekoste inali ndi uthengawake.20 Ndiponso, Iwo akunena, kuti, “Chifukwa iwe uli wofunda,osati wotentha kapena wozizira,” zotengeka za kunjaku,mamvetsedwe a luntha a Uthenga; “chifukwa,” Iye anati,“iwe uli chomwecho, Ine ndikulavula iwe kuchokera mkamwaMwanga.” Mwakulankhula kwina, izo zimamupangitsaIye kudwala akamawuwona mpingo uli mu chikhalidwechimenecho.21 Ndipo, kumbukirani, iwo anamulavulira Iye panja; ndipo Iyeanali ali kunja kwa mpingo, akuyesera kuti alowenso mkati, muM’badwowaMpingowaLaodikayawoyipitsitsa uwo.22 Mulungu wa dziko lino lero, munthu wopembedzedwawa dziko lino lero, ndi Satana. Ndipo anthu sakuzindikirakuti akumupembedza Satana, koma ndi Satana ameneakudzitsanzira yekha ngati mpingo, mwawona, ngatimpingo. Iwo akumupembedza Satana, kumaganiza kuti iwoakumupembedza Mulungu podzera mu mpingo, koma umo ndimmene Satana wachitira izo.

“O,” inu mukuti, “koma dikirani miniti; ife timalalikiraMawu.”23 Taonani mmbuyo apa pa phunziro langa, usikuuno. Satanaanali iyeyo amene analalikira Mawu kwa Eva, poyamba,“Mulungu wanena kuti,” mwawona.24 Ndi kupotoza uko kwa gawo lija la Lemba kumenekukufanana ndi tsikuli. Iye adzakulolani inu kudziwa kutizonse zimene Yesu ankachita zinali zabwino mwangwiro. Iyeadzakulolani inu kudziwa kuti zonse zimene Mose ankachitazinali zabwino mwangwiro. Koma pamene inu mutengamalonjezo omwe Iwo anapereka a tsiku la lero, ndiye Zimenezozinali za m’badwo wina. Ndizo basi zonse zimene iye ayenerakuchita, mwaona, ndikuti awafikitse anthu kuti azikhulupiriraIzo mwanjira imeneyo, ndipo izo—ndizo zonse. Chifukwa, “Inusimungachotsere Mawu amodzi kuchokera kwa Iwo, kapenakuwonjezerapo mawu amodzi kwa Iwo.” Koma ndizo zimene iyeakuchita.25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganizakuti iwo akumupembedza Mulungu; monga ife tikuchenjezedwandi uneneri, mu AtesalonikaWachiwiri. Izo, tiyeni tingowerengazimenezo, Atesalonika Wachiwiri, mutu wa 2. Tiyenitingopeza zimenezo mkamphindi, ngati ine ndingathe,

Page 7: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 7

pomwepo. Ine ndikufuna kuti ndiwerenge zimenezo. Basi,ine ndikukhulupirira, Atesalonika Wachiwiri. Ine ndalipezaLembalo apa. MuWachiwiri…

Tsopano ife tikukupemphani inu, abale, chifukwa chakudza kwa Ambuye Yesu…ndi pa kusonkhanitsirapamodzi kwa iye,

26 Tsopano, taonani, “kudza kwaAmbuye, ndi kusonkhanitsirakwa Iye,” monga Mulungu adzawasonkhanitsira anthu Ake kwaIye mu masiku otsiriza. “Kusonkhanitsira anthu kwa Ambuye,”osati kwa mpingo, “kwa Ambuye; kuwasonkhanitsira pamodzikwa Iye.”

Kuti inu musagwedezeke msanga mmalingaliromwanu, kapena…kuvutitsidwa—kuvutitsidwa, osatindi mzimu, kapena…mawu, kapena ndi kalata ngatikuti yachokera kwa ife, monga…tsiku la Ambuye liripafupi.

Munthu aliyense asakunyengeni inu mwanjirailiyonse: pakuti tsiku ilo silidzafika, pokhapokhapochifike kaye chipatuko poyamba, ndipo munthu watchimo uja (“munthu wa tchimo,” penyani chimene iyeali tsopano), munthu wa tchimo ataululidwa, mwanawa chiwonongeko, (ameneyo anali Yudasi, mwawona);

Amene amatsutsa ndi kudzikuza yekha pamwambapa zonse zotchedwa Mulungu, kapena zimenezikupembedzedwa; kotero kuti iye monga Mulunguakukhala mu kachisi wa Mulungu, kumadziwonetsayekha kuti iye ali Mulungu.

27 Chinyengo champingo chimenecho lero!Mwawona, “mwanawachiwonongeko,” mdierekezi. “Mwana wachiwonongeko,”mdierekezi. Ndiye, anthu akumupembedza Satana mu tsikula lero, kumaganiza kuti iwo akumupembedza Mulungu.Koma iwo akumupembedza iye kudzera mu kachikhulupiriro,zipembedzo zopangidwa ndi anthu ndi tizikhulupiriro timenetawabweretsa anthu mpaka kukafika ku chinyengo chachikuluchimene dziko linayamba lachidziwapo. Ziribe kanthu kuti ndiMawu a Mulungu ochuluka bwanji amene analonjezedwa kwatsiku la lero, akulalikidwa ndi kutsimikiziridwa, komabe iwosakukhulupirira Iwo. Iwo sangawakhulupirire Iwo.28 Ndiye bwanji? Ife timadabwa kuti zikukhala bwanji.Nchifukwa chiyani izo sizikutero; nchifukwa chiyani iwosakukhulupirira Iwo? Pamene Mulungu anati Iye adzachitachinthu chinachake, ndipo Iye nkudzachichita icho, ndipokomabe iwo akumapotoza nsana wawo kwa izo ndi kumachokakwa izo. Basi monga Eva ankadziwira kuti zimene Mulunguananena, Mulungu akanadzazichita; koma iye anapotolotseransanawake kwa izo, namvera zimenemwamunayo amati anene.

Page 8: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

8 MAWU OLANKHULIDWA

29 Ingokumbukirani, mu mibadwo inayo, nthawizonsechakhala chiri chinthu chomwe chomwecho. Mu m’badwouliwonse, nthawizonse zakhala ziri kuti Satana amayesetsakuwapotoza Mawu amenewo kwa iwo, amawapangitsa iwo kutiaziwona m’badwo wina.30 Taonani, pamene Yesu anabwera, mwawona, Satana analimu gulu lija la aphunzitsi Achiyuda, ndi marabbi ndi ansembe,akuyesera kumawauza iwo kuti azisunga lamulo la Mose,pamene Mawu amenewo amanena kuti mu tsiku limeneloMwana wa munthu adzakhala akuululidwa, mwawona, kuti Iyeadzakhala akudziulula Yekha. Kotero iwo anali akuyesera, bolangati iwo amasunga zipembedzo zimenezo, ndiponso lamulola Mose. Mukuona zimene iye anachita? Iye anali akuyeserakuti awawuze iwo, “Gawo limenelo la Mawu liri lolondola basindendende, koma Munthu uyu si Munthu ameneyo.” Mukuonamomwe iye aliri wachinyengo? Limenelo ndiye tsiku lenileni lijala chinyengo.31 Izo zakhala ziri, ndipo tsopano ziripo, Satanaakuwukhazikitsa ufumu wake pa dziko lapansi. Ndichochifukwa chake ndendende chimene iye akuchitira zimenezo,chifukwa iye akufuna kuti awukhazikitse ufumuwakewake.32 Monga munthu wa geni, amene sali Mkhristu, iyeangayesetse njira iliyonse imene iye angathe kuti akupangitseniinu kuchiwona chinachake mwanjira yoyipa. Ngati iye alindi—cholinga ndi kuti zimupindulire iyeyo pokupangitsaniinu kuti muchite zimenezo, kukupangitsani inu kuti muwoneizo mwanjira imeneyo, iye angakusonyezeni inu chirichonsechimene iye angathe, ndi kukubisilani inu choona chake,chifukwa iye akungozikonda yekha. Ziribe kanthu kuti iyeyoakunamizani mochuluka bwanji ndi kukunyengezani, ndi chinachirichonsecho, iye akungofuna zimupindulire iyeyo.33 Ndipo ndi chifukwa chake Satana wachita izi. Ndipoiye wagwira ntchito kudzera mu utumiki kuti achite izi,monga Mulungu analonjezera kuti iye akanadzachita zimenezo.Tsopano, iye anayamba ndi chinyengo cha chipembedzo muEdeni, ndipo wakhala akupitiriza chiyambireni.34 Osati pokhazikitsa gulu la achikominisi. Achikominisialibe chochita ndi izi. Ndi mpingo, ndi pamene inu muyenerakusamalitsa, mwawona. Sikuti ndi—sikuti ndi achikominisiamene akanadzanyenga Osankhidwa omwe. Ndi mpingo umeneuti udzanyenge Osankhidwa omwe, mwawona. Sikuti ndiachikominisi; ife tikudziwa kuti iwo amamukana Mulungu,ndipo iwowo ndi otsutsakhristu, ndithudi iwo ali, mu zochitazawo, koma iwowo si otsutsakhristuyo. Wotsutsakhristu ndiachipembedzo, achipembedzo kwambiri, ndipo amakhozakulankhula mobwereza Lemba, ndi kulipanga Ilo kumawonekalomveka bwino kwambiri.

Page 9: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 9

35 Monga Satana anachitira kumbuyo uko pachiyambi, iyeanalankhula mobwereza chirichonse mpaka pansi, “Mulunguanati, ‘Musadzadye mtengo uliwonse wa mmundamu.’”Mwawona, akulankhula mobwereza Iwo basi.

36 Mkaziyo anati, “Inde, ife tikhoza kudya za mmitengo yonseya mmundamu, koma pali mtengo pakati pa munda umeneMulungu wanena kuti tisadye, pakuti, ngakhale kuwugwira iwo;chifukwa, tsiku limene ife tidzatero, tsiku limenelo ife tidzafa.”

37 Iye anati, “O, ndithudi kufa simudzafa ayi. Koma undiloleine ndikuwuze iwe chifukwa chimene Mulungu ananenera izi,ndi chifukwa chakuti…” Mwawona, iye akutani tsopano? Iyeakulankhula mobwereza Choonadi ichi, inu mukuona. Iye anati,“Izo zidzatsegula maso anu, ndipo izo zidzakupangitsani inukudziwa chabwino ndi choipa. Inu mudzakhala ngati Mulungumukatero, ngati inumungathe kuchita zimenezo.”

38 Ndi zokhazo basi zimene iye akufuna kuti achite, ndipo izondi chinthu chomwe chomwecho basi chimene iye akuyesera kutiachite lero. Pakhala pali chinyengo chachipembedzo kuyambirapachiyambi pomwe ku Edeni, ndipo zakhala ziri chomwechochiyambireni. Mu nthawi ya Adamu, icho chinali chinyengo. Munthawi ya Nowa, icho chinali chinyengo. Mu nthawi ya Yesu,zinali chimodzimodzi. Ndipo tsopano ndi chimodzimodzi, njirayomwe yomweyo, kunyenga kwa chipembedzo!

39 Tsopano, ife tikuzindikira dziko lapansi, pamene Mulunguankalilamulira ilo. Tsopano, pamene Mulungu ankalilamulirailo…ilo linali pansi pa ulamuliro Wake. Kenako Satanaanadzalitenga, pa kukana Mawu a Mulungu. Mulungunthawi ina anali ndi dziko lapansi pansi pa ulamuliroWake. Iye analikhazikitsa ilo mu kanjira kake. Iye analiyikailo, analipanga ilo kuti lizigwira ntchito. Iye anachitachirichonsecho, ilo linali pansi pa ulamuliro Wake. Tsopanoife tifanizitsa izo ndi pamene Satana anadzalitenga ilo muulamuliro wake.

40 Tsopano, zinamutengera Mulungu zaka sikisi sauzande.Ilo silinamutengere Iye nthawi yaitali chomwecho, koma Iyeanatenga nthawi yaitali chomwecho. Zaka sikisi sauzande,chifukwa ife timaphunzitsidwa kuti “tsiku limodzi Kumwambandi zaka sauzande pa dziko lapansi,” ndipo zinali zaka sikisisauzande, kapena masiku sikisi amene Mulungu anamangadziko lapansi. Tsopano, zinamutengera Mulungu zaka sikisisauzande kuti alikhazikitse ilo, kulibzala ilo ndi mbewuzabwino ndikuti libale chirichonse monga mwa mtundu wake.Chirichonse chiyenera kubala monga mwa mtundu wake.Mbewu Zake zonse zinali zabwino, ndipo kotero izo ziyenerakubalamongamwamtunduwake.Mulungu anatenga zaka sikisisauzande.

Page 10: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

10 MAWU OLANKHULIDWA

41 Potsiriza, pamene Iye anatsiriza kulipanga ilo lonse, ndipopotsiriza ife…potsiriza anadzafika ndi likulu lake, la dzikolapansi, pa malo okongola aku mmawa kwa Edeni, otchedwamunda wa Edeni. Mulungu anaika likulu la dziko lapansimmunda wa Edeni, ku Igupto, ku mmawa komwe kwamundawonkumene kunali likulu lake.42 Ndipo pa chochitika chonsecho, Iye anakamuikako mwanaWake ndi mkazi wa mwana Wake, kukakhala oyang’anirapa zonsezo. Izo nzoona. Ndi zimene Mulungu anachita. Iyeanawaika iwo kukakhala olamulira zonse. Iwo amakhozakulankhula ndi mphepo, ndipo iyo imatha kusiya kuwomba. Iwoamakhoza kulankhula ndi mtengo, ndipo iwo umatha kusunthakuchoka apa kupita apo.43 Mkango ndi nkhandwe zimadyera pamodzi, ndipo nkhosainkagona limodzi ndi izo. Kunalibe choipa kumeneko. Iwounali mtendere wangwiro, mgwirizano wangwiro, chirichonsechinali mu ungwiro, ndi pamene Mulungu anali nalo ilo pansipa ulamuliro Wake. Ndipo zindikirani, Iye anali nalo Lake…Iye anali nalo dziko Lake, Iye anali akulamulira chirichonse.Iye anali ndi chirichonse chikubwera. Chirichonse chikudyazomera; panalibe choti chikanafa, panalibe choti chikhalabwinja, panalibe choti chikanawonongedwa. Panalibepo…Izozinali zangwiro basi.44 Ndipo pamwamba pa izo zonse, Iye anawaikapo ana Akeokondeka, mwana Wake wamwamuna ndi wamkazi, mwamunandi mkazake, kuti azilamulira izo.45 Mulungu anali wokhutitsidwa kwambiri! “Ndipo Iyeanakapuma ku ntchito Zake zonse, pa tsiku lachisanu ndichiwiri,” ndipo analiyeretsera tsiku ili la sabata lachisanu ndichiwiri kwa Iye.46 Chifukwa, Mulungu anadzaliyang’ananso ilo, Iye atathakukhala zaka sikisi sauzande akuliwumba ilo ndi kulikonzailo, kulipanga ilo kuti lifike pokhalapo; ndipo anadzutsamapiri, ndipo anapangitsa ziphala zamoto kuti ziwakankhiremapiri mmwamba, ndi zinthu zomwe zinachitika mukuphulikako; anawawumitsa iwo, ndi kuwakonza iwo momweIye amawafunira iwo. Ndipo awo anali malo okongola.47 Panalibe chinthu chirichonse chonga iwo, maparadizoopambana a Mulungu! Ndipo madinosaro akulu akulu, ndichirichonsecho, zikukwawa kudutsa mmenemo, ndi nyamazikuluzikulu; munalibe zakupha mwa izo. Izo zinali basizodekha monga mwana wa mphaka. Izo zinalibe basi kanthukalikonse; kunalibe—kunalibe matenda, kunalibe chisoni;kunalibe nyongolosi imodzi ya matenda pa dziko lapansi. O,anali malo bwanji!48 Mbalame zikuluzikulu zikuuluka kuchoka pa mtengo kupitapa mtengo, ndipo Adamu ankatha kuziitana izo ndi dzina, ndipo

Page 11: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 11

izo zimakhoza kuwulukira pa mapewa ake ndi—ndi kumalirapa iye. Ndipo, o, anali malo opambana bwanji amene Mulunguanali nawo!49 Ndipo kenako anapanga chimodzi cha zikhumbo ZakekuchokeraMthupi Lake Lomwe.Mulungu ali nazo zikhumbomuThupi Lake.50 Monga, inu muli chikhumbo cha abambo anu. Ndipo, inumukuzindikira, inu munali mwa agogo a agogo agogo anu.Koma, mmenemo, tinene kuti, ife titsike nazo izo mmusi mongainu ndi abambo anu. Tsopano, inu simunkadziwa kalikonsepamene inu munali mwa abambo anu. Nyongolosi ya moyoimachokera kwa mwamuna. Mwamuna amakhala ndi khungula magazi; mkazi amakhala ndi—dzira; tsopano, kotero, khungula magazi limakhala ndi moyo mwa ilo. Ndipo, ndiye, pameneinu munali mwa abambo anu, inu kwenikweni simunkadziwakalikonse za izo. Koma, komabe, sayansi ndi Mawu a Mulunguzimatsimikizira kuti inu munali mwa abambo anu, koma inusimunkadziwa kanthu za izo.51 Komano bambo ankafunitsitsa atakudziwani inu. Ndipondi mgwirizano wa kulumikizana ndi amayi, pamenepo inumunadzadziwika kwa bambowo. Tsopano, inu ndi chikhumbocha abambo anu. Inu mumawoneka ngati iwo, ndipo inumuli nazo ziwalo za thupi lanu zomwe zimawoneka ngatiabambo anu.52 Tsopano, umo ndi mmene Mulungu analiri pachiyambi.Mwana wamwamuna aliyense waMulungu ndi mwana wamkazialiyense wa Mulungu anali mwa Mulungu pachiyambi. Inusimukukumbukira izo tsopano, koma inu munali kumeneko.Iye ankadziwa izo. Ndipo Iye ankafuna kuti inu mudzakhalechimenecho kuti Iye azidzatha kumadzalankhula nanu inu,kumadzalankhula nanu inu ndi kumakukondani inu, ndikumadzagwirana nanu chanza.53 Kodi inu simumafuna mwana wanu yemwe…Kodisilimakhala tsiku lopambana pamene mwana wanu akhozakubwera kunyumba ndi kudzakhala nanu pa tebulo? Pamene iyewabwera kuchokera ku bwalo la nkhondo, kapena chinachakechimzake, ali ndi zipsyera; mmene inu mungakonzere chakudyacha madzulo; inu mungaphe mwana wa ng’ombe wonenepa,kapena chinachakenso, ndi kumukonzera iye! Ndi thupilanu lomwe ndi magazi, ndipo iyeyo anali mwa inu. Inusimunkamudziwa iye nthawi imeneyo, koma inu munkadziwakuti iye analipo.54 Ndipo chomwechonso Mulungu ankadziwa kuti ifetikanadzakhala kuno, komano Iye anadzatiika ife mu thupikuti ife tizidzatha kulankhulitsidwa. Ndi cholinga chakuti Iyeazidzatha kutilankhula, Iye anadzakhala mmodzi wa ife pameneIye anadzakhala Yesu Khristu, Mwana waMulunguMwiniwake,

Page 12: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

12 MAWU OLANKHULIDWA

chidzalo cha kuwonetseredwa kwaMulungu. Kotero chimenechochinali cholinga cha Mulungu, kuti adzawonetsere zikhumboZake mu chiyanjano.55 Pamene ine ndinali mwa abambo anga, ine sindinkadziwakanthu za izo. Koma pamene ine ndinadzakhala mwana wawondipo nkubadwa kwa iwowo, ine ndinali chikhumbo, gawo laabambo anga. Ndipo ndinu gawo la abambo anu.56 Ndipo monga ana a Mulungu, ife ndi gawo la chikhumbocha Mulungu chimene chinali mwa Iye, tinadzakhala thupimonga Iye anadzakhala thupi, kuti ife tidzathe kumakhalandi chiyanjano wina ndi mzake, monga banja la Mulungu padziko lapansi. Ndipo chimenecho chinali cholinga cha Mulungupachiyambi. Inde, bwana. Ndi chimene Mulungu ankafunapachiyambi.57 Iye anali nacho chirichonse pansi pa ulamuliro. Ndipo Iyeanadzambweretsa munthu mmunda wa Edeni, kukhala chinthuchaufulu; anati, “Mwanawe, ndi lako.”58 Malo okongola bwanji! Mulungu anali atakhutitsidwakwambiri, mpaka Iye anangobwerera mmbuyo ndipoanakapuma ku ntchito Zake zonse. Mtengo uliwonse siunkabalaminga ndi nthura. Panalibe nthuza zimene zinkachokera mumtengo wa minga. Chirichonse chinali changwiro. Mbewu zonsezinali zangwiro. Chirichonse chinalimu chikhalidwe changwiro.59 Kenako pamene Iye anapita kukapuma pang’ono, mdaniWake anazemberamo ndi chinyengo, ndipo analitenga ilo,potanthauzira mopotoka dongosolo Lake kwa ana Ake. Pamene,Iye anaika chidaliro Chake mwa mwana Wake Yemwe; mongammene inu mumakhalira ndi chidaliro ndi mwana wanuwamkazi pamene iye akukayenda panja usiku ndi mwamuna;monga mmene inu mumakhalira ndi chidaliro ndi mwana wanuwamwamuna pamene iye ayenera kuti apite ndi mnyamatawoledzera kapena mnyamata wosuta. Mwawona, Iye anali ndichidaliro ndi mwana Wake wamwamuna, kuti iye sangachitechirichonse cholakwika, ndipo asunga Mawu aliwonse omweIye ananena. Koma mdani anazemberamo; monga kathyali ujaamene angatenge mwana wanu wamkazi ndi kumakhala nayemakhalidwe oyipa; kapena—kapena mkazi wina kumutenga,kupita naye kokayenda mwana wanu wamwamuna, ndipochinthu chomwecho. Mwawona, iye anazemberamo. Mdani waMulungu anazemberamo ndipo anakatanthauzira mopotokaMawu kwa Eva.60 Tsopano, iye, ndi kugwa uku, iye walanda ndipo watengamunda wa Edeni, yekhayekha. Iye anawutenga iwo. Ndipotsopano iye wakhala ali ndi zaka sikisi sauzande za kulamulirakwa chinyengo; kumawanyenga anthu, ana a Mulungu, mongaiye anachitira nthawi imeneyo. Chifukwa, iwo anakhazikitsidwapa kukhala chinthu chaufulu, kuti azichita mulimonse mmene

Page 13: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 13

iwo angafunire. Ndipo ankakhulupirira kuti iwo azichitamolondola, kapena ankadalira kuti achita bwino, kenako iwoanabwera ndi kachitidwe kolakwika, ndipo anagulitsa maufuluawo oyamba kubadwa, monga Esau anachitira, ndi dzikolapansi. Ndipo Satana analitenga ilo, ndipo iye analilanda ilo.Ndipo iye wakhala ali nazo zaka sikisi sauzande kuti amumangeEdeni wake, monga Mulungu anali ndi zaka sikisi sauzande kutiamumalizitse EdeniWake. Ndipomwa chinyengo, chinyengo chaMawu, kapena anthu, tsopano wakhazikitsa Edeni wake wakepa dziko lapansi lino, mu tchimo.61 Edeni waMulungu anakhazikitsidwamu chirungamo. Edeniwa Satana akukhadzikitsidwa mu tchimo, chifukwa Satana nditchimo. Mulungu ndi chirungamo, ndipo ufumu wa Mulunguunakhadzikitsidwa mu chirungamo, ndi mtendere, ndi Moyo.Ndipo wa Satana ukukhadzikitsidwa mu tchimo, ndiponsotchimo lachipembedzo.62 Zindikirani momwe iye ananyengera, chinyengo chake,monga mmene iye anati akanadzachitira. Iye analonjeza kutiadzachita izi. Kodi alipo aliyense amadziwa zimenezo? Tiyeni ifetitembenuzire ku Yesaya, ngati inu mukufuna ena a Malembaawa. Ngati inu…Ine ndiyenera kuti ndiwerenge mobwerezazambiri za iwo, ine ndikuganiza. Tiyeni titembenuzire ku Yesayamutu wa 14, mphindi chabe, ndipo tikangowona zomwe Satanaananena apa, mphindi chabe. Mu Yesaya 14, ife tiwerengazimenezo, ndipo muwone zomwe munthu uyu anachita. Yesaya14, kuyambira ndi ndime ya 12.

Iwewagwa bwanji kuchokera kumwamba, O Lusifara,mwana wa m’banda kucha! momwe iwe wadulidwirapansi, yemwe unkawafooketsa mafuko!Pakuti iwe unati mu mtima mwako, ndidzakwera

kumwamba, ine ndidzakweza mpando wangawachifumu pamwamba pa nyenyezi (amenewo ndi anaaamuna), nyenyezi za Mulungu: ndipo ndidzakhalansopamwamba pa phiri la osonkhana,…dera la kumpoto:Ndipo ine ndidzakwera pamwamba pa mitambo;

ndipo ndidzakhala monga Wammwambamwambayo.63 Tsopano mufanizitse zimenezo apa ndi Malemba athuena mu Atesalonika, kanthawi kapitako, momwe iye anati,“Iye akukhala mu kachisi wa Mulungu, akudzikuza yekhapamwamba pa zonse zotchedwa Mulungu, kuti iye ngatiMulungu akupembedzedwa ngatiMulungu pa dziko lapansi.”64 Ndi ameneyotu mulungu wa dziko lino amene inendinamulalikira kwa inu Lamlungu lathali. Ndi uyu apalero mu chinyengo, ora lowopsya lija, nthawi yopambana iyoimene ife tiri nkukhalamo. Ndi nthawi ya ulemelero kwambiriya mibadwo yonse, chifukwa ife tikuyang’anizana nazoZakachikwi zopambana kachiwiri; ife tikuyang’anizana nayo

Page 14: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

14 MAWU OLANKHULIDWA

Edeni kachiwirinso. Koma mu m’badwo uno kumene, chinyengochonse ndi njomba iliyonse imene iye anayamba waigwiritsapontchito ndipo yomwe anakwanitsa kunyenga nayo, iyewadzisonkhanitsa zonsezo pamodzi ndipo wadzilimbikitsayekha; ndipo watsika pansi ngati Mulungu, ndipo wadzadziyikayekha pa malo a Mulungu; wachipembedzo, ndipo akhozakuwerenga mobwereza Lemba ndipo akhoza kukuuzani inuLemba, chimodzimodzi basi monga Satana anachitira kwa EvammundawaEdeni. Koma kusiyamalo amodzi a Iwo, ndizo zonsezomwe iye ayenera kuchita, kupanga danga limenelo, pamenechiphunzitso cha chiphe chamdierekezi chingadutsirepo, mongaSefa yamunthuwoganiza imene ife timaikamba usikuwina.65 Tsopano, iye anati iye akanadzadzikuza yekha pamwambapa Wammwambamwambayo; iye adzakwera pamwambapa mitambo ndi nyenyezi, ndipo iye akanadzakhalapamenepo ngati Mulungu, ndipo nkudzakhala pamwambapa Wammwambamwambayo. Ndipo iye wakwaniritsa mukuchita ziwopsyezo zakezo. Iye ndithudi anali ndi kupambanakodabwitsa pochita zowopsyeza zakezo, podzera mwa anthuomusiya iye kuti azifotokoza mopotoka, mu m’badwo uliwonse,mtengo wa Mawu olonjezedwa a Mulungu kwa m’badwoumenewo. Umo ndi mmene ndendende iye wachitira izo. Mum’badwo uliwonse, iye amawafotokoza Iwomopotoka.66 Mu masiku a Nowa, iye anafotokoza kuti zinali zosathekakuti mvula ivumbe kuchokera kumwamba, pakuti, “kulibekomvula kumwambako.” Uthenga wake wopambana wa sayansiumene iye anaulalikira mmunda wa Edeni! Iye ankakhozakuponyera zida ku mwezi ndi kukatsimikizira kuti kulibekochinyontho kumwambako. Koma Mulungu ananena kutikukanadzabwera mvula. Koma Satana anapambana, ndipoanawathira chiphe malingaliro a anthu, podzera mu kafukufukuwa sayansi, kuti, “izo sizingatheke kuti zichitike.” Koma izozinachitika. Mulungu ananena kuti zidzachitika, ndipo izozinadzachitika. Iye anazichita.67 Tsopano, mu masiku a—a Yesu, iye anachita chinthuchomwe chomwecho. Iye anaikanso chiphe mmalingaliro awomwa chinyengo, mwawona, powatanthauzira Mawu mopotoka.“Ngati Iwe uli Mwana wa Mulungu, tsopano undilole inendikuwone Iwe ukuchita chinachake za izo.”68 Yesu sanampangire chisudzo iye. Iye sanatero konse.Mulungu samapanga zisudzo. Iye samasowa kuti ayankhechirichonse chimene Satana angamfunse. Iye anali kokha…Yesu anati, “Kwalembedwa, ‘Iwe sudzakhala moyo…Munthusadzakhala moyo ndi mkate wokha, koma ndi Mawu onseotuluka kuchokera mkamwa mwa Mulungu.’” Mwawona,Iye sanasowe kuti amuchitire chisudzo, iyeyo. Iye sanasowekuti apange mkate. Iye akanakhoza kuchita zimenezo, koma

Page 15: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 15

zikanakhala kuti Iye akumumvera mdierekezi, kotero Iyesanasowe kuti amumvere mdierekezi.69 Ndipo panonso ilo ndi tchimo lachipembedzo, mongapachiyambi paja, zachinyengo kwambiri. Penyani izo tsopano.Sikuti basi kwenikweni tchimo lakale la tsiku ndi tsiku, kuchitachigololo ndi kuledzera, ndi kumagwiritsa ntchito Dzina laMulungu pachabe. Si zimenezo. Ayi.70 Inu mukukumbukira zaka zapitazo, ambiri ainu pano, a nthawi zakale, mukukumbukira ulalikiuja umene ine ndinalalikira, pa, Zokhumudwitsa PaChiweruzo. Wachiwerewere, sakakhumudwa kumeneko. Iyeakudziwa kumene iye akupita. Woledzera sakakhumudwakumeneko. Wotcheza mowa, wajuga, wabodza, wakuba, iyesakakhumudwako. Koma, munthu uyo amene amaganiza kutiakulondola, kumeneko akakhumudwa.71 Munthu wake ndi ameneyo, adzati, adzabwera ndikuti,“Ambuye, kodi ine sindinalalikire Uthenga, kodi inesindinatulutse ziwanda, mu Dzina Lanu?”72 Yesu anati, “Chokani kwa inu…kwa Ine, inu akuchitakusaeruzika. Ine sindinakudziweni inu nkomwe.”Ndi kumenekokukhumudwako, mwawona, chinyengo chija.73 Ndi chimene ine mosalekeza…pamenepo ndi pamene inesindimamvetsetsedwa kwambiri. Sikuti ine ndimafuna kukhalawosamvetsetseka. Ine sindimafuna kukhala wosamvetsetseka,koma ine ndiyenera kukhala woona mtima. Ine ndiri ndiUthenga, ndipo Umenewo uyenera kupita kwa anthu. Izozimapangitsa kukhala wosamvetsetseka pakati pa anthu.Iwo amaganiza kuti ine ndimatsutsana ndi aliyense. Iwoakadangodziwa kuti, ndine wa aliyense, ndipo ndikuyesetsamwakukhoza kwanga kuti ndiwabweretsere iwo chomwechiri Choonadi, basi monga zimaikidwira pa mtima wangandi mmene zinaikidwira mu Baibulo umu. Ndipo Mulunguamatsimikizira izo kukhala Choonadi, kotero palibenso chinachimene tingachite za izo. Kotero, kaya iwo ayang’ana pa Icho,kapena iwo satero.74 Mwaona, iwo samafuna kuti azichiwona Icho, chifukwaiwo anagulitsa kale, anagulitsa maufulu awo akubadwakwa bungwe lina, chipembedzo china; kuti akayesere ufuluwawo wakubadwa, kuti akalowe Kumwamba pa maziko achipembedzo cha bungwe lina, chimene Satana ali mutuwa chirichonse cha izo. Mulungu sanakhalepo konse ndichipembedzo cha bungwe, sanateropo konse. Ndipo iwoamadzigulitsa kwa zimenezo, kumene iwo, gulu la amuna,amawatanthauzira Mawu ndikuti Iwo akutanthauza ichi ndipoIwo akutanthauza icho.75 Mulungu samasowa womutanthauzira. Iye amachitakutanthauzira Kwake Yekha. Iye samasowa wina aliyense kuti

Page 16: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

16 MAWU OLANKHULIDWA

amuuze Iye mmene angachitire izo. Iye ndi wochita mwayekha.Iye ananena momwe Iye akanadzachitira izo, ndipo umo ndimmene Iye ayenera kuwasungira Mawu Ake. Pamene Iye anati,“Zizindikiro izi zidzawatsatira iwo amene akhulupirira,” Iyeankatanthauza zimenezo basi. Chirichonse chimene Iye anatichidzachitika, Iye anati icho chikanadzachitika mu masikuotsiriza ano, kuti Iye akanadzachita zinthu zinazake, ndipo Iyewazichita izo. Iye samamufunsa wina aliyense ngati ili nthawiyake kapena ayi. Iye amaidziwa nthawi yakeyo, ndi lomwe liridongosolo lake.76 Tsopano, Satana, wonyenga uyu, monga zinakambidwa muMateyu 24:24, wokhala ndi chinyengo chochuluka choncho.Tsopano, ife tikupeza kuti ndi madongosolo ake a uthengawa chidziwitso, maphunziro abwinoko, mfundo zapamwamba,chitukuko, ndi zina zotero, wawalodza anthu amene akufunakuti azimutumikira Mulungu, kuwapangitsa kukhulupirirabodza lake.77 Eva sankafuna kuti achite zimenezo, koma iyeanamusonyeza iye momwe izo zinali ndi nzeru yochulukamwa izo. Iye samadziwa; iye ankafuna kuti adziwe. Iyesamazimvetsetsa, koma iye ankafuna kuti amvetsetse. NdipoMulungu anamuuza kuti asayesere kuti azimvetsetse.78 Ine ndingathe bwanji kumvetsa chirichonse cha zinthu izi?Ine sindingathe kuzimvetsa izo. Ine ndimazikhulupirira izo. Inesindisowa kuti ndizizimvetsa izo. Mulungu ndi chikhulupiriro,ndipo osati kumvetsetsa. Ife timangokhulupirira zimene Iyeananena.79 Tsopano, mufanizitse Edeni wa Mulungu kwa wa Satanatsopano, patadutsa zaka sikisi sauzande za kupotoza kwakutanthauzira kowona kwa Mawu olonjezedwa a Mulungukwa m’badwowo. Tiyeni tifanizitse izo tsopano, ndipo tiwonepamene ife tingafikepo. Monga iye anachitira kwa mpingo mu—mu nthawi ya Khristu, mwa Yesu, kuyesera kuti awabisile—awabisile ana omvera a Mulungu kuti asachidziwe Choonadi.Amenewo ndi a Mulungu. Mulungu anadzawaika ana Akekuno, zikhumbo Zake, kuti aziyanjana ndi Iyeyo pakumveraMawu Ake.80 Nanga bwanji ngati bambo anu atakuuzani inu, ndipo ndinumwana womvera kwa abambo anuwo, ndipo iwo nkukuuzaniinu, “Mwana, iwe usakalowe mmadzi amenewo kunja uko,kukasambira, chifukwa muli m’ngazi mmadzi amenewo”;ndipo wina nkubwerapo, nkudzati, “Zoonadi, madzi okongolangati amenewo, mulibemo m’ngazi mmenemo”? Tsopano inumungamvere ndani? Ngati iwe uli mwana weniweni, iweungamvere abambo ako.81 Ndipo mwana wamwamuna weniweni kapena mwanawamkazi wa Mulungu amatenga Mawu a Mulungu poyamba.

Page 17: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 17

Ine sindikusamala zomwe wina aliyense akunena za izo, iwoamatenga Mawu a Mulungu poyamba. “Muli chiphe mkapumo,”ndipo iwo akhulupirira izo.82 Pokhala ndi chikhulupiriro mu Mawu Ake onse, MbewuZake, zinabweretsa Edeni wachiyero, chikondi, ndi MoyoWamuyaya. Ndi chimene Edeni wa Mulungu anabala, chiyero.Ndipo izo zinabweretsa Edeni wachiyero, wa chikondi,kumvetsa, ungwiro, ndi Moyo Wamuyaya. Ndi zimene Mulunguakubzala, Mawu Ake, Mbewu Yake. Ndi chimene MpingoWake uti udzakhale pamapeto; Iwo udzakhala chinthu chomwechomwecho.83 Zindikirani, lingaliro lake ndi ili. Musaiwale izi. Inendidzafika kwa izo nthawi ina yake kapena Uthenga winawake.Koma, inu mukudziwa, Mulungu anati, “Musiye mbewu iliyonseibale za mtundu wake.” Kodi limenelo ndi lamulo la Mulungu?Tsopano ndi chaubwino wanji kuti mlaliki aliyense, kapenawina aliyense, kuyesera kuti awapange Mawu amenewo anenechinachake? Mwawona, Mawu aliwonse a Mulungu ndi Mbewu.Yesu ananena choncho, “Mbewu yomwe wofetsa anafetsa.”Kotero ngati Marko 16 ali Mawu a Mulungu, iwo adzabalaza mtundu wake. Ngati Malaki 4 ali Mawu a Mulungu,iwo adzabala za mtundu wake. Ndipo lonjezo lina lirilonselolikuyenera kubala za mtundu wake.84 Inumukuona,mukuona Satana kunja kuno akuziziimbaitsa?Iye akuyesera kunena kuti, “Siziri, siziri chomwecho.” Kodiinu mukumvetsa izo? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]Mwawona, Satana akuti, “O, Zimenezo si za tsiku la lero. Izo,i—izo ndi…Imeneyo inali nthawi ina. Izo, izo sizikutanthauzankomwe zimenezo.”85 “Mbewu iliyonse iyenera kubala za mtundu wake.” Umo ndimmene Mulungu anamukhazikitsira Edeni Wake. Nkulondolauko? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.] Ndipo ndi iziapa, umo ndi mmene Mulungu amawukhazikitsira MpingoWake, Mawu aliwonse monga mwa mtundu Wake! “Munthusadzakhala moyo ndi mkate wokha, koma ndi Mawu onseotuluka kuchokera mkamwamwaMulungu.” Mukuona? Satana,amatenga chinachake. Koma Mulungu anati, “Mbewu iliyonsemonga mwa mtundu wake.”86 Ngati lonjezo linanena kuti, “Zizindikiro izi zidzawatsatiraiwo amene akhulupirira.”87 Tsopano mpingo umati, “Mudzajowine mpingo.Mudzalakatule kachikhulupiriro. Mudzadziwe katekisimu.”Mulibemo zinthu zoterozo mu Baibulo lonse.88 Koma Yesu anati, “Zinthu izi zidzawatsatira iwo ameneakhulupirira: mu Dzina Langa iwo azidzatulutsa ziwanda;iwo azidzalankhula ndi malirime atsopano; ngati iwo adzatolanjoka, kapena kumwa zinthu zakupha, izo sizidzawapweteka

Page 18: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

18 MAWU OLANKHULIDWA

iwo; ngati iwo adzayika manja awo pa odwala, iwo adzachira.”Munthuwake ndi ndani amene angakaneZimenezo?Mukuona?

89 “Mbewu iliyonse idzabala za mtundu wake.” Ngati iwe ulimbewu ya Mulungu, chikhumbo, mwana wa Mulungu, ndiyekuti Mawu a Mulungu afetsedwa mwa iwe. Mukuona? Ndiyenopamene iwe uwamvaMawu aMulungu, “nkhosa Zanga zimamvaMawuAnga; mlendo izo sizingamutsatire.” Inumukumvetsa izo?“Ndiyembewu iliyonse imabala zamtunduwake.”

90 Tsopano ife tikupeza, kuti mbewu iliyonse kubala zamtundu wake, munalibemo imfa mwa watsopanoyu…muEdeni ameneyo. Simudzakhala imfa mu Edeni watsopanoyu.Mwawona, munalibemo, china chirichonse koma chiyero,ungwiro, ndi Moyo Wamuyaya.

91 Tsopano, posakhulupirira Mawu onse a Mulungu,zabweretsambewu ya chidetsomu Edeni wa Satana. Tsopano ifetikulowa kumene Satana akutenga mpando wachifumu, ngatiwotsutsakhristu, mu—Edeni wa dziko lapansi lino, Edeni watchimo, chipembedzo chopotozedwa. Iye sanayambire pakuti,“Ine ndine Satana. Ine ndine mngelo wamkulu.” Ayi, osati pazimenezo, koma pa kupotoza Mawu a Mulungu. Ndipo umondi mmene iye amawubweretsera ufumu wake, mu m’badwouliwonse. Ndipo tsopano mu m’badwo wachinyengo chachikuluuwu, wakonzekera kuti atenge mpando wake wachifumu,powagwiritsa ntchito anthu ake! Iye wadzimangira yekhaEdeni wa luntha, wophunzira, wa sayansi; kulondola, alalikiasayansi, mpingo wa sayansi, zamulungu za sayansi, chirichonsechakhala sayansi. Chirichonse chakhazikitsidwa pa maziko achidziwitso. Mpingo wonsewo wamangidwa pa chidziwitso. Iwosunamangidwe pa chikhulupiriro.

92 Nthawi ina ndinapita kukapangitsa msonkhano kumpingo wa munthu. Iyo inali nyumba yolankhuliramoyaikulu kumadzulo. Munthu wabwino, ndipo iye amakanazinthu izi zimene ife tikuzikambazi. Komabe, iye anali…Ine ndinamukonda iye; bambo wabwino, bambo wachikulire.Pamene gulu lake linatuluka…Amakhalamo pafupifupianthu sikisi sauzande. Pamene gulu lake linatuluka, mumsonkhano wa kumadzulo, pafupifupi fifitini handiredi, iwoonse anali ophunzira ovala-bwino. Ine ndinakhala pamenepondi kumawayang’ana iwo.

93 Iye analalikira ulaliki wabwino kwambiri, bamboyo anatero.Ndipo kenako anafunsa ngati alipo amafuna kumulandiraKhristu; kuti angokweza mmwamba manja awo. Ndipopalibe amene anakweza mmwamba manja awo. Ndipopotsiriza mkazi anakwezera manja ake mmwamba. Iye anati,“Chabwino, tsopano ndiwe Mkhristu,” ndipo anakamubatizaiye. Ndiyeno pamene iye anali kutuluka…Iye amadalitsa

Page 19: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 19

mwana, anamupsyopsyona mwana wamng’onoyo ndipoanamupempherera iye, ndipo anabalalitsamsonkhanowo.94 Pamene osonkhana ake anatuluka panja; onse abwino, mwasukulu, anthu ophunzira. Ndiye ine ndinali nditaima pambali,kuti ndimugwire bamboyo chanza ndi kumufunira iye madalitsoa Mulungu, pamene iye amatuluka.95 Ndipo pamene ine ndinatero, apa panadzalowa gulu langa.Iwo sanathe kuwaloleza iwo kuti alowemo pamene gulu lakelinali mmenemo. Apa panabwera langa, mu zikuku, machira,zinsaru, amisala, ndi china chirichonse. Mukuona kusiyanakwakeko? Ndi zimenezotu. Chinthu chake ndi chimenechochimene ine ndikuchikamba, mwawona. Mwawona, ndichinachake chosiyana.96 Pamene, mwa nzeru za sayansi inu mukhoza kupangaUthenga womveka, zimenezo, ndi inu, “iye amene akhulupirirapa Yesu Khristu sadzatsutsika,” mwawona.97 Koma, “Zizindikiro izi zidzawatsatira iwo ameneakhulupirira,” mwawona, iye amalephera kuti aikemo Izommenemo, mwawona. Iye anakhulupirira pa Yesu Khristu, iyeanapulumutsidwa, ngati zizindikiro izi zitsatirawokhulupirira.98 “Ndipo iye wamva Mawu Anga,” osati kungozipanga,osati kuwamva Iwo ndi makutu ake, koma, “kuwamvetsetsaIwo.” Aliyense akhoza kuwamva Iwo; wachiwerewere akhozakuwamva Iwo ndipo nkukhalabe wachiwerewere; mwawona,woledzera akhoza kuwamva Iwo; wabodza akhoza kuwamva Iwondipo nkukhalabe wabodza. Koma, “Iye amene awamvetsetsaMawu Anga, nakhulupirira pa Iye amene anandituma Ine, alinawoMoyowosatha.” Ndi zimenezotu, mwawona.99 Ndipo palibe munthu amene angachite zimenezopokhapokhapo ngati Mulungu anamudzozeratu iye. Yesu anati,“Palibe munthu amene angadze kwa Ine, pokhapokhapo AtateAnga atamukoka iye, ndipo onse omwe Atate wandipatsa Ineadzadza kwa Ine.” Ameni. Zonsezo ndi kuchita kwayekha ndikudziwiratu kwa Mulungu. Iye amakhala yekha ndipo palibealiyense yemwe amamuuza Iye choti achite.100 Tsopano, chifukwa cha kusakhulupirira, posatenga Mawuonse a Mulungu, zabweretsa mbewu ya kusakhulupirira,chidetso, utchimo, udani, ndipo imfa Yamuyaya ili mum’badwo wa mpingo wochimwa, waluntha uno. Tsopanoinu mwamva zimenezo? Mu tsiku ili, pamene dziko lonseliri lachipembedzo! Kodi inu mumadziwa zimenezo? Dzikolonseli ndi la chipembedzo. Ndipo mu m’badwo wachipembedzo uwu, matchalitchi akuluakulu pa ngodya iliyonse;chirichonse, chinthu chonsecho chikutheramwa Satana kukhalaakupembedzedwa. Ndi izi apa, ziri pomwe apa mu Baibulo.Izo nzoona. Ndipo mu maseminare aluntha, azamulungu awaamene abalamunthuwa luntha amene akuchita kuphunzitsidwa

Page 20: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

20 MAWU OLANKHULIDWA

kulankhula, zoti azichita, momwe angakhalire ndi kutengeka;ndi chirichonse monga kuwerenga maganizo, zaka firii kapenaforo, kuti adziwe momwe angamachitire ndi malingaliro amunthu. Mwaona, ndizo…101 Mzimu wa Mulungu si chinachake chimene, iwe, chimenechimaphunzitsidwira mwa iwe. Ndi chinachake chimenechinakonzedweratu mwa iwe, ndi dzanja la MulunguWamphamvuzonse. Zokuchitikira zako sizingaphunzitsidwekapena kuphunzitsidwira mwa iwe. Izo zimachitakukonzedweratu, ndi dzanja la Mulungu ndi kudziwidwiratukwaMulungu mwa iwe. Izo nzoona.102 Tsopano, izo zinabweretsa Edeni wamkulu uyu amene iwotsopano akukhalamo, Edeni wa mpingo wa dziko. Iwo onseakuyanjana pamodzi tsopano ku Ecumenical Council yaikulu,ndipo akhala ndi mpingo wa dziko onse kubwera pansi pa mutuumodzi, kumene Satana adzakaikidwe pa mpando wachifumu,ndendende basi.103 Ndipo kuitana komaliza kukupita, kukamutengaMkwatibwi Iye asanakalowe mu zimenezo. Pakuti akangokhalamu zimenezo, iye atenga chilemba cha chirombo, ndipo athedwa,iye sadzatha konse kuti adzatuluke mmenemo. Ndi chifukwachake, akuti, “Tulukani pakati pawo, anthu Anga,” zisanapitemwa iye, mwawona. “Tulukani pakati pawo, ndipo inu mukhaleopatulidwa.”104 Tsopano, udani ndi imfa, ndi kulekana Kwamuyaya ndiMulungu, mu Edeni uyu; kusilira, uve, chisokonezeko, (motani?)pofetsa mbewu zolakwika.105 Zikundikumbutsa ine za masomphenya omwe inendinawaona ndisanakomane ndi anthu a Pentekoste, a Munthuuja akuzungulira pa dziko lapansi, atavala zoyera. Inumwandimvapo ine ndikunena izo nthawi zambiri. Ndipo winaamabwerammbuyoMwake, akufetsambewu za chisokonezo.106 Koma iye anapambana izo mwabwinobwino, mwa Eva…mmunda wa Edeni, ndi kusilira kwa Eva pa tchimo; kusilirakwa Eva, pa tchimo. Ndiye, ngati Eva anasilira chidziwitso, ichochinali tchimo.107 Ndipo pamene ife tisilira chidziwitso, kumafuna Ph.D.,LL.D., ndi tchimo kuchita zimenezo. Awo ndi maneno awukali,koma izo ndi Choonadi. Ziribe kanthu kaya ndi zaukali bwanji,izo ndi Choonadi apobe, mwawona. Kusilira chidziwitso,kumvetsetsa!108 Chinthu chake ndi chakuti, ndi, lero sitikuyesera kutitikhazikitse Mawu aMulungummitima ya anthu. Ife tikuyesetsakumadzikhazikitsa tokha. Mipingo ikuyesetsa kukhazikitsachiphunzitso champingo, mumtimawamunthu.

Page 21: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 21

109 Ife tinalamulidwa kuti tidziwakhazikitsa Mawu a Mulungu.Paulo anati, “Ine sindinabwere kwa inu ndi mawu odololaa munthu, kuti chikhulupiriro chanu chikakhoze kukhazikikamu chidziwitso cha munthu; koma ine ndikubwera kwa inumu mphamvu; mu mawonetseredwe a Mzimu Woyera, kutichikhulupiriro chanu chikakhazikike mwa Mulungu.” Ndizimenezotu.

110 Munthu asamadzikhazikitse yekha. Ife timazipeza izopakati…Mulungu angomuchitira chinachake munthu ndikumutumiza iye azipita, inu mukapeza munthu wina aliyenseakuyesera kutsanzira izo. Mwawona, iwo akuyesetsa kutiadzikhazikitse okha. Munthu aliyense, “Ine ndinachitaizi. Ineyo, ine, changa, chipembedzo changa, ine, ichi,”kudzikhazikitsa okha. Kodi ife tikulalikira chiani, eniakefekapena Ufumu wa Mulungu?

111 Tidzikhazikitsa Mawu a Mulungu. Tidzichotsamokusakhulupirirako ndipo tizikhadzikitsamoUfumuwaMulungumu mtima wa munthu. Ndipo Ufumu wa Mulungu sungakhozekukhadzikitsidwa mu mtima wa munthu pokhapokhapo ngatiMulungu anamupanga munthu ameneyo chomwecho. Iyesangakhoze kukhadzikitsidwa mu…

112 Ndipo, kumbukirani, gawo la chinyengo, ndi limene anthuamaganiza kuti ndi zolondola. Mwaona. “Ilipo njira yomweimawoneka yolondola kwa munthu.” Munthu aliyense woganizaamaganiza kuti ndi zolondola.

113 Monga mmene ine ndinakuwuzirani inu ma Lamlunguangapo apitawo; pamene ine ndinaima pafupi ndi mwanawanga akufa, ndipo Satana nditaima pamenepo ndipo anati,“Abambo ako ndi awo, anamwalira mmanja mwako usiku wina.Mkazi wako ndi uyo wagona ukoyo mu—mosungira mitembo,ndipo apa pali mwana wako akupita. Ndipo iwe unamupemphaIye kuti akuyankhe iwe, ndipo Iye wakokera chako…Iyewakokera chotchinga pa iwe. Tsopano, ndipo komabe Iyeyo ndiMulungu wabwino, ndipo komabe iwe ukuti Iye ndi Mchiritsi.Ndipo iwe, amene ukuima ndi zomwe iwe umati zinali zoona,iwe ukulakwitsa.” O, kuganiza kulikonse, maganizo aliwonseankayenera kuvomereza kuti izo zinali zoona; ndipo iye analikulondola, pamenepo.

114 Monganso iye anali kulondola pamene anamuuza Eva,“Maso ako adzatseguka, ndipo iwe udziwa chabwino ndichoipa. Ndipo iwe udzakhala ngati milungu, mwanjira imeneyo,wodziwa chabwino ndi choipa,” chifukwa Mulungu sanawaloleiwo kuti aziwone okha apobe, kuti iwo anali amaliseche. Koteroiwo anadziwa kuti iwo adziwa chabwino ndi choipa; ndipo iyeanali kulondola. Koma, inu mukuona, izo zinali zotsutsana ndiMawu a Mulungu.

Page 22: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

22 MAWU OLANKHULIDWA

115 Ndi momwemonso amachitira atumiki mmaseminare,kumaphunzira zamulungu zopangidwa ndi anthu; izo zikhozakuwoneka zolondola, izo zikhoza kukhala kumvetsa kwabwinokwa chinthucho, koma izo nzolakwika.116 Ife sitisowa kuwamvetsetsa Iwo. Ife timawakhulupirira Iwochifukwa Mulungu anati ndi choncho, ndipo izo zikukhazikitsaizo kwanthawizonse. Chinthu chonsecho, ndiyo njira yakeyokhulupirira Iwo.117 O, momwe Eva ankasililira atakhala ndi Ph.D., mwaona,momwe iye ankasililira atakhala wanzeru kuposa chimeneiye anali!118 Zindikirani momwe analiri ofanana, mwamuna ndi mkaziwake…Tsopano zindikirani, mwamuna ndi mkazake, onse alimalisechemmundawa Edeni, Edeni waMulungu.119 Tsopano ine ndikutseka. Ine ndinati ine ndingotengamphindi pang’ono. Taonani, penyani, pamene ndikutseka.120 Mufanizitse izi tsopano, momwe analiri ofanana mwamunaameneyo ndi mkazi wake, onsewo anali mu Edeni wa Mulungu,opanda nsoko uliwonse wa zovala pa iwo, ndipo sankadziwa izoayi. Pakuti nchifukwa chiyani iwo samadziwa izo? Chifukwaiwo anali ataphimbidwa ku zokhudzira zawo za umaliseche,ndi Chophimba Choyera, cha Mzimu Woyera. Iwo ankathakuyang’anizanawina ndimzake, ndipo iwo osamadziwa kuti iwoanali amaliseche. Iwo anali ataphimbidwa ndi Mzimu Woyera,wa chiyero. Iwo anali ataphimbidwa.121 Chophimba cha Mulungu, chiripobe lero, ukhozakuyang’ana ndipo osasilira. Iwo amatembenuza mutu wawo.Icho ndi Chophimba Choyera, mwawona, Chophimba Choyera.Mulungu anali ndi maso awo…iwo anali onse awiri, winayoanali mwamuna ndipo winayo anali mkazi, ndipo iwosankadziwa kuti anali amaliseche, chifukwa chiyero chaMulungu chinkapangitsa maso awo kukhala ataphimbidwa.Zindikirani, Mulungu anabisa chikumbumtima chawo kwatchimo, pogwiritsa ntchito Chophimba Choyera.122 Ndikukhumba ife tikanakhala nayo nthawi ina kutitikhazikike pa zimenezo, maminiti pang’ono. Taonani apa,“Pakuti iye, wopembedzayo akayeretsedwa kamodzi,” Ahebri,“wopembedzayo akayeretsedwa kamodzi, samakhalanso ndichikumbumtima cha tchimo.” Tchimo lachokako kwa iye.123 Ine ndimamumva M’bale Neville akunena, mmawa uno;winawake ayenera kuti amamufunsa iye chifukwa chimene inesindinalalikire pa Mzimu Woyera, ndi chifukwa chiyani inesindinachite izi. Ndi izi apa. Mzimu Woyera ndiye ntchitoyomwa iwe. Iwo ndi Moyo, osati zotengeka; osati mtunduwina wa umboni wa chithupithupi. Koma Iwo ndi Munthu,Yesu Khristu, Mawu a Mulungu atakhazikika mu mtimamwanu, kuti akafulumizitse Mawu aliwonse a m’badwo uno.

Page 23: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 23

Kulondola. Kumawuwona Mzimu Woyera ukugwira ntchito,osati mochuluka kwambiri mu zowonetsera; koma, kumagwirantchito, zomwe Iwo ukuchitamolingana ndiMawu.124 Zindikirani tsopano Mzimu Woyera, wa Mawu Oyera aMulungu, unali ndi mwamuna ndi mkazi ali maliseche, ndipoosadziwa izo. Zokongola bwanji, Moyo wa Mawu; Mbewu,Mawu!125 Mulungu anati, “Pali mtengo pakati pa mundawo, mkazi.Ndipo pakati pa munda pali mtengo uwu; musadzawukhudzekonse iwo. Pakuti, tsiku limene inu mudzadye za iwo, tsikulimenelo inu mudzafa.” Iwo anali ataphimbidwa ndi choyerakwa iwo, sankadziwa kalikonse za iwo, musadzayerekezekuwukhudza iwo.126 Iwo anali ataphimbidwa ndi choyera. Iwo anali otetezekamuchihema cha Mulungu. Iwo anali ali amoyo. Iwo analibe imfapowazungulira iwo. Aleluya! Iwo anali ndi chikondi changwirokwa wina ndi mzake, Moyo wangwiro kwanthawizonse. Iwoanali ndi chikondi changwiro, kumvetsetsa kwangwiro kwachikondi cha Mulungu. Iwo anali ndi Mawu a Mulungu, ndipoankawasunga Iwo. Ndipo anali a moyo ndiponso otetezeka muEdeniwaMulungu, analibe imfa, nkomwe, powazungulira.127 Kenako, Satana anampangitsa Eva kuti akamvereuthenga wake wa zamulungu, uthenga wa chidziwitso,kuphunzira kwapamwamba, machitidwe apamwamba,chitukuko chabwinoko, maphunziro apamwamba, ndi zinazotero; kenako pamene iye anampangitsa…iye kuti aimendi kumumvetsera iye miniti, ku zoganiza zakezo (zomweife tinalamulidwa kuti tiziziponyera pansi), pamene iyeanampangitsa mkaziyo kuti amvetsere kwa izo.128 “Tsopano, taonani apa, mpingo ndi wakuti-wakuti. Iwounakhazikitsidwa kale kale. Ndife umodzi wa mipingo yakalekwambiri mu dzikoli. Kumene ameya a mzindawu amapitako.”Ine sindikusamala kuti iwo ndi chiyani, mwawona. Ngati iwoumatsutsana ndi Mawu a Mulungu, muzitsutsana nawo iwo.Ameneyo ndi mdani wanu. Chirichonse chimene chikutsutsanandi Mawu ndi mdani wako.129 Chirichonse chimene chiri cha Mawu ndi m’bale wako. Iyeyondi gawo la iwe.130 Zindikirani, iye anavula Chophimba Choyeracho, kutiakawone kuti kugonanako kunali chiyani kwenikweni;mufanizitse zimenezo, chimene kusilira kungachite kwenikweni.Iye anachotsapo Chophimbachommasomwake, chinthu choyerachimene Mulungu anali atachiika mmaso ake. Iye ankafunachidziwitso, kuti adziwe kuti zonsezo zinali chiyani; kotero iyeanachotsapo Chophimbacho kuti awone kuti chonsecho chinalichiyani. Iye anakamvetsera kwa mdierekezi, ndipo zindikiranimalo omwe izo zinamuikapo iye.

Page 24: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

24 MAWU OLANKHULIDWA

131 Iwo akhala akuchita zomwe zomwezo mum’badwo uliwonsekuyambira pamenepo, nthawizonse kumatenga mbali ya luntha;ndipo tsopano amanga ufumu wa Satana, chidziwitso, mbewuyake yomwe iye anafetsa, ndipo alipanga dziko lapansi kukhalaEdeni wa imfa.132 Tsopano zindikirani. Tsopano tayang’anani paChivumbulutso 3, M’badwo wa Mpingo wa Laodikaya. Iwemuziganizire izo mmalingaliro anu.133 Tsopano zindikirani. Iye, Eva, ndi mfumukazi ya Satana.Mwawona, Satana, serpenti, anafika kwa Eva asanapitekoAdamu kwa iye. Mukuona? Izo nzoona. Kotero iye anamunyengamkaziyo,mwawona; kotero Satana, serpenti, analimwamunawaEva asanadziwidwe ndi Adamu. Mwawona, iye anamunyengamkaziyo. Baibulo limati iye anatero, ndipo iye anazindikira kutianali maliseche, pamenepo. Mukuona?134 Tsopano taonani pa—M’badwo wa Mpingo wa Laodikaya.Iye, Eva, wakhala ngati mfumukazi ya Satana. “Iye ndiwolemera mu katundu wa mdziko; wakhungu, wamalisechekachiwiri, ndipo sakudziwa izo,” chimodzimodzi basi mongammene zinaliri mu Edeni wa Mulungu. Koma tsopano, osatichifukwa chakuti Chophimba Choyera chiri pankhope yake,koma chophimba cha kusilira. Chimene, iye anachotsapoChophimba Choyera cha Mulungu, ndipo anadzavalachophimba cha chidziwitso, cha kusilira. Ndipo tsopano iyeali ndi chophimba cha kusilira, mwakuti iye ndi “wakhungu”kwa izo kuti ndi tchimo. Iye ali “wamaliseche” pa msewu,“ndipo sakudziwa izo ayi.” Iye ndi wachiwerere pa msewu.Akazi atavala makabudula awa, pamaso pa Mulungu, ndiachiwerewere, “ndipo sakudziwa izo ayi.”135 Zindikirani, muwatenge akazi athu. Tsopano, ngati inumukufuna kuti muwone chikhalidwe chomwe mpingo ulimo,muwone momwe akazi akuchitira. Iye nthawizonse amaimirampingo. Mu Edeni wa Satana, wa tchimo ndi kusakhulupirira,kupotoza kwa chipembedzo; ufumu wopotozedwa. Mmalomotenga Mawu a Mulungu, iwo atenga kuphunzira kwa lunthakwa munthu. Ndipo mmalo motenga Mpingo, iwo atengabungwe, ndipo iwo akuwubweretsa iwo ku mutu umodziwawukulu.136 Tsopano zindikirani, kupotozedwa kuchoka ku kusalakwa.Musaphonye izi tsopano. Mpingo wakhala utavala chophimbachosilira ichi. Zindikirani chimene icho chachita kwa iwo.Icho—icho chawupotoza iwo kuchoka ku kusalakwa kupitaku chidziwitso. Mukuona? Chophimba Choyera, iye analiwosalakwa; ndi chophimba cha kusilira, iyeyo ndi chidziwitso.Iye akudziwa kuti ndi chokoma. Iye akudziwa chimene ichochimapanga,mwaona. Icho ndi chipatso, mtengowokhumbirika,womupangitsa wina kukhala wanzeru. Mukuona? Iye

Page 25: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 25

wapotozedwa kuchoka ku kusalakwa kupita ku chidziwitso,wachoka ku chiyero wapita ku nyansi ndi kusilira, ndipowachoka ku Moyo wapita ku imfa.

137 Ufumu uwu uyenera kufa. Ufumu uwu udzafa! Mulungu waKumwamba adzawuwononga iwo kuwuchotsapo pa nkhope yadziko lapansi.

138 Zindikirani, mu kupotoza uku, izo zakhala kuchoka kwamwamuna zapita kwa mkazi, ndipo zachoka kwa mkazi zapitakwa mwamuna, “ndipo sakudziwa izo ayi.” Chida chabwino chaEdeni wa Satana, ngati inu mungayang’ane mmisewu lero, paanthu athu amakonowa.

139 Zindikirani, anali Eva amene Satana anamugwiritsa ntchitokuti amupangitse Adamu kuchimwa ndi mphamvu yake yakusilira. Tsopano chomwecho, akuchita chinthu chomwechomwecho lero. Zindikirani, tsitsi lodula, nkhope yopentedwa,kumavala modolola, mwawona, iye akuchita zimenezo, ndiposakudziwa kuti zirizonse za zinthu zimenezo ndi zotsutsanandi Mawu a Mulungu. Akadula tsitsi lake, zikumupangitsaiye kukhala mkazi wosalemekezeka, wachiwerewere. Akavalamakabudula, zikumuika iye kukhala wonyozeka. Akavalazovala zodolola, zikumupangitsa iye kukhala wachiwerewere.“Ndipo iye sakudziwa izo ayi,” osati chifukwa cha chiyero chaMulungu; chifukwa cha kusilira kwa Satana. Iye akumupangitsawake…Iye akumupangitsa Adamu wake kuti azimusiliraiyeyo.

140 Iye anavula zovala zimene Mulungu anamuvekamo iye,kumbuyoko mu Edeni, zoti ayende nazo mu ulendowu—mchipululu ichi. Iye anazivula izo. Iye anadzivula yekha.Pamene, Mulungu anali atamukutira iye paliponse pa khungulo;iye anayamba kumazivulapo pang’ono nthawi iliyonse, tsopanoiye wabwererammbuyo komwe anali pachiyambi.

141 Tsopano iye wamupanga Adamu wake kuti adzivalazovala zake zamkati. Mwamuna akumavala makabudula akaleowoneka mwachikazi awo, ndi kumatuluka nazo kuno, inesindikuganiza kuti muli umuna wochuluka mwa iyeyo. Iyeyondi wachikazi wamkulu amene ine ndikumudziwa. Mukuona?Mwawona, iye wamupanga Adamu wake wopotokayo kutiazichita monga iyeyo, mwawona, akumavala zovala zakezamkati. Iye wawona zomwe iye angachite kunja uko iye atavulazovala zake zonse nkusiya zamkatizo. Makabudula amenewo.Zoona, zimenezo ndi zovala zamkati za mkaziyo, ndipo apaAdamu wake akuvala izo tsopano. Chimene, molingana ndiMawu apachiyambi a Mulungu, “Ndi chonyazitsa kuti mkaziazivala chovala choyenera mwamuna, ndi mwamuna kumavalazovala zoyenera mkazi,” kuchokera ku Mawu apachiyambi.Taganizani za izo!

Page 26: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

26 MAWU OLANKHULIDWA

142 Tsopano, mwamunayo tsopano akuweta tsitsi la mkaziyo,nayenso. Iye akumalipesera ilo pansi, nkuikamo zolipotolerammenemo. Ena a mawonekedwe odwalitsitsa kwambiri ameneine ndinayamba ndawawonapommoyowanga, ndi ena a ana awokunja kuno lero okhala ndi tsitsi lawo atalipesera pansi mongachonchi, ndi lopentedwa, tsitsi lotsukulutsidwa, ndi mtunduwina wa mankhwala a peroxide enaake, ndi kulitsukulutsatsitsi lawolo, ndi kulipiringiza ilo mu zolipotolera, zokonzeratsitsi. Iwe wachikazi wamkulu! Chimenecho ndi chinthu choipakuchinena pa guwa, koma chiweruzo chimayambira mnyumbaya Mulungu. Iwe sukudziwa nkomwe kuti ndiwe mwamunakapena mkazi. Ndipo ine ndamva kuti Ankhondo athu a UnitedStates azikhala mmakabudula posachedwapa. Izo nzoona.Mukuona chimene kupotozako kuli? Izo ndi zovala za mkazi;akuweta tsitsi la mkaziyo.143 Tsiku lina ine ndinali uko kwa, Howard Johnson; osatiuyu kuno, koma uyo wa ku msewu wotulukira. Ndipo inendinangokhala modabwitsidwa. Apa panabwera mnyamatawamng’ono, atatsegula kamwa yake. Ndipo iye anali nditsitsi lakuda apa, ndipo analipesera ilo mbali iyi; ndipoanaikamo zolipotolera mmenemo, ndipo analipiringiza ilomozungulira, pamwamba pa maso ake; akuyang’ana motuzulamaso ake, akuyendayenda. Ngati ine ndinayamba ndawonapochisokonezo! Mwawona, iye sakanakhulupirira izo. Iyemwinamwake akanakhoza kutsimikizira kuti anali mwamuna,koma mu mzimu wakewo iyeyo anali mkazi. Iye sakudziwakuti ndi mbali iti ya nyumba yomwe iye alimo. Izo nzoona.Zasokonezeka bwanji!144 Ndi zimene Satana akuchita. Iye akusokoneza mafuko.Iye akusokoneza mpingo. Iye akuwasokoneza anthu. Iyeyo ndiwachinyengo, wosokonezawaChoonadi chapachiyambi.145 Mulungu anampanga mwamuna kukhala mwamuna.Anampanga mkazi kukhala mkazi. Ndipo Iye anawaveka iwomosiyana, ndipo Iye ankafuna kuti iwo azikhala mwanjiraimeneyo ndi kuti azichita mwanjira imeneyo; winayo ndiwamkazi, ndipo winayo ndi wachimuna. Iye anamulekanitsaAdamu mmunda wa Edeni, ndipo anachita izi, anamulekanitsaEva kwa iye.146 Tsopano akuweta tsitsi la mkaziyo; iye akudula tsitsi lakengati mwamunayo, ndipo mwamunayo akuyesera kumawetalake ngati la mkaziyo. Mukuona? Mkaziyo akumavala zovalazakunja za mwamunayo, ndipo mwamunayo akumavalazovala zamkati za mkaziyo. Tsopano, zimenezo zikumvekamosinjirira, koma ine sindikutanthauza izo mwanjira imeneyo.Icho ndi Choonadi cha Uthenga mwamtheradi. Ngati inusimukuzidziwa izo, ndiye kuti pali chinachake cholakwikandi inu; mwinamwake ndinu akhungu kapena simunayambemwakhalapo pa misewu. Ndipo mkaziyo amaganiza komanso

Page 27: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 27

mwamunayo amaganiza kuti izo nzabwino, iwo akuyanjanalimodzi penapake.

Akazi amati, “Chabwino, kukutentha kwambiri!”147 Amwenye akale a Apache kutali uko akhoza kukuchititsanimanyazi inueni. Iwo akamakhala ndi kutentha kochuluka, ndipamene iwo amavala zovala zambiri, kuchitira kuti dzuwalisawawotche iwo; o, kupangitsa thukuta, kuti iwe uzikhala ndizokuziziritsa pamene ukuyenda. Mukuona? Iwo amaima kumenepa dzuwa.148 Inu simungaime nazo; inu mukhoza kuchita matuzandi kuwotchekapo. Koma, inu mukuwona, ndi zimene inumumadzitcha maphunziro apamwamba. Sayansi yamakonoyabala zimenezi. O, mai! Ndi ameneyo apo, “wamaliseche,” muLaodikaya, “ndipo sakudziwa izo ayi.”149 Iye anali wamaliseche mu Edeni. Mukuwawona maufumuawiriwo akufanana? Umodzi ndi wa tchimo ndi imfa; winawondi wa Moyo ndi chirungamo. Mmenemo iye anaphimbidwandi Chophimba Choyera. Iwo onse anali a maliseche; iwosankadziwa izo ayi. Iwo sankadziwa kanthu za izo, chifukwa iwoanali ataphimbidwa ndi MzimuwaMulungu.150 Ndipo kuno iwo aphimbidwa ndi chisiliro, ndipo iwoamayang’anizana pa wina ndi mzake ku…Mwawona, Adamuankakhoza kuyang’ana pa Eva, ndipo osamadziwa kuti iye analimaliseche. Koma tsopano ndi chophimba cha chisiliro ichi, iyesakuzindikira kuti ali maliseche, koma iye akuchita izo pansipa chophimba cha chisiliro ichi kuti azimupangitsa mwamunakuyang’ana pa iye. Ndi chinthu chokhacho chimene iye angathekuchitira izo. Inu simukukhulupirira zimenezo, koma inumumachita izo mulimonse, ndipo mwamuna amayang’ana.Ndipo iye anapeza kuti inu muli ndi chikoka chochulukakwambiri, mpaka iye anabwerapo ndipo anadzavala zina zazovala zanuzo iyemwini.151 O, ndi chisokonezeko bwanji! M’badwo wotani! Ndi nthawiyanji imene ife…Ndi zachinyengo bwanji izi! O, zinthu zonseizi, “ndipo osadziwa izo ayi,” mzimu wopotozedwa mwangwirouli mwa mwamunayo. Iye waphimbidwa kwa chisiliro chaSatana, ndipo mkaziyo watero, nayenso. Iwo ndi mzimuwa usatana wa gulu lalikulu. Mwawona, iwo sakudziwa,koma iwowo ndi bungwe. Akazi ovala makabudula, ali abungwe. Mwamuna wovala monga choncho, ali wa bungwe.Ine ndikupatsani inu kulemba kwachidule kwake, B.S.S.,Big Sister Society, [Gulu Lalikulu la Alongo—Womasulira.]kotero ndi chimene iwo alimo. Kumatuluka kumeneko, gululalikulu lachikazi, atavala matharauza akale aang’ono awo,mawonekedwe aakulu akale onyansa, chinthu chowoneka-mwauve. Ine—ine…

Page 28: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

28 MAWU OLANKHULIDWA

152 Anthunu, tsopano inu mukhoza kutsutsana nane ndi izi,koma izo ndi Choonadi. Inu mwapotozedwa ndipo simukudziwaizo ayi. Simuli ayi, simukuchitanso monga mwamunapanonso. Mwawona, mukufewera fewera; ndipo, mwana wawowamwamuna, sakhalanso kanthu kwa iwo panonso; amuna,ndi akazi, nawonso. Iwowo ndi gulu. Ndi limenelo bungwelo.Bwanji? “John, khomo linalo, amavala makabudula, ndiye inendisiyirenji? Luella amafuna kuti ine ndizivala iwo chifukwaJohn amavala iwo, khomo linalo. Ndipo, chabwino, ngati—ngati Susie Jane amatha kuvala iwo, chomwechonso MarthaJane akhoza kuvala iwo, kapena Susie Lou,” kapena aliyenseyoamene dzina lake liri, mwawona. Mwawona, ilo ndi gulu. Ilo ndibungwe. Inu mwauzimu ndinu a limenelo, ndipo simukudziwaizo ayi.153 Ndipo ngati izo ziri chomwecho, ndipo ife tikuwonakuti ziri chomwecho, inunso mwachititsidwa khungu. Inumwachititsidwa khungu ku zipembedzo izi zomwe Satanawakusokonezeranimo inu. Ndipo uko ndi kupotoza kwa Mawua Mulungu a pachiyambi, ndi Ufumu Wake, ndi dongosolo Lakekwa anaAke. Satanawawasokoneza amuna ndi akazi kuti alowemu zinthu izi, ndipo iwo sakudziwa izo ayi. Apotozedwa!154 Salinso mwana wamwamuna wa Mulungu! Tsitsilikumazendewera pansi pa nkhope yake, ndiponso atavalakabudula, kumayenda pa msewu; mwana wamwamuna waMulungu, dikoni mu mpingo, m’busa pa guwa? Ayi, ameneyosi mwana wamwamuna wa Mulungu. Iye sanabwere podzeramu Sefa ya Mulungu yoganizira. Iye sibwenzi akuvala zovalazachikazi zimenezo; iye ndithudi sibwenzi akutero; komansomkaziyo sibwenzi akuvala zovala za mwamuna. Mwaona,iyeyo si mwana wamwamuna wa Mulungu. Iye ndi mwanawamwamuna wa Satana, ndiponso mwana wamkazi wa Satana.Chinthu chovuta kuti uchinene!155 Satana wapambana mu kusokoneza ndi kulilanda dzikolapansi lino, ndi kulipanga ilo kukhala ufumu wake; limenemunthu anayikidwamo, mwa ufulu wochita mwakufuna kwake,kuti azidzisankhira yekha mtundu wa moyo umene iwoakuwufuna. Ndipo izo zimasonyeza zimene ziri mu mtima wako.Mukuona? Liwu lako…Inu mukudziwa chiyani? Zochita zakozimaphokosera kwambiri, izo zimameza zonena zako.Uh-huh!156 Ine nditapita kwa munthu. Ndi kukati, “O, ine…Ndifetonse Akhristu. Ife ndi a mpingo.” Ndipo odzivula ali paliponsepa ofesi yake? Huh! Izo sizingapange kusiyana kulikonsekondi zimene iye wandiuza ine, ine ndingadziwe bwinoko;chomwechonso inu.157 Mungamulole mkazi kumanena kuti iye ndi Mkhristu, alindi tsitsi lalifupi? Huh-uh! Inu mukudziwa bwinoko kuposazimenezo, mwawona. Inde, bwana. Mungamulole iye kumanena

Page 29: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 29

kuti ndi Mkhristu, atadzipentapenta ndi zodzoladzola, ndimakabudula, ndipo nkumanena kuti iye ndi Mkhristu? Inumukudziwa bwinoko kuposa zimenezo. Mawu a Mulunguamakuphunzitsani inu zabwinoko kuposa zimenezo. Mawuamanena kuti iye sangathe kuchita zimenezo ndi kukhalaMkhristu. Iye ndi wosalemekezeka nkomwe, ndi chirichonse.Mulungu angadzachiike bwanji chinthu chopanda ulemu muUfumu Wake? Ayi, bwana, ayi mpang’ono pomwe. Ayi, bwana.Iwoeni, iwo akusonyeza chokhumba chawo.158 Inu simungaipange nkhunda kuti izidya ndi khwangwala,ayi mpang’ono pomwe. Nkhunda ilibe ndulu iliyonse. Iyosiingadye nyama yovunda iyo. Ngati iyo italuma pang’ono,iyo ingamuphe iye, ndipo iyo imadziwa zimenezo. Komakhwangwala akhoza kudya pafupifupi chirichonse chimene iyeakufuna. Mukuona? Iye ali ndi ndulu yambiri.159 Kotero ndiye inu mukupeza kuti, umo ndi mmene ziliri ndidziko lero, chinthu chomwe chomwecho, “Iwo ali amaliseche,akhungu, ndipo sakudziwa izo ayi.”160 Satana anachita izo ndi chisiliro cha mkazi pofunachidziwitso, cha kugonana, chimene iye anasankha mwakusankha kwake kwake. Tsopano zindikirani, anali Eva ameneanamutsogolera Adamu kuti akachite cholakwika, ndipoanali mkazi amene anavula zovala zake Adamu asanavulezake. Mukuona? Amakhala mkazi, nthawizonse. Nthawizonsewakhala ali. Zikadali panobemwanjira yomweyo.161 Ndi mpingo umene umamusocheretsa munthu. Ndi mpingo,mwawona, umene umamutsogolera munthu amene amafunakuti akhale mwana wa Mulungu. Ndi mkazi, mpingo. OsatiBaibulo, Mulungu, pakuti Baibulo ndi mwamuna. O, eya,“Mawu anasandulika thupi,” ndipo Iye anali Mwamuna.Mukuona? Baibulo ndi mwamuna; mpingo ndi mkazi. Mukuona?Siunali mpingo…Baibulo limene limamusocheretsa munthu.Ndi mpingo umene umamusocheretsa iye. Ndi mpingo umeneiye anayenda nawo ali maliseche, osati Baibulo. Mukuona?Ayi, ndithudi. Baibulo limamuuza iye kuti ali maliseche. Inde,bwana.162 Tsopano zindikirani momwe, mwa kugonana, chikhumbocha kugonana, iye anasilira chidziwitso, kuti akadziwe kuti ichindi chiyani, ndi momwe, ngati chipatso ichi chinali chabwinokapena ayi. Ndipo iye anachita izo.163 Mulungu adzalilandanso ilo tsiku lina, ndithudi,ndi Mwamuna. Ilo linaperekedwa ndi mkazi. Koma ilolinawomboledwa ndi Mwamuna; Mwamuna, Yesu Khristu,amene ali Mawu.164 Ndiyeno ndi chiyani zimenezo? Zindikirani, potseka. Kunoosati kale litali, ine ndinanena maneno awa. Ine ndiri ndipafupifupi masamba foro kapena faivi ena pamenepo, koma

Page 30: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

30 MAWU OLANKHULIDWA

ine…a Malemba ndi zinthu zimene ine ndimafuna kutindilozereko. Koma,mvetserani. Tiyeni titseke, ponena izi.

165 Kumbukirani, kuno osati kale litali, ine ndinalikukuphunzitsani inu pa Malipenga Asanu ndi awiri, PhwandoLa Malipenga, ndi zina zotero. Ndipo ine ndinati, “Paliphwando la tsiku la chisanu ndi chitatu.” Kotero, tsiku lachisanu ndi chiwiri lingakhale lotsiriza, limenelo lingakhaleZakachikwi. Koma pali phwando la tsiku la chisanu ndichitatu; limene, ngati ilo linali la chisanu ndi chitatu,ndipo pali masiku asanu ndi awiri okha, zingalipangitseilo kukhala tsiku loyamba aponso, kubwereranso ndithu kutsiku loyamba. Ndiye, zikadzati Zakachikwi zatha, ndiyepadzakhazikitsidwanso Edeni kachiwiri. Ufumu wawukuluwa Mulungu udzabwezeretsedwanso. Chifukwa, Yesu anachitakumenyanirana iwo ndi Satana, mmunda wa Getsemani, ndipoanamutenganso Edeni; amene, Iye anapita kuti akatikonzereKumwamba, kuti adzabwererenso kachiwiri, nkudzapitansoKumwamba. Iye anati, “Mitima yanu isavutike.”

166 Pamene Iye anali kuno pa dziko lapansi, Iye anati,“Inu, inu Ayuda, mwakhulupirira pa Mulungu. Tsopano, Inendikudziwa kuti ine ndiri ndi dzina loyipa,” Iye anati. “Ndipoiwo amati Ndine wakuti, winayo. Koma, inu mwakhulupiriramwa Mulungu; ndipo pamene inu mwakhulupirira mwaMulungu, mukhulupirirenso mwa Ine.” Iye anali Mulungu,akuwonetseredwa.Mukuona? “Mukhulupirirensomwa…”

167 “Mnyumba ya Atate anga alimo ambiri…” Kapena, “Muchuma cha Atate anga, mu madongosolo a Atate Angamuli nyumba zambiri. Ine ndikupita kukakukonzerani malo.”Taonani kutalika kwake, amphwamphwa mamailosi fifitinihandiredi! Mukuti, ali kuti iwo? Iye anapita kuti akatikonzereiwo. Iyeyo ndi Mlengi. Iye akulenga golide yense ameneyo.Misewuyo ndi yamandala. Iyeyo ndi Mlengi. Iye akukonzamalo. Mu Chivumbulutso 21, iye anati, “Ndipo ine YohanendinawuwonaMzindawoyera, YerusalemuWatsopano, ukutsikakuchokera kwaMulungu kuchokera Kumwamba.”

168 “Kunalibenso nyanja; kumwamba koyamba ndi dzikolapansi loyamba zinachokapo.” Kodi miyamba yathu yoyambainali chiyani? Inali Zakachikwi. Kodi dziko lapansi loyambalinali chiyani? Linali ili. Ilo lidzakonzedwanso. Chimodzimodzimonga mmene ilo linabatizidwa ndi Nowa, mu masiku akulalikira kwake; linadzayeretsedwa ndi Khristu, pamene Iyeanadzakonkha Magazi Ake pa ilo; ndipo lidzakonzedwanso,adzachotsamo majeremusi onse ndi chirichonse kuzichotsa pailo, mu kukonzanso pamapeto, ndi ubatizo wa Moto umene utiudzaphe jeremusi iliyonse, matenda aliwonse, nthenda iliyonse,chonyansa chirichonse chimene chinakhalapo pa dziko lapansi.

Page 31: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 31

169 Ilo lidzaphulikapo, ndipo padzatulukirapo DzikoLatsopano. “Ndipo ine ndinawona Kumwamba Kwatsopano ndiDziko Latsopano. Kumwamba koyamba, dziko lapansi loyambaili, linachokapo; ndipo uko kunalibekonso nyanja. Ndipo ineYohane ndinawuwona Mzinda woyera, Yerusalemu Watsopano,ukutsika kuchokera kwa Mulungu kuchokera Kumwamba.”Kumeneko Mulungu adzakakhala ndi zikhumbo Zake zenizeni,ana aamuna ndi aakazi, kumene Iye azikayanjana ndi iwomu chiyero, ndi maso awo atachitsidwa khungu kwa tchimolirilonse. Uko sikukakhalanso tchimo kuchokera pamenepompakana.170 Tiyeni ife tilimbikire zolimba; musanyengedwe mu tsiku lalero, koma, “muzilimbikira kutimukalowe pa chipatacho.”171 “Pakuti onse omwe adzasiyidwe kunja adzakhala achigololo,osilira.” “Yense amene ayang’ana pa mkazi ndi kumusilira iyewachita naye kale chigololo.” Onse a…kunja kudzakhala akazia mbiri yoipa, amuna ambiri yoipa, ndi ena otero.172 Ndipo okhawo amene ali owomboledwa, ndipo ali mu Bukhula Moyo wa Mwanawankhosa, adzakalowa pa chipatacho.Kotero limbikirani, abwenzi; musanyengedwe mu tsiku lotsirizalino.173 Ino ndi nthawi yopambana. Aliyense ali nazo ndalama.Aliyense akhoza kuchita izi, ndipo aliyense akhoza kuchita izo,ndipo ndalama zikuyenderera paliponse, ndi magalimoto akuluakulu, ndi chirichonse. Simudzakhala chirichonse cha zimenezomu Mzinda umenenewo. Simudzakhala galimoto imodzi, ndegeimodzi. Ayi. Icho chidzakhala chonse palimodzi chitukukocha mtundu wina. Icho chidzakhala aponso chitukuko osaticha chidziwitso, osati cha sayansi, koma cha kusalakwa, ndichikhulupiriro mwaMulungu wamoyo.174 Tiyeni ife tilimbikire kuti tikalowe Mmenemo. Pakutindicho cholinga changa chonse, ndi kuti ndidzakalowe muMzinda umenewo tsiku lina; ndipo ndikadzayang’ana mmbuyo,mudzakhale mukubwera nane limodzi, ndidzakuwonenialiyense wa inu mukuguba, pamene ife tizidzaimba, “oyeraakalowa.” Ine ndikufuna ndidzakhale mu chiwerengerochimenecho pamene oyera azidzalowa.

Tiyeni tipemphere.175 Wokondedwa Atate Akumwamba, pamene masiku akutseka,ndipo ife tikuwawona iwo akuyandikira, lonjezo likuyandikira.Ife tikupemphera, Mulungu Wokondedwa, kuti Inu muikechimenecho pa mitima yathu, kuti ife tisapange kulakwitsakulikonse. Wokondedwa Mulungu, musunge chikumbumtimachathu chikhale choyera. Musunge mitima yathu yophimbidwa,Ambuye, maso athu ophimbidwa kwa zinthu za mdziko, ndizinthu zachabe za mdziko, ulemerero wachabe wofuna kukhalachinachake chachikulu.

Page 32: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

32 MAWU OLANKHULIDWA

176 Ziribe kanthu kuti iwowo ndi aakulu bwanji, mafumu onse,atsogoleri, amphamvu, ndipo china chirichonsecho chiyenerakudzatha, ndipo iwo sadzaukamu-…mu chiukitsiro choyamba.Pakuti kunalembedwa, “Wodala ndi woyera ali iye amene ali ndigawo mu chiukitsiro choyamba, pa amene imfa yachiwiri ilibemphamvu.” O Mulungu! “Imfa yachiwiri,” imfa yauzimu, “ilibemphamvu”; iye ndi wowomboledwa!177 O Mulungu, tikaganiza kuti limodzi la maora awa,wina adzakhala akupita kukamchezera mzake, ndipoadzakakwatulidwako. “Awiri adzakhala pa bedi; ndimdzatengammodzi, ndi kumsiya winayo. Awiri adzakhala ali mmunda; Inendimdzatengammodzi, ndi kumsiya winayo.”178 O Mulungu, mutithandize ife kuti tikhale angwiro pa—pamaso pa Inu, Ambuye, ziribe kanthu kutimunthuyo akuganizachiyani za ife, zimene anthu ena akunena. Ambuye, mulolezoyera zathu…zolankhulana zathu zizikhala zoyera. Muloleizo zikhale zokhwimitsidwa ndi Mawu a Mulungu; zokhwimakwambiri, Ambuye, kuti pasapezeke ndulu iliyonse mwa ife.Pamene ife tikupempha, mu zolakwitsa zathu zomwe, kutiMagazi a Yesu Khristu adziima pakati pa ife ndi Mulungu,kuti Iye aziyang’ana pansi pa ife kudzera Magazi a Yesu;osati pa chirungamo chathu chomwe, kapena yemwe ife tiri,zomwe ife tachita, koma pa kuyenereza Kwake kokha. Mulungu,perekani izi!179 Musalole kuti mmodzi amene wakhala pano usikuuno ndipowamva Uthenga, musalole mmodzi wa iwo kuti akataike,kuchokera kwa mwana wamng’ono kukafika kwa munthuwachikulire. Mulole chokhumba chawo choyera chikangokhalapa Mulungu yekha ndi Mawu Ake. Ife sitikudziwa ora limeneIye angawonekere, kapena ora limene Iye angatiitanitse ife kutitidzakayankhe kumwamba uko pa Chiweruzo. Ife sitikudziwaora limene Iye angatero, monga zinaliri, kutenga chitupa chathukuchokera mu kabati, ndikuti, “Ndi nthawi yopita kwathu. Iweuyenera uzipita.” Mulungu, mutithandize ife kukhala angwiro.Perekani izi, Ambuye.180 Mulole ife tikhale moyo mpaka Kudza kwa Ambuye, ngatikutakhala kotheka. Mutilole ife tikachite chirichonse chimenechiri mu mphamvu zathu, ndi chikondi ndi kumvetsetsa,kumvetsetsa kuti Mulungu akufunafuna m’dzikoli, lero, kutiapeze nkhosa yosochera iliyonseyo. Ndipo ife titakalankhula ndiiwo ndi pemphero lokhwima la chikondi ndi Mawu a Mulungu,kuti ife tikakhoze kumupeza wotsirizayo, kuti tizipita Kwathu,ndi kuchokamomuEdeniwakale uyuwaSatana kuno, Ambuye.181 Amene yense wamangidwa pa chisiliro, ndi akazi okongola,monga mmene amadzitchulira mdzikoli, ndi zolengeza zawopamenepo, “Ife tikulengeza, ndipo tikufuna anyamata abwereatazipaka jamu pa nkhope zawo, ndi atsikana okongola atavala

Page 33: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 33

makabudula,” pa mawailesi athu kumene ndi matelevizioni;ndi mtundu wonse wa nyansi ndi uve, ndi Hollywood; mitunduyonse ya madiresi odolola, oyipa, onyansa a akazi. Ndipo—ndipoamuna akupotozedwa ndipo akutenga zovala zachikazi, ndikumadula tsitsi lawomonga akazi; ndipo akazi ali ngati amuna.182 OMulungu, ndi ora loipa bwanji limene ife tiri nkukhalamo!O, bwerani, Ambuye Yesu, bwerani! Bwerani, Ambuye!Dzatitsukeni ife ndi Magazi. Muchotsemo nyansi zonse ndindulu mwa ife. Mutilole ife tikhale ndi moyo, Ambuye, mutiloleife tizikhala moyo pansi pa Magazi, nthawizonse, pamaso Panu.Ndi chokhumba cha mitima yathu, ndiponso pempho lathuloona.183 Wokondedwa Mulungu, zaikidwa apa pa-…kapena izo,desiki, usikuuno, pamene Uthenga waikidwapo. Ambuye, apapaikidwa mipango ndi maphukusi pang’ono zimene zikupitakwa odwala ndi osautsika. Mulole pemphero la chikhulupiriro,Ambuye, ligwe kuchokera mmitima yathu tsopano, pamasoPanu. Ndiye, Ambuye, ngati pangakhale chinthu chosayerachirichonse mwa ife, Ambuye, mutenge zathu…mutitengereife wa ku chiweruzo tsopano; ndipo ife tikupempha chifundo.Muwulule kwa ife zimene ife tikulakwitsa, Ambuye, kuti ifetikathe kupempha, kuti titenge Magazi ndipo atiyeretse ife.Mukawachiritse anthu odwala awa ndipo mukawapange iwokukhala bwino bwino, Atate, kwa aliyense amene zikumupitira,kulikonse kumene zikupitako. Mulole izo zikakhale chomwecho,Ambuye.184 Mutipatse ife kulimbikira kokutumikirani Inu, ndipo Inunokha. Perekani izi, Ambuye.185 Mupereke chitetezero kwa anthu okondedwa awa amene alipa njira yopita kwawo.186 Zikomo Inu chifukwa cha mmene Inu mwawachiritsiraanthu. Ndi mnyamata wamng’ono wa Mlongo Shepherdndi M’bale Shepherd, amene anavulala pa njinga, inendikupemphera kuti pasakhale choipa chiti chibwere kwaiye; mwana wamng’onoyo amakwera njinga yake, inendikupemphera kuti akhale bwino bwino. Ife tikukuthokozaniInu chifukwa cha machiritso Anu pa ena awa omwe ifetawapemphera. “Ndipo ife tikudziwa kuti zimene ife tapempha,ife talandira, chifukwa ife tiri nacho chidaliro mwa Mmodziamene anapanga lonjezolo.”187 Tipatseni ife za chisomo Chanu, Ambuye, ndipomutikhululukire ife machimo athu, ife tikupempha mu Dzina laYesu Khristu. Ameni.188 Kodi inu mukunkonda Iye? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Kodi inu mukumukhulupirira Iye?[“Ameni.”] Kodi inu mwadwala nawo ndi kutopa nawo ufumuwa Satana? [“Ameni.”] Kodi inu mukukhulupirira kuti zikufika

Page 34: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

34 MAWU OLANKHULIDWA

ku Zakachikwi, ku Zakachikwi Zake; Zake, ku Edeni Wake?[“Ameni.”]189 Kodi inu mukukhulupirira kuti akupangidwa lero?Taonani, chirichonse chikukhazikika pa luntha. Zonse,chirichonse, chiyenera kutsimikiziridwa mwa sayansi iwoasanachikhulupirire icho.190 Ndipo inu simungamutsimikizire Mulungumwa sayansi. Inumuyenera kumuvomereza Iye mwa chikhulupiriro, “Pakuti iyeamene adza kwa Mulungu ayenera kukhulupirira kuti Iye ali,ndiponsowoperekamphotho kwa iwo amene amufunitsitsa Iye.”191 O Mulungu, ine sindikufuna kudziwa kalikonse komaMagazi a Yesu Khristu amene amandiyeretsa ine ku tchimo. Inesindikudziwa kanthu koma Yesu Khristu. Ndipo monga Paulowakale ananena, inenso ndikunena usikuuno, “Ine sindikudziwakanthu pakati panu, ndikungomutumikira Yesu Khristu, ndi Iyewopachikidwayo.”192 Ndi zokhazo zimene ine ndimadziwa kukuuzani inu. Kuti,Baibulo ili, ine ndimalikhulupirira ndi mtima wanga wonse(ngati ine ndikuwudziwa mtima wanga), kuti ndi Mawu aMulungu osaipitsidwa. Ndi Ili ine ndimakhala moyo. Ndi Iliine ndikuima. Ndipo ngati ine ndikadakhala ndi miyoyo tenisauzande, ine ndingakonde kupereka uliwonse wa iwo ku Mawuawa, pakuti iwo ndi Mawu a Yesu Khristu. Ndipo ine ndiribenazo ntchito kuti iwo ayesera kangati kuti awatsutse Iwo,ndi sayansi yochuluka bwanji ikuyesera kunena kuti Iwo ndiosadalirika, ndi zina zotero. Kwa ine, Iwo ali chinthu chokhachomu dziko chimene ine ndingathe kuchidalira, ndi Mawu awa. Iyendi wanga. Ine ndimamukonda Iye. Sichoncho inu? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi.]193 Ngati muli tchimomumtimamwanu, ngati muli cholakwikamu mtima mwanu, ngati inu muli ndi chirichonse, mupempheretsopano ndipo mumufunse Mulungu kuti akukhululukireniinu. Inu mundipempherere ine; ine ndizikupemphererani inu.Mulungu akudalitseni inu, ndiro pemphero langa.

Mpaka tidzakomane! mpaka tidzakomane!Mulungu akhale nanu mpakatidzakomanenso!

194 Kodi inu mumakondana wina ndi mzake? [Osonkhana akuti,“Ameni.”—Mkonzi.] Yohane anati, “Ana aang’ono, kondananiwina ndi mzake.” “Kondanani wina ndi mzake, pakuti chikondichimaphimba unyinji wamachimo.” Tsopano tiyeni ife tigwiranechanza wina ndi mzake.

Mulungu akhale nanu mpakatidzakomanenso!

Mpakana tidzakomane! mpakanatidzakomane!

Page 35: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 35

195 Tsopano muzikhala achifundo kwa wina ndi mzake.Muzikhala a chifundo kwa aliyense. Muzichita nayewoyandikana naye mwabwino. Mudzizisunga nokha opandabanga mpaka Yesu adzadze.

…mapazi;Mpakana tidzakomane! mpakanatidzakomane!

Mulungu akhale nanu mpakanatidzakomanenso!

196 Inumukunkonda Iye? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]Ndiro pemphero langa. Inu mundipempherere ine; inendizikupemphererani inu. Ine ndiyenera kuti ndibwerereku Tucson tsopano. Ndipo i—ine ndikupemphera kutiMulungu akudalitseni inu nonse. Ine ndikapita ku Canadandikamakachoka kumeneko, ndi kukabwereranso kuColorado; kuzungulira, kuzungulira, kuzungulira, mwawona.Mpakana…197 M’bale Tony ali kumeneko, ndipo chinthu chachikuluchachitika. Pansi pomwe pa Vatican, mu Roma, iwo akuitanitsachitsitsimutso, msonkhano, kuti ine ndipite kumenekondi kukachititsa chitsitsimutso mu Roma, mu Roma. Iyewangobwera kumene. Anthu onsewo ali pamodzi. Iwo alindi bwalo lalikulu kumeneko, lokhala anthu masauzandendi masauzande, ndipo iwo akufuna kuti ine ndipitekondikukakhala ndi chitsitsimutso. Iwo akufuna kuti akawoneulemerero wa Ambuye mu utumiki. Ine sindikudziwa. Inendiyenera kuti ndizipempherere izo, ndiwone zomwe Ambuyeati andiuze ine. O, mai! Mukumbukire, kutipempherera, tonse aife limodzi. Ife tikugwira ntchito…

Ife tikuwona kudza kwa Mpulumutsi wathuwodala,

Yang’anani, ndi kuwona masamba a mkuyutsopano akukhala obiriwira;

Uthenga wa Ufumu Wake wapita ku fukolirilonse;

Ndipo ife tayandikira mapeto, akukhozakuwoneka.

198 Kodi izo nzoona? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi.]Ndiye mokondwera ife tikalengeza Uthengawa kuwonekera Kwake kodala,

Posachedwa Iye akubwera mu ulemerero,tikamuwuze mmodzi ndi onse;

Ndiye galamukani, inu oyera a Ambuye,bwanji mukugona pamene mapetoakuyandikira,

Tiyeni tikhale okonzekera kuyitanakotsirizako.

Page 36: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

36 MAWU OLANKHULIDWA

199 Iwo udzatembenukira kumadzulo ndipo udzabwereranso,limodzi la masiku awa, ingokumbukirani. Iwo ndithudiudzatero. Ndipo izo nzoona. Mpakana pamenepo:

Tenga Dzina la Yesu ndi iwe,Mwana wosauka ndi watsoka;Lidzakusangalatsa ndi kukupatsa iwechitonthozo,

Tenga ilo, kulikonse upita.

Dzina lofunika (Dzina lofunika), O ndilokoma!

Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba;

Dzina lofunika, O ndi lokoma! (ndi lokoma!)Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba.

Pa Dzina la Yesu kugwada,Kugwa modzilambatitsa pa mapazi Ake,Mfumu ya mafumu Kumwamba tidzamuvekaIye korona,

Pamene ulendo wathu watha.

Dzina lofunika, O ndi lokoma!Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba;

Dzina lofunika, O ndi lokoma!Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba.

200 Tsopano, pa ndime yotsirizira iyi, tiyeni tiimbe iyo ndimitima yowerama tsopano.

Tenga Dzina la Yesu ndi iwe,Monga chishango ku msampha uliwonse;Ndipo pamene mayesero akuzinga iwe, (zinthuizi za ufumu wa Satana, mwaona, mwaona)

Udzangopuma Dzina loyeralo mu pemphero.

201 Ndizo zonse; ndiye nkuchokapo. Izo zimagwira ntchito.Ine ndaziyeserapo izo. Ingokhulupirirani izo tsopano, chifukwaizo zidzagwira ntchito. Kungopuma Dzina Lake loyera mupemphero.

…Dzina la Yesu ndi iwe,Monga chishango ku msampha uliwonse;Pamene mayesero akuzinga iwe, (Uchitachiyani ndiye pamenepo?)

Udzangopuma Dzina loyeralo mu pemphero.(Chophimbacho chidzabwera pa nkhopeyako.)

Page 37: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA 37

Dzina lofunika (Dzina lofunika), O ndilokoma!

Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba;

Dzina lofunika, O ndi lokoma!Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba.

202 Tiyeni tiweramitse mitu yathu tsopano, pamene inendikumupempha M’bale Beeler kumbuyo uko kuti abwere kunsanja. [M’bale Branham akuyamba kung’ung’uza Tenga DzinaLa Yesu Ndi Iwe—Mkonzi.]

Mudzangopuma Dzina Lake loyera mupemphero.

203 Inu mutibalalitse ife, M’bale Beeler. Inu mutibalalitse ife mupemphero.

Dzina lofunika,Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba;

Dzina lofunika, (Dzina lofunika), O ndilokoma!

Chiyembekezo cha dziko ndi chisangalalo chaKumwamba.

204 Tsopano ndi mitu yathu yoweramitsidwa, ndi mitima yathuyoweramitsidwa. M’bale Beeler, mmodzi wa othandizana nawopano, M’bale Estle Beeler, m’bale wabwino wa Chikhristu,munthu womvera. Ine ndimupempha iye ngati angabalalitsegululi, usikuuno, ndi pemphero. Mulungu akudalitseni inu,M’bale Beeler.

Page 38: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

EDENI WA SATANA CHA65-0829(Satan’s Eden)

Uthenga uwu wa M’bale William Marrion Branham, woperekedwa muChingerezi Lamlungu usiku, Ogasiti 29, 1965, ku Branham Tabernacle muJeffersonville, Indiana, U.S.A., unatengedwa kuchokera pa matepi ojambulidwandi maginito nudindidwa mosachotsera mawu ena mu Chingerezi. Kumasulirakwa Chichewa uku kunadindidwa ndi kugawidwa ndi Voice Of God Recordings.

CHICHEWA

©2015 VGR, ALL RIGHTS RESERVED

VOICE OF GOD RECORDINGS, MALAWI OFFICE

P.O. BOX 51453, LIMBE, MALAWI

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. BOX 950, JEFFERSONVILLE, INDIANA 47131 U.S.A.www.branham.org

Page 39: CHA65-0829 Edeni Wa Satana VGR - download.branham.orgdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA65-0829 Satans Eden VGR.pdf · 25 Anthu, mosadziwa akumupembedza Satana, kumaganiza kutiiwoakumupembedzaMulungu;mongaifetikuchenjezedwa

Chidziwitso kwa ofuna kusindikiza

Maufulu onse ndi osungidwa. Bukhu ili mukhoza ku printa kunyumba kwanu ngati mutafuna kuti mugwiritse ntchito inuyo kapena kuti mukawapatse ena, ulere, ngati chida chofalitsira Uthenga wa Yesu Khristu. Bukhu ili simungathe kuligulitsa, kulichulukitsa kuti akhalepo ambiri, kuikidwa pa intaneti, kukaliika pakuti ena azitengapo, kumasuliridwa mu zinenero zina, kapena kugwiritsidwa ntchito ngati njira yopezera ndalama popanda chilolezo chochita kulembedwa ndi a Voice Of God Recordings®.

Ngati mukufuna kuti mumve zambiri kapena ngati mukufuna zipangizo zina zimene tiri nazo, chonde mulembere ku:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org