48
Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville. Ndi pepani basi kuti ndakusungani inu mutaima, mmbali mw a makoma. Ndipo ine ndinadutsa kuno pa chochita china, pafupi ora ndi theka lapitalo, ndipo anthu anali akubwerera pa chitseko, akumapita kwao. Ine ndinakomana ndi Billy kunja uko, ndipo iye anati malo anali atakonzeka kale kuti msonkhano uyambike, kuchokera madzulo ano. Chotero, ife tinangokhala nawo msonkhano waung’ono uwu kuno. Ife sitinawuyike nkomwe iwo mu mapepala akuno. Kotero, ife tingokhala ndi kanthawi kakang’ono ka chiyanjano. 2 Ndipo tsopano ndi zotangwanitsa nthawizonse, monga anthu a kunja kwa mzinda mungadziwe, kuti, kuno ku malo akwathu nthawizonse ndimakhalira kulumpha, kuthamanga kuchokera ku malo kupita ku malo, ndi kupanikizika. Chotero, ine ndikukhala ngati ndikuzolowera izo. Ine ndangofika pa malo amene ine sindikulola kuti izo zizindisautsa ine, mochuluka monga zikanathekera. Ndipo inu mukudziwa, iwe uyenera kutaya pang’ono pokha nthawi, ndipo iyenera kukhala yochuluka, ndi Ambuye. Ngati iwe suchita izo, ndiye iwe sumabwera mu msonkhano ndi kutsitsimuka kwa Mzimu Woyera. Ndipo pamene iwe ubwera mkati, monga lero zakhalira, pamene izo zangokhala chimodzi chachikulu, chokopa chachikulu, chabwino, izo zimakhala ngati zovuta nthawizina kuti ine ndibwere mkati, kuti ndipewe kukhala wotsinidwa pang’ono pokha ndi kukankha, inu mukuona, ndi kudzipangitsa ndekha kukwiya. Pamene ine ndichita izo, ndiye ine sindingakhoze kuupeza Mzimu Woyera paliponse mu izo. 3 Chotero, ine ndikumvera chisoni, ngakhale, kwa anthu amene aimirira mu_mu timipita ndi kuzungulira panja. Ndipo iwo amabwera, kuyang’ana mkati, kukalowa mu galimoto yawo ndi kumabwerera kwawo. Ine ndimafuna kuti nditenge sukulu yapamwamba kumusi kuno, kuti ndidzachititse msonkhano wa mausiku angapo okha, koma sukulu ikupitirira nthawi ino, ndipo ziri ngati zovuta kwa ine kuti ndiitenge iyo mu nthawi imeneyo. Koma ine ndikufuna kunena kuti inu ndikuyamikira ndithudi mmodzi aliyense wa inu, mkati muno ndi kunja, ndi chifukwa cha mgwirizano wanu wabwino, ndi pa zonse zimene inu mwachita. 4 Ndipo mmawa uno, mu Sande sukulu, ine ndinawathokoza anthu chifukwa cha chopereka chimene chinaperekedwa kwa ine usiku wathawu, chimene chinali chopereka chosapemphedwa. Mosabisa, ine ndinawauza abusa kuno, abusa athu okondedwa, M’bale Neville, ndi iwo, ine

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

  • Upload
    vophuc

  • View
    288

  • Download
    17

Embed Size (px)

Citation preview

Page 1: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1

Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu

` ^Neville. Ndi pepani basi kuti ndakusungani inumutaima, mmbali mw a makoma. Ndipo ine

ndinadutsa kuno pa chochita china, pafupi ora ndi thekalapitalo, ndipo anthu anali akubwerera pa chitseko, akumapitakwao. Ine ndinakomana ndi Billy kunja uko, ndipo iye anatimalo anali atakonzeka kale kuti msonkhano uyambike,kuchokera madzulo ano. Chotero, ife tinangokhala nawomsonkhano waung’ono uwu kuno. Ife sitinawuyike nkomweiwo mu mapepala akuno. Kotero, ife tingokhala ndi kanthawikakang’ono ka chiyanjano.

2 Ndipo tsopano ndi zotangwanitsa nthawizonse, mongaanthu a kunja kwa mzinda mungadziwe, kuti, kuno ku maloakwathu nthawizonse ndimakhalira kulumpha, kuthamangakuchokera ku malo kupita ku malo, ndi kupanikizika.Chotero, ine ndikukhala ngati ndikuzolowera izo. Inendangofika pa malo amene ine sindikulola kuti izozizindisautsa ine, mochuluka monga zikanathekera. Ndipo inumukudziwa, iwe uyenera kutaya pang’ono pokha nthawi,ndipo iyenera kukhala yochuluka, ndi Ambuye. Ngati iwesuchita izo, ndiye iwe sumabwera mu msonkhano ndikutsitsimuka kwa Mzimu Woyera. Ndipo pamene iwe ubweramkati, monga lero zakhalira, pamene izo zangokhala chimodzichachikulu, chokopa chachikulu, chabwino, izo zimakhalangati zovuta nthawizina kuti ine ndibwere mkati, kutindipewe kukhala wotsinidwa pang’ono pokha ndi kukankha,inu mukuona, ndi kudzipangitsa ndekha kukwiya. Pamene inendichita izo, ndiye ine sindingakhoze kuupeza Mzimu Woyerapaliponse mu izo.

3 Chotero, ine ndikumvera chisoni, ngakhale, kwa anthuamene aimirira mu_mu timipita ndi kuzungulira panja. Ndipoiwo amabwera, kuyang’ana mkati, kukalowa mu galimotoyawo ndi kumabwerera kwawo. Ine ndimafuna kuti nditengesukulu yapamwamba kumusi kuno, kuti ndidzachititsemsonkhano wa mausiku angapo okha, koma sukulu ikupitiriranthawi ino, ndipo ziri ngati zovuta kwa ine kuti ndiitenge iyomu nthawi imeneyo. Koma ine ndikufuna kunena kuti inundikuyamikira ndithudi mmodzi aliyense wa inu, mkati munondi kunja, ndi chifukwa cha mgwirizano wanu wabwino, ndipa zonse zimene inu mwachita.

4 Ndipo mmawa uno, mu Sande sukulu, ine ndinawathokozaanthu chifukwa cha chopereka chimene chinaperekedwa kwaine usiku wathawu, chimene chinali choperekachosapemphedwa. Mosabisa, ine ndinawauza abusa kuno,abusa athu okondedwa, M’bale Neville, ndi iwo, ine

Page 2: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

2 MAWU OLANKHULIDWA

ndikanakonda ngati iwo akanati asachite izo. Koma iwoanachita izo, chonchobe, chotero ine ndimangofuna kutindinene pa izo. Tsopano, ano ndi malo aang’ono, ndipo iwosangati akhazike kupitirira pafupi anthu mazana atatu, inesindikuganiza. Ndipo choperekacho chinali madola mazanaatatu ndi makumi awiri mphambu anai, chimenechikutanthauza kuti inali pafupi dolla imodzi aliyense. Ndichopereka chopambana chimene ine ndinayambandapatsidwapo mu moyo wanga, pa chiwerengero cha anthu.Kawirikawiri, icho chimakhala pafupi masenti makumi awirindi anai pa munthu, makumi awiri ndi asanu. Masenti makumiawiri ndi asanu ndi awiri ndi chopereka chachikulu, kwamunthu. Koma ichi chinali pafupi dolla pa aliyense. Ndipo inendithudi ndiri kuyamikira izo.

5 Ndipo mwina ine sindinathe kutenga, mmawa uno, kutindifotokoze kwa ena a inu. Ife tinapeza zakudya, bokosi lazakudya ziri pa masitepe, ndi zopereka zazing’ono zomwezatumizidwa kwa ife. Mkazanga ndi ine tikukhumba kutitifotokoze kuthokoza kwathu kwa inu anthu. Ndipo inendikutsimikiza mwakupambana kumene ife tikudziwira, zonseizo zikhale kwa Ufumu wa Mulungu.

6 Ndipo izo zimandipangitsa ine kumangomverera ngatindikukhumba ine ndikanakhala nao malo aakulu kwambirikumene ife tikanakhoza kumangopitirira kupita mtsogolo kwanthawi yaitali ndi kutumikira kwa anthu. Koma ngakhaleusikuuno, ukatha msonkhano, ine ndikuyenera kumapita.Chimene, ine sindikhoza kuchoka usikuuno, koma mmawamolawirira, kuti ndizipita.

7 Ine ndidzabwerera Loweruka lotsatira usiku. KudzachokaLamlungu mmawa, kachiwiri, waku Colorado. Ziri basiumodzi pambuyo pa umzake womwe, kumapita.

8 Ndiyeno msonkhano wanga wotsatira waku tsidya lanyanja ukubwera mu Januwale, kumene kuli ku Australia ndiNew Zealand, ndi kudutsa uko. Tsopano, ine ndikufuna inukuti mundipempherere ine. Ine ndithudi ndikukhumbamapemphero anu.

9 Ndiyeno ine ndikufuna kuti^tonse ife kuti tikhaleoyamikira kwa Mulungu Wamphamvuzonse, Yemwewatichitira ife zinthu zazikulu choterezi mu msonkhanowaung’ono uwu. Ine ndikukhulupirira, kwa chiwerengero chanthawi, zakhala ziripo zochuluka zimene zakwaniritsidwa mumsonkhano uno kuposa msonkhano uliwonse umene inendinayamba ndachititsapo mu moyo wanga pa kachisi uyu.Ambuye akungowoneka kuti akutsegula madalitso.

10 Ine ndaganiza, mwina, pa msonkhano uno, kuti kuchokeramu masomphenya amene ine ndakhala nawo, kuti utumikiwanga ukuti usinthidwe ukhale wabwinoko ndi utumiki

Page 3: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 3

waukulupo. Tsopano izo zingochitika motsimikiza basi mongainu anthu munamva mautumiki ena atatu awaakunenedweratu, kapena ena awiri awa. Umodzi uwuudzakhala basi monga chomwecho, kungoti wokulirapo. Komausiku woyamba, ine ndinangowaitanira anthu kuno ku guwa,ndinapita molunjika basi ku kuzindikira zamumtima. Usikuwachiwiri, ine ndinawatengera iwo mu chipinda, ndinapitamolunjika basi ku kuzindikira zamumtima. Ndipo mausikuawiri otsiriza, ndiye, ife timawabweretsa iwo kuno pa nsanja,molunjika basi ku kuzindikira zamumtima.

11 Koma kungoti ndinenepo zinthu zina, mtumiki wakhunguanalandira kupenya kwake pa nsanja.

12 Ndipo asungwana awiri aang’ono, usiku watha, atakhalamu chikuku, ali ndi matenda amene palibe mmodzi yemweakudziwa chimene iwo ali, palibe dokotala. Mapazi awoaakulu patali, ndipo zala zawo zakuphazi zikugwa, zalazakumanja zikugwapo, ndipo palibe chimene chikanachitidwakwa iwo. Ndipo basi pamene Mzimu unali kudzoza, inendinapita apo, ndipo mu Dzina la Ambuye Yesu,ndinatemberera matenda amenewo, ndipo kunyamukakuchoka mu chikuku iwo anapita. Ndipo mmawa uno,amayenda kuzungulira kuno ku kachisi, monga mwana winaaliyense, ndipo anabwera kuno ndipo anadzabatizidwa ndiubatizo wa Chikhristu, pomwe pano mu dziwe, mmawa uno.

13 Pamene ine ndinali ndi maminiti angapo a kuwerenga,kanthawi kapitako, ndipo uko kunali abwenzi ena a ine,M’bale Hoover, mtumiki wochokera kumusi mu Kentucky,amangodutsa kuno ndipo anawasiyira mawu akazanga, kutiusiku watha pa kuyitana mzere, kunja mwa omvera, akaziamene anali opanda makadi aliwonse a pemphero kapenachirichonse, atangokhala panja uko akupemphera. Ndipo ukokunali mkazi mmodzi yemwe anali asanadye, ine ndayiwalakuti ndi motalika bwanji, chakudya; zophuka mu mimba yake,monse zitadzaza. Ndipo Ambuye anamuitana iye ndipoanamuchiza iye. Ndipo mmawa uno iye anawuka ndi kudyakadzutsa wamuyezo wabwino, ndipo ali pano penapakeusikuuno.

14 Ndipo ena, anali akunena zokhudza izo, ndipo, o, nthawisiikanati, itilole, pa zinthu zomwe Ambuye wathu wachita.Chotero, kwa ife, izo zikutipatsa ife kulimbika kudziwa kutiizo zangokhala pafupi, chinachake chikukonzekera kutichichitike, chachikulu.

15 Usiku watha, utatha msonkhano, utatha Uthenga, inesindinayambe pa nthawi iliyonse ndawuwonapo MzimuWoyera ukudzoza konse anthu mokula mulimonse kuposamomwe Iwo unachitira usiku watha. Ife tikuyembekezera kukwina, usikuuno. Ndipo tsopano mundipempherere ine.

Page 4: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

4 MAWU OLANKHULIDWA

16 Ndipo ine ndikufuna kuti ndiwerenge ena a Mawuodalitsidwa a Mulungu. Ndipo ife tisanawerenge Mawu, tiyenitingoyankhula kwa Iye, ndi mitu yathu yoweramitsidwamphindi chabe.

17 Okondedwa Atate Akumwamba, ife tikubwera kwa Inuusikuuno, mwina otopa pang’ono chabe mu thupi, koma, o,momwe mizimu yathu ili yofewera! Zizindikiro za Mulunguwamoyo, kuti Iye ali ndi ife, ndipo akutidalitsa ife, ndipoakutipatsa ife chija chimene Iye analonjeza, mopitirira,mochuluka, pamwamba pa zonse zimene ife tingakhozekuchita kapena kuganiza. Ndipo ngati ife tapeza chisomopamaso Panu, kupyolera pokhulupirira pa Mwana Wanu,Ambuye Yesu, ife tikanapempha usikuuno kuti Inumukanatichezera ife kachiwiri ndi magawo awiri a MzimuWanu. Mulole Iwo utsanuliridwe mu mphamvu yaikulu ndimiyezo pa munthu aliyense pano, kuti akhulupirire Uthengandi kulandira Mphamvu ya Mzimu Woyera mu miyoyo yawo.Pulumutsani iwo amene ali okhoza kupulumutsidwa usikuuno,Ambuye, ndipo achiritseni iwo amene ali okonzekeramachiritso. Perekani izi, Ambuye.

18 Ndipo pamene ife tikuwawona anthu akukanikizira mkati,ataimirira mu makomo, mazana akubwerera ku tchalitchichaching’onochi, izo zikutikumbutsa ife kuti Yesu Khristu aliyemweyo dzulo, lero, ndi kwa nthawizonse. Kuti, mu masikupamene Iye anatichezera ife kuno mu mawonekedwe a thupi,kukanikiza kunali kwakukulu kwambiri, iwo sankakhozankomwe kuti afike kwa Iye ndi munthu, ndipo anachitakumubweretsa iye kupyolera pa denga la nyumba. Ndipo ifetikupemphera, Mulungu, kuti usikuuno, kuti mmodzi aliyenseyemwe ati akanikizire kulowa mwa njira iyi adzakhozekulipiridwa monga munthu uja anachitira.

19 Dalitsani Mawu Anu pamene ife tikuwawerenga Iwo.Ndipo mulole Iwo akhale Nyali, Kuwala ku mapazi athu.Pakuti ife tikupempha izi mu Dzina la Yesu. Ameni.

20 [Wina akuyankhula ndi M’bale Branham_Mkonzi.] Ayi.Rosella Griffith? [“Inde.”]

21 Zangonenedwa kumene kwa ine pomwe pano kutimsungwana yemwe ine ndinamuitana mmawauja^chidakhwa yemwe anakhala ataitanidwa mumsonkhano ku Chicago. Iye anali yemwe anali atakhala muchipinda pamene Mzimu Woyera unayankhula kwa iye ndipoanati iye anali chidakhwa. Ndipo madokotala aakulu asanuaku Chicago anali atamulephera iye. Othandiza Zidakhwaanali atamulephera iye. Ndipo iye anaitanidwa, ndi PAKUTIATERO AMBUYE. Iye anachiritsidwa. Iye sanachite chibabakuti amwe kuyambira pa nthawi imeneyo.

Page 5: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 5

22 Ndipo dona wina wamng’ono uko mu khonde la pamwambapamtunda pa iye, yemwe anali mzake wa iye, omwe iwoankakhala mu Mzinda wa Calumet. Ngati aliyense akudziwakumene uko kuli, ndimo mmizere ya mmalire kumene kulikoyipa kuposa Paris, France, mitundu yonse ya zoipazikuchitikako. Ndipo ndinamuuza iye kuti iye anali wogulitsazozunguza ubongo, ndipo iye anali wovina ndi Fred Astaire.Ndipo bambo ake anayipidwa nazo izo. Koma iye anawukandipo anati, “Bambo, bamboyu akulondola ndendende.” Iyetsopano wakwatiwa, msungwana wamng’ono, ndipo ali pa njirayake, kumapita ndi mwamuna wake, akulalikira Uthenga.

23 Rosella ndi wogwira ntchito yautumwi, kuchokera kundende iliyonse kutumikira ndi chirichonse chimene iyeangakhoze kulowamo, kuwauza zidakhwa kuti chiripochiyembekezo, ndipo ndicho mwa Khristu.

24 Iye wakhala wolemedwa mochuluka kwambiri chifukwa chabambo ake; si kupitirira kuposa dzana, pa maminiti-khumi,kuyankhulana kwapadera. Msungwanayo wakhalawothandizira kwenikweni wa misonkhano, kwa zaka zinaikapena zisanu zapitazi. Zimene iye anandiuza ine, mukulongosola kwakung’ono kwa maminiti khumi, panja ku ngolo,pa zoyankhulana, kumene anati, “M’bale Branham, chirichonsechimene inu muchita, ndine wolemedwa moyipa chifukwa chabambo anga. Iwo amakukondani inu, koma iwo sakubwera basikwa Khristu.”

25 Ine ndinati, “Rosella, Mulungu akudziwa momwe angatiachitire izo. Iye akudziwa momwe angamupangire iye kuti achiteizo.”

26 Ndipo tamva kuti tsopano iye wakwiriridwa pansi pagalimoto itasenza miyala ya laimu. Tiyeni ife timupempherereiye.

27 Ambuye, pa kamwa ya mwana wamkazi wokhulupirika uja,ndipo iwo akodwa pansi uko, mwakuti akhoza kufa pansi apo;Mulungu, perekani kuti iwo asatero, koma moyo wao uyang’anemmwamba ndi kukumbukira kuti Inu ndinu Mulungu Yemwemukhoza kuyankha pemphero pansi pa mulu wa miyala yalaimu; mofanana monga Inu munakhoza kuchitira mu mimba yansomba, kapena mu ng’anjo ndi moto, kapena mu khola ndimikango. Inu mudakali yemweyo. Atulutseniko iwo, Ambuye,Mkhristu wotsukidwa. Ife tikudziwa kuti zinthu zonsezimachitira palimodzi kwa iwo amene akukondani Inu. Ndipo ifetikupemphera kuti ichi chikhale chimodzi cha zinthu zimenezo,pamene ife tikuzipereka izo kwa Inu, mu Dzina la Yesu. Ameni.

28 Mu kuwerenga kwa Mawu usikuuno, mu Bukhu la MafumuWachiwiri, ine ndikukhumba kuti ndiwerenge mu mutuwachiwiri, kwa mutu wapang’ono chabe, kuti ndipeze nkhaniyake, Mulungu akalola.

Page 6: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

6 MAWU OLANKHULIDWA

Ndipo zinafika pochitika, kuti pamene Yehova anatiamutengere mmwamba Eliya kupita kumwamba mukamvuluvulu, kuti Eliya anapita ndi Elisha kuchokeraku Giligala.

Ndipo Eliya anati kwa Elisha, Dikira iwe pano, inendikukupempha iwe; pakuti Yehova wandituma ineku Bet-eli. Ndipo Eliya anati kwa iye, monga AMBUYEalimoyo, ndi moyo wanu ulipo, ine sinditi ndikusiyeniinu. Chotero iwo anapita mpaka ku Bet-eli.

Ndipo ana a aneneri^anali kumeneko ku Bet-elianabwera uko kwa Elisha, ndipo anati kwa iye, Kodiiwe ukudziwa kuti Yehova akuchotsera mbuye wakopa utsogoleri wako lero? Ndipo iye anati, Inde, inendikudziwa izo; khalani^muli chete.

Ndipo Eliya anati kwa iye, Elisha, dikira pano, inendikukupempha iwe; pakuti Yehova wandituma ineku Yeriko. Ndipo iye anati, monga Yehova alimoyo,ndipo moyo wanu ulipo, ine sinditi ndikusiyeni inu.Chotero iwo anapita ku Yeriko.

Ndipo ana a mneneri^anali uko ku Yerikoanabwera kwa Elisha, ndipo anati kwa iye, Kodiukudziwa iwe kuti Yehova akuchotsera mbuye wakopa utsogoleri wako lero? Ndipo iye anayankha, Inde,ine ndikudziwa izo; khalani^muli chete.

Ndipo Eliya anati kwa iye, Dikira pano, inendikukupempha iwe, pakuti Yehova wandituma ineku Yordani. Ndipo iye anati, monga AMBUYE Alimoyo,^moyo wanu ulipo, ine sindikusiyani inu. Ndipo iwoawiri anapitirira.

29 Ambuye atawonjezera madalitso Awo ku Mawu Ake.Phunziro langa la usikuuno ndilo: Munthu Woitanidwa NdiMulungu.30 Ndipo ine ndiyesa kuti ndikhale mwachidule basi mongandingakhoze, chifukwa ife tiri ndi mzere wa pempherowaukulu umene ukubwera mu maminiti pang’ono chabe,koma, kungoti ndikupatseni inu kuyang’ana kwakung’ono panthawi zimene ife tiri kukhalamo. Ife tikumva kulira uku pawailesi, ndi mmalo osiyana, ndi kuchokera ku mitimayodzipereka, “Ambuye, tipatseni ife chitsitsimutso mu nthawiyathu.” Ndipo kuchokera pa makalata ochokera kwa Akhristukuzungulira dziko, ife tikumva kulira kumeneko, ndipo izozimachita chinachake kwa mtima wako. Izo ndi zodzoza. Izondi zokunyamula. Izo ndi zofulumizitsa, kwa moyo, kumvaanthu a Ambuye akuitanitsa chitsitsimutso. Ndipo Mulunguanapanga lonjezo, “Ngati anthu amene ali oitanidwa ndi DzinaLanga adzadzisonkhanitsa okha palimodzi ndi kupemphera,ndiye ine ndidzamva kuchokera Kumwamba.” Ndipo chotero

Page 7: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 7

ife, usikuuno, tikufuna kuti tiganize pa izo. Ndipokumbukirani, kuti, mkati mwa kulira konse uku, Mulungusangakhoze kutumiza chitsitsimutso mpaka Iye ali nawoamuna moyenera kuti achitenge icho. Ife sitingakhoze kukhalanacho chitsitsimutso mpaka ife titapeza amuna, amunaoyitanidwa ndi Mulungu, amuna ophunzitsidwa ndi Mulungu,omwe sali ophunzitsidwa mu sukulu za zamulungu ndi zamaphunziro, koma amuna opirira a chikhulupiriro, omweMulungu wawalera mu sukulu ya kuphunzitsa Kwake kovuta.Amuna amene sali owopa kuti akumane ndi moto! Amunaamene abwerapo mu Kukhalapo kwa Mulungu; ndipoakudziwa mphamvu Yake, ndipo akudziwa umphamvuzonseWake, ndipo akudziwa mphamvu Yake yochiritsa! Amuna enaamene aphunzitsidwa kuti amudziwe Mulungu wamoyo! Ndizabwino kuwaphunzitsa iwo mwa Mawu, koma, “Lembalimapha; Mzimu umapatsa Moyo.”

31 Ndipo ife tisanati tikhale nacho chitsitsimutso ichi,Mulungu ayenera kuti aitanepo ndi kuwaphunzitsa amuna,amuna ophunzitsidwa ndi Mulungu, kuti awutenge Uthengauwu. Ndipo iwo samasamala kuti kutsutsako ndi chiyani. Iwoamakhala ali ololera kuti apite ku ng’anjo ya moto mwakugonja, kapena ku makola a mikango, kapena kulikonsekumene kungakhale kuli. Iwo ali okonzeka kuti apite,chifukwa iwo akhala ali mu Kukhalapo kwa Mulungu, ndipoakudziwa chomwe Iye ali. Kaya ndi ku chigonjetso kapenakugonja, iwo amaima apobe chimodzimodzi. Ndiwo mtunduwa kaphunzitsidwe kamene Mulungu amachita kwa anthu.Ndipo ndi chachilendo kwambiri kuganiza kuti Mulunguakanakhoza kuchita izo, kuti Mulungu amaphunzitsa amunaAke monga choncho, koma Iye amatero. Inu mukudziwa, ifetiri nayo nyimbo yachikale imene timayimba:

Ena kupyola mmadzi, ena kupyolamnamondwe,

Ena kupyola mmayesero ozama, koma tonsekupyola mMwazi.

32 Mulungu amatsogolera anthu Ake kupyola mmayeseroaakulu, kuti awatsuke iwo. Ndipo nthawizina izo zimatengazaka kuti achite izo. Ndipo kwa inemwini, usikuuno, inendikukhulupirira kuti pakali pano Mulungu akuwaphunzitsaamuna oterowo kuti akakomane ndi mzere wapatsogolo,amuna amene akupyolamo, ndi, nthawi, kugwedezedwakuchokera ku mapazi awo. Nthawizina zimawoneka ngatichinthu chonsecho chikugwa, komabe, mkati mwa izo zonse,iwo amamudziwa Mulungu wamoyo uyo ndipo amaika nkhopezawo patsogolo, kukhala akumasunthabe.

33 Ndipo anthu ambiri akupempherera chitsitsimutso, inendikudabwa ngati ali nthawizina, ngati iwo amene

Page 8: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

8 MAWU OLANKHULIDWA

akupemphera, ngati mapemphero awo omwe samaimitsazitsime za madalitso. Pamene, ali mwamantha ndi owopa kutiamudalire Mulungu, owopa kuti amutenge Iye pa Mawu Ake,owopa kuti akhulupirire kuti Iye akadali wamoyo lero, pameneBaibulo Lake limanena mwachimvekere, kuti, “Iye aliyemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse.”

34 Mulungu samaitana, mwakamodzi, anthu anzeru,ophunzira, aluntha. Iwo amasewera gawo lawo, ndipo iwo ndianthu opambana. Koma kawirikawiri pamene Mulungu afunakuti ntchitoyo ichitidwe, Iye amatenga winawake yemwesadziwa nkomwe ABC wake. Fufuzani Malemba. Penyanikupyola mmbirizakale. Amuna amene anafika ku chinachakendi Mulungu sanali amuna omwe anali ndi maphunziroaakulu, koma amuna omwe, chabwino, anali opandamaphunziro, kukhumba kokha mu mtima mwawo kutiamutumikire Mulungu. Iye ankatenga mlimi, m’busa, nsodzi,msaki, iwo amene ankakhala mu chirengedwe. Mu kayeziyezindi kachetechete uja wa chirengedwe, uko Mulungu amakhozakuyankhula kwa iwo. Ndipo ndi omwe Iye ankawaitana.

35 Ndipo ngati iwo apeza kuti, pamene Iye akupereka kuitanakwa waluntha wamkulu, munthu ameneyo potsirizaamabwerera ku malingaliro ake aluntha. Ndipo pakapitakanthawi, pamene izo zifika pakuti achite chopambana, iyeamakhala ali wosokonezeka kwambiri ndi anthu a mdziko,kuti avomereze zoterozo. Chotero, iye amatsirizira kuchipembedzo, ndipo amapitirirabe kumbali ndi kukapangamtumiki. Ndipo izo zonse nzabwino, ndipo ine ndiribe kanthukotsutsa munthu ameneyo yemwe angati achite izo.

36 Koma pamene Mulungu akonzeka kuti achite chinachakemu malo auzimu, Iye kawirikawiri amatenga munthu yemweIye angakhoze kuika chidaliro Chake mmenemo, ndipoamamudzoza iye ndi kumutumiza iye kunja, ndipo iye ndiwopandamantha pa ntchitoyo. Ndiwo mtundu wa amunaamene ife tikuwasowa lero; osati masikolala opukutidwa,koma amuna amene amamudziwa Mulungu mu Mphamvu yachiwukitsiro Chake.

37 Mwa chitsanzo, panali mwamuna mu Baibulo, dzina lakeMose, yemwe anali ndi kuphunzitsidwa kwake konse. Iyeankadziwa zamulungu zonse. Iye ankadziwa chirichonsechimene iye ankayenera kuti achidziwe. Ngakhale iyeakanasowa maphunziro aliwonse, iye akanakhozakuwaphunzitsa olamulira mu Israeli, kapena mu Igupto. Iyesankasowa chinthu chimodzi. Ndipo Baibulo limatiuza ife kutiiye anali wophunzira mu nzeru zonse za Aigupto. Mwakuti, iyeankakhoza kuwaphunzitsa masikolala awo. Iye ankakhozakuwaphunzitsa azasayansi awo, zinthu. Iye anali ndimafungulo mpaka ku nsonga yomwe, pamene izo zifika kuzaluntha. Koma, apobe, izo zinamutengera Mulungu zaka

Page 9: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 9

makumi anai kuti apunthe zonse izo zichoke mwa iye, kunjauko mu michenga. Ndipo pamene iye anapeza malingaliro akeonse aluntha a Mulungu atapunthidwa kuwachotsa mwa iye,kunja kuja mu michenga, chitsulo chinali chokonzeka kutichiwumbidwenso.

38 Umo ndi momwe Mulungu amawatenga anthu Ake ndikupunthamo mantha awo onse ndi luntha lawo lonse, ndiyenoMbuye Wowumba wamkulu amawaika iwo pa gudumu ndipoamayamba kuwawumbanso iwo kachiwiri. Amuna antchito,oyenera! Ndiye munthu wa Mulungu. Ndani yemweangamuphunzitse munthu mochuluka kuposa MulunguMwiniwake? Penyani momwe Iye amawaphunzitsira iwo.

39 Ife tikanakhoza kulingalira kachiwiri za wina, dzina lakeDavide. Mulungu anali kumuphunzitsa Davide pamene iyeanali mnyamata wamng’ono chabe. Mneneri Samuelianabwera uko ndipo anatsanulira mafuta pa mutu wake, ndipoanamudzodza iye, chifukwa Mulungu ankafuna kutiamuphunzitse Davide kuti akhale wankhondo wamphamvu.Ndipo tayang’anani pa kuphunzitsa kumene Iye anamupatsaiye.

40 Ine ndinali kuwerenga, nthawiyina kale, kumtunda kunoku Chigayo cha a Green, kumene ine kawirikawiri ndimapitakukapemphera, kumene Mulungu ananena kwa Davide, “Inendinakutenga iwe kuchokera ku khola la nkhosa, kuchokerakotsatira nkhosa zapang’ono zija za atate ako kunja kuja,ndipo Ine ndinakupangira iwe dzina lalikulu ngati amunaaakulu a pa dziko.”

41 Ndipo ine ndikuganiza za kuphunzitsa kolimba kumeneIye anachita kwa Davide. Iye sanachite kumuphunzitsa iyemochuluka kwambiri mu sukulu ina, koma Iyeanamuphunzitsa iye mu sukulu Yake yomwe. Davide analimsaki ndi wolishya. Ndipo mu Masalmo iye analemba zamsipu wobiriwira ndi madzi odikha, chifukwa kumeneko iyeanali ali yekha, kwa iyeyekha. Iye sanali atakhathamitsidwandi zinthu za mdziko.

42 Mulungu ayenera kumuchotsa munthu ku zinthu zamdziko, kuti Iye akhoze kumufikitsa iye mwachete, kuti iyeazikhoza kumvetsera kwa Mulungu, ka Liwu ka kachetechetekaja, kakang’ono. Ndiye, kamodzi akakomana ndi Mulungu,iye amakhala wopanda mantha ndiye. Zindikirani kuti iyesamasamala chimene aliyense anena; iye wakhala ali muKukhalapo kwa Mulungu. Iye akumudziwa Mulungu muMphamvu ya chiwukitsiro Chake.

43 Ndiyeno, Davide, ife tikumuwona iye. Tsiku lina, Mulunguanaloleza chimbalangondo kuti chibwere ndi kudzatengaimodzi ya nkhosa zake. Davide anangopita motsatirachimbalangondo chimenecho. Mosakaika koma kuti iye

Page 10: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

10 MAWU OLANKHULIDWA

anapemphera, chifukwa kanthawi kenako iye anavomereza zaizo. Ndipo iye anapemphera ndipo anamupempha Mulungu.Iye anali wosamalira wa nkhosa imeneyo. Iye sakanakhozakuitaya nkhosa imeneyo. Ndipo iye ayenera kuti aipulumutsenkhosa imeneyo, mwa mtengo wonse. Ndipo iye anatengalegeni yake yaing’ono, ndipo anapita motsatirachimbalangondo chija ndipo anachipha icho. Iye ayenerakuipulumutsa nkhosa imeneyo. Inu mukuona chimeneMulungu anali kumuphunzitsira iye?

44 Mulungu akufuna kuti azibusa Ake azipulumutsa nkhosa,mosasamala chimene iye angati azitchedwa ndi zomwe iyeayenera kuti azidutsamo. Azipulumutsa nkhosa zimenezo!

45 Ndiye Iye anawona kuti Davide anali wolimba pachimbalangondo ichi, kotero Iye anangokweza mphamvu yachinyamacho mokulira pang’ono, ndipo Iye anatumizamwanawankhosa^mkango unabweramo ndipo unadzatengaimodzi ya anaankhosa.

46 Ndipo mkango ndi chinyama chopandamantha. O, muAfrika, pamene ine ndinali kusaka izo^Mkango ukhozakupha amuna khumi iwe usanati, “Jack Robinson.” O, chirombochamphamvu, chachikulu! Ndi kubangula kwakukulu kokhandi, basi, anthu amadyedwa. Ndipo iwo amene amafa pansi pamphamvu ya mkango samamverera kuwawa kulikonse. Ndichowopsya chotero, kuti umve kubangula kumeneko pameneiwo ukupereka. Mapazi aakulu amphamvu awo, mu mphindichabe, iye amagwetsera pansi amuna dazeni.

47 Ndipo kuti uganize, za mnyamata wamng’ono! Baibulolimati iye anali “khanda.” Izo zikutanthauza kuti iye analimunthu wamng’ono chabe, ndi kugenda kwakung’ono kwalegeni. Inu mukudziwa chimene icho chiri, kachidutswakakang’ono ka chikopa ndi chingwe ku mbali iliyonse. Ndipomkango wanjala, uli nako kale kulawa kwa magazi mkamwamwake, unathamangira umo ndipo anaimbwandira nkhosa.Davide anayang’ana mmwamba kwa Mulungu, ndipo anati,“Ine sindingakhoze kuitaya imeneyo. Inu mundithandize ine,Ambuye.” Ndipo iye anaugwetsera mkango pansi, ndi kugendakwa legeni. Ndipo pamene mkango unawuka momutsutsa iye,mnyamata wamng’ono ameneyo, ndipo mkango wolemerapafupi mapaundi mazana asanu, kapena bwinoko, mnyamatawamng’ono ameneyo akulemera mwina makumi asanu ndiawiri kapena makumi asanu ndi atatu. Iye anakoka, kuchokeraku lamba wake wamng’ono, mpeni. Ndipo pamene mkangounawuka, umene ukanapha amuna khumi mwa kukwapulakungapo, iye anawumbwandira mkango pa ndevu ndipoanawupha iwo.

48 Kulimbamtima! Mulungu samafuna amantha. Iyesangakhoze kukugwiritsa iwe ntchito ngati iwe ukuchita

Page 11: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 11

mantha kuti uwatenge Mawu Ake ndi kumukhulupirira Iye.Iye akufuna amuna olimba, osasamala chirichonse komachimene Ambuye anena. Ndiwo mtundu umene Iye akufunakuti aziyenda nawo. Mosasamala zimene mpingo unena,zimene m’busa anena, zimene mpingo uli kuimira; iyeamaimira Mulungu ndi chilungamo, ndi Mawu Ake. Ndiwoamuna ife^Mulungu awatumize masiku ano kwachitsitsimutso Chake chimene anthu Ake akuchipempherera.

49 Kenako mu zaka, pamene iye anapita kuti akakomane ndiabale ake ku nkhondo, uko kunali chimphona chinachachikulu kumtunda uko, zala mainchesi khumi ndi anai.Ndipo iye ankabwekerera, ndipo iye ankati, “Tsopano mloleniwina abwere adzamenyane ndi ine. Ngati inu mungakhozekundikwapula ine, ine ndigonjera; ndi inunso momwemo,ndipo ife tidzatumikira.” Yense yemwe ati agonjere, ndithudi,akhala iye yemwe ati agonje.

50 Ndi momwe Mdierekezi amakonda kuchitira izo. Pameneiye aganiza kuti iye wafika mmalire mwako, iye amakuuzaiwe, “Iwe sungakhoze kumapitirira nazo izo. Iwe sungakhozekulalikira machiritso Auzimu mu mpingo wa Methodisti,mpingo wa Baptisti.” Chabwino, inu alaliki a Methodistimudzangofika pomugwira Mulungu nthawi imodzi, ndipomudzapeze ngati inu mungakhoze kapena ayi. U-nhu. Inusimudzakhoza konse kuchita izo ndi zamulungu zanu zimeneiwo amaphunzitsa. Inu mudzasowa kuti mufike pomugwiraMulungu ndi kudziwa kuti Iye ali.

51 Iwo amati, “Anthu Achipentekoste.” Zaka zingapozapitazo, uko kunali gulu la anthu linkaima pa ngodya, opandankomwe_nyumba zimene iwo akanakhoza kulowamo. Komakodi inu munawerenga mu Life magazini, tsiku lina, zomweiwo ananena za iwo? Ndicho chimodzi cha zopambanazazikulu zomwe m’badwo uno unayamba wazidziwapo, ndichokuwuka kwa mpingo wa Chipentekoste. Zedi. “Ndipo iwoamapanga otembenuka ochuluka mu chaka chimodzi kuposamomwe mipingo ina yonseyo ingachitire, itayikidwapalimodzi.” Ndicho chimene Life magazini inanena. Bwanji?Iwo akhoza kukhala ali osokonezeka mu zinthu zina, koma,m’bale, iwo ndi olimbamtima; ataima kunja uko, chala-ku-chala, ndi kutcha chakuda “chakuda” ndi choyera “choyera.”Pamene potsitiriza chitsitsimutso chiti chisweke, ichochiswekera pakati pa iwo. Inu mupenye ndi kuwona ngati izosizitero. Iwo adzawongoledwa, limodzi la masiku awa.

52 Ndipo, Davide. Pamene Sauli anaika chida chake pa iye,ndipo anati, “Davide, ngati iwe uti upite kukamenyana nayemunthu uyu, chimphona^” Anati, “Bwanji, sindiwe kanthukoma mnyamata, mwana chabe, ndipo iye wakhala aliwankhondo kuyambira ali mwana. Iwe ungakhoze bwanjikumenyana naye iye?”

Page 12: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

12 MAWU OLANKHULIDWA

53 Tamvetserani kwa Davide wamng’ono uyu. Inu mukuona,iye sananene izi monga chonchi, “Sauli, wolemekezeka inu,bwana. Bambo anga ananditumiza ine ku sukulu ya galamala,koleji, sukulu yapamwamba. Ine ndiri ndi Ph.D. Ine_ine_inendiri nazo zida zoti ndichitire izi. Ndine munthu wophunzira.”Iye sananene konse izo monga choncho.

54 Iye anati, “Mbuye wanga,” iye anati, “pamene ine ndinalikuweta nkhosa za bambo anga kutsidya uko, chimbalangondochinabwera ndipo chinadzatenga imodzi, ndipo inendinachipha icho. Ndipo mkango unabwera ndipochinadzatenga imodzi, ndipo iye ndinaugwetsera iwo pansi.Ndipo pamene iwo unadzukapo, ine ndinawupha iwo.” Ndipoiye anati, “Mulungu yemwe anandipulumutsa ine ku dzanja lachimbalangondo ndi mkango, akhozanso kundipulumutsa ineku manja a Mfilisiti wosadulidwa uyo.” Munthuwophunzitsidwa ndi Mulungu!

55 Apo anaima Sauli ndi kuphunzira konse kumene munthualiyense angakhoze kukhala nako, kuti azidziwa momweangamenyere. Davide sankadziwa kanthu za lupanga. Iyesankadziwa kanthu za chishango. Ndiye, Sauli anapita ndipoanakaika chida chake chachikulu champhamvu pa iye, ndipoDavide wamng’ono anali ataima wamatewe pafupifupi. Iwoanapeza kuti chovala chake chachipembedzosichinamukwanire munthu wa Mulungu; zinangomugwetseraiye pansi. Ndipo tizikhulupiriro tathu tonse ndi zinthusizingafanane konse ndi chida cha Mulungu kutsidya.

56 O, momwe ife tingakhoze kumangopitirira pitirira, ndikunena zochuluka, za ochuluka ena osiyana. Koma, molunjikaku mutu wathu, kuti tifulumire.

57 Eliya anali kuyamba kukalamba, ndipo iye anadziwa kutiizo sizikanakhala ziri motalika kufika poti iye anayenera kutiachoke mdziko. Ndipo Mulungu anali atamupeza munthuyemwe anali munthu woonamtima, yemwe anali munthuwabwino. Dzina lake anali Elisha. Tsopano, ngati inu mutatimuzindikire, mmodzi wa iwo dzina lake ndi Eliya ndipommodzi winayo ndi Elisha.

58 Tsopano, iye sanapite konse mu maonekedwe, ndi zinazotero, ndi kupita ndi kukapeza mu sukulu za zamulungu, ndikupita ku sukulu zapamwamba zazikulu za masiku amenewo.Kodi iye anachita chiyani? Iye anapita kunja ku munda ndipoanakapeza munthu akulima ndi magori khumi ndi awiri ang’ombe. Chiyani? Elisha, yemwe anali akulima, ankadziwakuyamikira mzere woongoka. Ndipo iye ankadziwa kuti ngatiiye akanati atembenuke ndi kuyang’ana mmbuyo, iyeakanapotoza nasiya msewu. Ndipo Mulungu anadziwa kutimunthu yemwe amadziwa kulima mzere woongoka, amadziwakuti asaike manja ake pa khasu ngakhale kupotoloka kuti

Page 13: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 13

ayang’ane mmbuyo. Iye sanayembekezere mpaka iye atapezamaphunziro ake, napotoza popitirira mu njirayo. Iye anangophang’ombe ndipo anapanga nsembe, ndipo ananyamuka kupitandi Eliya, mwamsanga pamene chovala icho chinakhudza paiye. Iye anali wokonzeka, wololera. Mulungu ankadziwa kutiIye akanakhoza kumupangitsa iye kukhoza.

59 Tsopano, Mulungu ayenera kuti amupatse iye maphunziroena. Iye anakhala ali, kumuphunzitsa iye momwe akanatiaziyika maso ake pa mzere, ndi magoli khumi ndi awiri ang’ombe, ndi munthu mmodzi akulima ndi iwo. Iyeanamuphunzitsa iye kupirira kwina, ndi momwe angakhalirewopirira, ndi kuziphunzitsa ng’ombe zija kuti ziziyendamowongoka mu mzere.

60 Iye ankayenera kuti aphunzitse amuna ena, pambuyo pake;kuwayika iwo pa Baibulo, pa Mawu, atafola ndi Mulungu,kukhala moongoka mu mzere.

61 Ndipo, ndiye, ngakhale Mulungu anachita kumuphunzitsaiye pang’ono pokha. Iye anati, “Tsopano iwe udikire pano,pakuti ine ndikupita uko ku_ku Giligala. Ambuye andiyitanaine.”

62 Ndipo mneneri, atamverera kale Mphamvu imeneyo pa iye,mwinjiro uja wa Eliya, iye anati, “Monga Ambuye ali wamoyo,ndipo solo yanu ili yamoyo, ine sindikusiyani inu.”

63 Anapitirira mpaka ku Giligala, kumene kuli_malo akuvomereza kwa Chikhristu ndi ubatizo. Ndiyeno iye anati,“Ingotsala pano tsopano. Izi ndi zabwino mokwanira. Iwewapanga kuvomereza ndi ubatizo. Izi ndi zabwino mokwanira.Ine ndikupita mpaka ku Beteli,” kumene kumatanthauza,“nyumba ya Mulungu.”

64 Tsopano izo zikanakhala zabwino kwa odzinenera ambiri.“O, ine ndangobwera kumene mu mpingo ndipo ndiri ndichiyanjano. Bwanji osangokhala pomwe pano?”

65 Koma, mvetserani. Elisha sakanakhoza kuganiza mwanjiraimeneyo. Iye anali atamverera kale Mphamvu ya Mulungu. Iyeankadziwa zinalipo zina kwa iye. Kotero iye anati, “MongaAmbuye ali wamoyo, ndipo moyo wanu ulipo, inesindikusiyani inu.” O, momwe ine ndikuzikondera izo!

66 Ndipo iye anapita mpaka ku Beteli, ku nyumba yaMulungu, ndipo uko iye anakapeza gulu la masikolala. Iwoanali onse alaliki ophunzitsidwa bwino, ndipo iwo anayendapozungulira ndipo anamuuza iye, anati. “Bwana, kodi inumukudziwa chiyani? Inu muli pa mapeto aang’ono a ndodo.Kodi iwe umadziwa kuti Eliya amati atengedwe kwa iwe? Iyewakalamba kwambiri. Iye sangakhoze kukhala moyo motalikakwambiri. Eliya akuti atengedwe, ndipo iwe udzakhala utaimakunja uko monga wotentheka.”

Page 14: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

14 MAWU OLANKHULIDWA

67 Ndiroleni ine ndikuuzeni inu chinachake tsopano. Munthuyemwe anayamba wamulawapo Mulungu, sadzakhala aliwololera, kapena, sangakhoze kuthetsa ludzu lake pa chitsimechokumbidwa ndi munthu. Iye sangakhoze kuchita izo. Uko,zamulungu zawo zonse zimene iwo anali nazo uko ku sukuluya aneneri, sizikanakhoza kuthetsa ludzu la munthu waMulungu uyo, yemwe anali nako kulawa kwa Mulungu.

68 Ndipo iwo anapitirira kumukakamiza iye, “O, iwe uyenerakutsala pano. Ndipo, bwanji, mu masabata asanu ndi limodzi ifetikhoza kukupatsa iwe Ph.D yako. Ndipo iwe ukudziwa kuti izosizikhala ziri motalika kwambiri mpaka iwe utatenga pafupizaka zinai za kuphunzira kuno, ndipo ife tikhoza kukupatsa iweufulu woti uzilalikira. Iwe ukudziwa, ngati iwe usonyeza kutiukuchita bwino, ife tikanadzakutumiza iwe mu chipembedzochathu.” Izo sizingakhoze kumukhutitsa munthu wa Mulungu.“Ife tikuphunzitsa iwe kuti ukhale mtumiki, ngati iwe utiungokhala ndi ife pafupi zaka zinai kapena zisanu kuno.”

69 Iye analibe nthawi ya zinthu za mtundu umenewo. Iyeanali pa ulendo wake ku Kasupe uja. Iye anali atabwerapamwamba pa izo. Iye anali atalawa kale za Kumwamba musolo yake.

70 Ndipo iye anati, “Kodi iwe ukudziwa kuti mtsogoleri wakoakuti achotsedwepo?”

71 Ndipo mvetserani ku zimene iye ananena. “Inde, inendikudziwa izo. Koma khala bata lako.” Mwa kuyankhulakwina, “Sungani mpweya wanu. Musati muyesere kundiuzaine za izo. Musati muyesere kundiuza ine zomwe inendikuchita. Ine ndikudziwa kumene ine ndikupita ndi chimeneine ndikutsatira.” [M’bale Branham akuwombetsa manja akekatatu_Mkonzi.]

72 Mulungu, tipatseni ife amuna onga amenewo, amunaophunzitsidwa ndi Mulungu amene sadziwa za kupotokerakumbali ku izi ndi kupotokera kumbali ku izo.73 “Ine ndikudziwa kumene ine ndikupita. Ndipo musatimuyankhule kwa ine za izo. Ingosungani mpweya wanu.Musati muyesere kundikhumudwitsa ine, chifukwa izo sizitizichite ubwino uliwonse.”

74 O, ngati anthu amene apemphereredwa akanati angokhalandi kulimbamtima kochuluka chotero!

75 “O, masiku a zozizwitsa anapita. Izo sizinali zenizeni. Inumupenye, inu mukhala odwala kachiwiri.”

76 “Ingosungani mpweya wanu. Musati mundiuze inekalikonse ka izo. Ine ndikusuntha mopitirira. Chitsitsimutsochiri kudza. Mulungu wachilonjeza icho.” O, inu ana aamuna aMulungu, sunthirani kunja mu danga ilo kutali, opandamantha.Opandamantha! Mtengeni Mulungu pa Mawu Ake.

Page 15: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 15

77 “Ine ndikudziwa iye_iye akuti akatengedwe achokepo.Koma izo siziri zimene ine^Inu mulibe chinthu pano chotichingandisangalatse ine. Madigirii anu onse ndi ma Ph.D, ndiBachala ya Luso, ndi zinthu zonse izi, siziri kundikhutitsa ine.Ingosungani mpweya wanu.”

“Chabwino, inu mukasweka kunja uko.”

78 “Chabwino, ngati ine nditi ndisweke, ndisiyeni inendisweke. Ine ndiri pa ulendo wanga.” Ulendo, iye analiakupita.

“Inu simungakhoze kuzipangitsa izo kuoloka.”

79 “Ine ndikudziwa ine sindingakhoze kuzipangitsa izokuoloka, koma Mulungu akandiwolotsa ine,” iye anatero.

“Chabwino, Elisha akupita ku Yordani.”

“Ine ndikupita ndi iye.”

Mulungu akufuna Yordani mu moyo uliwonse.

80 Kotero, Elisha anabwera pamenepo. Anati, “Tsopano,Elisha^” Eliya ananena kwa Elisha, “Ndiwe munthuwamng’ono chabe,” mwinamwake chinachake monga ichi,“ndipo kwenikweni inu simunakhale nako kuphunzirakulikonse.” Mneneri wachikulireyo anali kuyesera kutiamuyese iye. Iye anati, “Ndiwe mwamuna wamng’ono chabe.Iwe sunakhale nako kuphunzira kokwanira. Bwanji, inusimuli^Ndi, kwenikweni, iwe sunakhale nawo maphunziro asukulu ya galamala. Chinthu chokha chimene iwe umachidziwandi momwe ungalimire. Chotero iwe kuli bwino utsalire pano,ndipo ukhoza kupeza Bachala ya Luso yako. Mukuona? Iwendibwino utsalire kuti upeze digirii yako.”

81 Koma osati Elisha, osati munthu uja yemweanamukhudzapo Mulungu kamodzi, anamverera Mphamvu ijaya kudzoza pa iye. Iye anati, “Monga Ambuye ali moyo, ndimoyo wanu usanafe konse, ine sinditi ndikusiyeni inu.” Iyeanali ndi cholinga. Iye anawona masomphenya. Iye ankadziwazimene zimati zikachitike.

82 Ndipo iwo onse anapita mpaka ku Yordani. Yordaniamatanthauza “imfa.” Uko iwo anaima, mwamuna wokalambandi mnyamata. Izo kwenikweni zikuimira Khristu ndi MpingoWake. Ndipo apo iwo anaima, mphepete mwa Yordani. Uko iyeali, akutsika kuchokera ku mapiri a Yudea, mafunde aakuluakukukuma monga choncho. Ndipo Elisha^ndi tsitsi lakelaimvi logwera pansi kunsana kwake, ndi maso ake osawonabwino okalamba akuyang’ana kutsidya kwa Yordani. Ndipomwamuna wamng’onoyo akupenyetsetsa kusuntha kulikonsekumene iye ankapanga. Mmodzi, mwamuna wamng’onoyo,anali akuyembekezera masomphenya, kuti achite chifuniro chaMulungu. Mmodzi winayo anali akupita Kwawo. Iwo onsewoanali pa Yordani. Elisha, kwa iye^Iye akupita Kwawo.

Page 16: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

16 MAWU OLANKHULIDWA

83 Eliya anakhala moyo wovuta. Mlaliki wamkazi uja kumusikuja anali atamupatsa iye nthawi yovuta yoti ayendemo,Yezebeli ndi Ahabu. Ndi miyala ndi zonse zimene iyeanadutsamo! Elisha anali kuyamba kutopa. Ndipo iyeankadziwa kuti iye anali atamenya nkhondo yabwino, ndipoiye anali atatsiriza mtundawo. Patsidya pa Yordani pokhaponkomwe kunali kupuma ntchito kwake.

Koma Elisha anali akuyembekezera Mzimu uwo umeneunali pa iye.

84 Kotero, ngati inu mutazindikira, wokhulupirira aliyense,pamene iwe ufika pa malo pamene iwe uyenera kuti ugulitsezonse, iwe udzamverera mafunde ozizira a Yordani akukuta pamapazi ako. Kodi iwe uwoloka, kapena sutero? Yordani ndi“kulekanitsa,” kulekana.

85 Ndipo ataima mmbuyo pa phiri anali alaliki awa, apobe,akukuwa pa Elisha, “Iwe kunali bwino kuti usawoloke. Iweupitirira malire.” Inu mumazimva izo, ndemanga, ngakhale,lero.

86 Koma, Elisha anati, “Ngati Mulungu ali Mulungu, ndipouyo ndi mneneri Wake, ine ndiyenera kuti nditenge malo ake.Ndipo ine ndikusowa Mzimu Wake kuti ndichitire izo nawo.Ine sindikusowa sukulu yawo. Ngati sukulu yawo ikanakhalaitachita izo, iwo akanakhala akutenga malo ake. KomaMulungu anandiitana ine kuti ndizichite izo, ndipo inendikusowa Mzimu Wake.”

87 Ngati masukulu a mipingo akanati atenge malowo, ndiMphamvu imene Yesu anapereka, iwo akanazitenga izo, zakazapitazo; Methodisti, Baptisti, Katolika, Presbateria. Koma iyosidzachita konse izo.

88 Zimatengera Mzimu wa Yesu Khristu! Ndipo inumudzawoloka Yordani, ya chipembedzo chirichonse kuserikwa icho, china chirichonse, ndi kuima wekha ndi Mulungu.

89 Chotero, Iye anaima ndi iye pa Yordani. Elishaakuyang’ana mmwamba uko, akudziwa, kwinakwake kutsidyauko, Mulungu akanati akakomane naye iye. Ndipo iyeanauvula mwinjiro wake, ndipo iye anayang’ana mozungulirakwa mwamuna wamng’onoyo. Ndipo iye anakantha Yordani.Ndipo pamene iye anatero, Yordani anatseguka. Ndipo iwoanayenda mowoloka, pa nthaka yowuma.

90 Mukuona, Yordani sali woyipa kwambiri, pambuyo pazonse, ngati iwe uli nacho Chinachake limodzi nawe chotiutsegulire njira.

91 O, pamene iwo anakagunda mbali inayo! Atakolowekedwaku thengo lirilonse anali kavalo ndi galeta. Mfumu ya mafumuanali atatumiza operekeza kuti amubweretse Eliya Kwawo. Izozonse zinali zitatha, kwa Eliya. Iye anali atakhala nazo

Page 17: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 17

zomkwanira za izo, pafupi zaka makumi asanu ndi atatu ndichinachake, za kukangana ndi anthu awo kumeneko, ndikumakhala ali^kudutsa mu njala ndi zokangana, ndichinthu chirichonse. Iye anali wokonzeka kuti azipita Kwawo.Ndipo iye anayang’ana pamenepo kwa Elisha.

92 Ndipo Elisha ankafuna kuti awone masomphenya. O, iyeanali ndi kuphunzira konse, kumbuyo kuja iye akanakhozakuimako. Iwo sanali kufika kulikonse. Mulungu ankatiamuphunzitse iye mwa njira Yake yomwe. Chotero pamene iyeanayang’ana cha kumeneko, anayang’ana, konse_mathengoonse awo uko, atakolowekedwa pa magaleta awa a Moto ndiakavalo a Moto, izo zinachita chinachake kwa Elisha. Iyeanawona masomphenya. Inde, m’bale!

93 Ndipo pamene Mulungu anamutengera Eliya mmwamba,iye anabwerera ndi magawo awiri a Mzimu wake. Iye analiwokonzekera chitsitsimutso pamenepo.

94 Zindikirani mwamunayo ndiye, pokhala mnyamata wolimachabe poyamba. Mulungu anapanga dzina lake kukhalalachisavundi. Aneneri onse amene anaima pozungulira,akumuyang’ana iye, anachita kugwada pa mapazi akechifukwa iye anali nayo Mphamvu ya Mulungu pa iye. [M’baleBranham agogoda pa guwa katatu_Mkonzi.]

95 Liri kudza ora pamene Mulungu ati adzapange dzikokugwada pa mapazi a amuna ndi aakazi amene agweramonadutsa ndipo awoloka Yordani, ndipo alekanitsa chinthuicho^okha, kuchoka ku zinthu za mdziko. M’bale ndimlongo, usikuuno, chirichonse chimene muchita, chirichonsechimene mukuganiza, inu muwoloke Yordani ndi Mulungu.Pitirirani kuoloka ndipo mudzilekanitse, lisiyeni dzikommbuyo. Muloleni Mulungu akuphunzitseni inu kwa utumikiWake womwe. Ife tiri kukhala mu tsiku chisanafikechitsitsimutso chimenechi, koma Mulungu akufufuza, kuyeserakuti apeze mitima.

96 Penyani. Iye anamupeza mwamuna dzina lake Paulo, o,Mfarisi wochita zayekha. Koma Iye anachita kumugwiritsa iyentchito, ngati, iye asanafike pokhala wophunzira. Penyanizimene Iye anachita, monse kupyola mibadwo, kwa anthu. Iyeankachita kuwatenga iwo ndi kupopera panja zamulunguzawo kuzichotsa mwa iwo. Ndipo Paulo, mwamsanga pameneiye anawona masomphenya, iye sanapite uko ku Yerusalemu,kwa Gamalieli, mphunzitsi wamkulu, wamkulu kwambiri muIsraeli, yemwe iye anaphunzitsidwa naye. Iye sanabwererekonse mmbuyo kwa iye, kuti akamufunse iye. Bwanji, iyesanapite nkomwe ku Yerusalemu, kwa zaka khumi ndi zinaizotsatira. Koma iye anapita uko ku Igupto, ku msonkhanowapemphero. Uko Mulungu anamulola iye kulemba Mabukuochuluka a Chipangano Chatsopano. Mukuona? Mulungu

Page 18: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

18 MAWU OLANKHULIDWA

akufuna amuna. Iye anali naye winawake yemwe Iye ankafunakuti alembe Chipangano chimenecho, kotero Iyeanangomusankha Paulo. Ndipo Iye anangomuchotserazamulungu zake zonse mwa iye. Ndipo Paulo anati iyeanachita kuyiwala zonse zimene iye anayamba wazidziwapo,kuti aphunzire Khristu.

97 Mulungu lero akuyesera kuti akhuthule dziko lichoke mwaife, ndi kutitenga ife kuti tidzikhuthule tokha, ndi kukhalaamuna ndi akazi opandamantha amene amamukondaMulungu, ndipo akhala ndi Mulungu, ndipo awoloka mzerewolekanitsa, Yordani, kuti Iye angakhoze kutigwiritsa ifentchito kwa ulemerero Wake.

98 Ili ndi ora limene ine ndikufuna inu kuti muganizemolimba. Ndipo ngati inu simunayambe mwawoloka konsemalo awa, ngati inu simunayambe mwafika powoloka mzereuwu, kumene inu mukanali kumati, “Chabwino, mayi angaanali a mpingo winawake.” Izo zonse nzabwino. Izosizimatenga malo anu. Mwaona?

99 Mulungu akuitanira amuna ndi akazi, lero, kutsogolo kwankhondo. Iye sikuti akuwaitanira iwo ku Giligala, ngakhalekuti Iye akuwaitanira iwo ku Yeriko, kapena Beteli. Iyeali^Awo adzawonongeka. Koma Iye akuwaitanira iwo kutiawoloke Yordani, kotero Iye angakhoze kukutengerani inu kusukulu ya Mphamvu Zake Zomwe, ndi kukupangani inu ndikukuwumbani inu.

100 Penyani zimene Iye akuchita komwe kuno tsopano,akutumiza pansi Mzimu wa Mwana Wake. Iye akuchitazizindikiro ndi zodabwitsa ndi zozizwitsa, zimene dzikosilinaziwone zaka zikwi ziwiri zapitazi. Dziko lasayansi lagwirachithunzi Chake, Lawi la Moto, Mngelo wa Ambuye.Lapachikidwa mu Washington, D.C., usikuuno, cha mu holo yaluso lachipembedzo, Chinthu chauzimu chokha chimenechinayamba chatsimikiziridwirapo mwasayansi kuti chinalichitajambulidwa. Iye akuyika apo zizindikiro Zake zomwezondi zodabwitsa.

101 Ndi chiyani icho? Ndiko kuwoloka Yordani. Kukhalawekha ndi Mulungu. Kugona mu ng’anjo Yake Yomweyokonzedweramo. Kukhala pa gudumu lalikulu la Wowumbandi kumulola Iye akuwumbe iwe. Usikuuno, pamene ife tiri mupemphero, pamene ife tikufika ku malo amenewo, dzigonekeninokha pa gudumu Lake lomwe, ndi kuti, “Ambuye, ine ndiripano. Ndiumbeni ine ndipo mundipange ine monga mwamapangidwe Anu Omwe.” Ndipo Mulungu azichita izo.

102 Pamene, ife tikuweramitsa mitu yathu mphindi chabe kwamawu a pemphero. Tisanati tipereke pemphero, ine ndikanafunakuti ndifunse funso ili kwa anthu mkatimu ndi kunja. Ndi angatimkati muno moonamtima akanafuna kuti apite ndi Yesu mpaka

Page 19: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 19

ku Yordani, usikuuno, ndipo uko kukawoloka uko kumene inumungakakhoze kuwona masomphenya ndi kukawona chimeneMulungu amatanthauza kwenikweni? Mungakweze manja anu?Mulungu akudalitseni inu. Tangoonani! Ine ndikungoganizakuti alipo manja mazana awiri mnyumba muno, akwezedwa.Pitani mpaka ku Yordani, osati mpaka ku seminare. Elishaanadutsa kumene cha pamenepo.

Iwo anati, “Dikira pano.”

103 Iye anati, “Ine sindikufuna kutero. Izo ndi zopangidwa ndianthu.” Aa, izo sizidzakhoza kuthetsa nkomwe ludzu ilo lamunthu yemwe akuchitira ludzu kwa Mulungu. Wopandakujayira kwa ku seminare, wopanda_wopanda luso lamadigirii, kapena zina zotero, sizidzakhoza, konse kuthetsaludzu ilo, mpaka inu mutamwa kuchokera ku Kasupe wa Moyouyo.

Inu amene munakweza manja anu, pempherani ndi inetsopano.

104 Mulungu wokondedwa, mu maminiti pang’ono awa autumiki, amuna ndi akazi ayima kuzungulira makoma,anyamata ndi asungwana; ndi panjapo, atatsamira pamazenera; kotentha. Komabe pali chinachake mwa iwo,chimene Inu mwagwira tcheru chawo, kapena iwo akanachokankumapita. Iwo sakanati ayime pamenepo monga choncho.

105 Koma, Ambuye Mulungu, chifukwa iwo akudziwa kuti iwondi anthu okhalapo chabe. Ndipo ife tinawerenga mu pepalakumene mmodzi wa mameya athu akale olemekezekaamamvetsera kwa Purezidenti-Wachiwiri akuyankhula,anatengedwa napita. Wina ku masewera a mpira, usiku wina,mwamuna wodziwika, anapita mwamsanga. Ndipo miyoyoyawo ili kwinakwake usikuuno. Mulungu, imeneyo idzakhalanjira yathu tsiku lina. Mwinamwake osati mwa chikhalidwechofanana, koma ife tiyenera kupita.

106 Ndipo lolani amuna abwere kwa iwoeni ndipo azindikirekuti kungokhala wa mpingo si zimene Inu mumafuna. Inumukufuna anthu kuti akhale odzazidwa ndi Mzimu, obadwa,otemedwa nkuchotsedwapo, owotchedwa mkati ndi MzimuWoyera, odindidwa, anthu amene awoloka mzere, anthuoitanidwa ndi Mulungu. Ndipo ife tikukhulupirira kuti Inumutumiza chitsitsimutso chimene Billy Graham ndi ena ambiriali kuchipempherera. Pamene Inu mungakhoze kuwatengeraanthu kwa iwowokha, kuchoka ku sukulu zawo za zamulungu,kuchoka ku njira za-kachitidwe kawokawo, anthu opandamantha, anthu a_a khalidwe ndi Inu, ameneamakukhulupirirani Inu ndipo amakutengani Inu pa MawuAnu.

107 Mulungu, mulole ambiri a iwo ayime alipo tsopano, ameneati apereke zonse zimene iwo ali nazo kwa Ambuye Yesu, ndi

Page 20: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

20 MAWU OLANKHULIDWA

kudzigulitsa mochoka ku dziko, kupita kupitirira Giligala,malo a kuvomereza ndi kuyamba kwa Chikhristu. Apitekudutsa sukulu ya aneneri imene inali kumbuyo kuja ndizamulungu zawo. Apitirira mpaka ku Yordani, kumasomphenya otseguka pamene iwo anawoloka, akapeze kutiMulungu wamoyo akanali wamoyo.

108 Kenako ife tikumupeza mneneri uyu akuyang’ana ponsepomzungulira iye, ndipo apo panali Angelo omwewa a Moto,ndi magaleta, ku Dothani kuja, tsiku lina.

109 Iwo akadali pano usikuuno, Ambuye. Itanani amuna Anu,itanani Akazi anu, anyamata Anu, asungwana Anu, Ambuye.Yankhulani mtendere kwa mitima yawo ndipo aloleni iwo kutiawolokere kwina kutali ndi zinthu za mdziko. Pakuti ifetikupempha izi mu Dzina la Yesu ndi chifukwa cha Iye. Ameni.

110 Ine ndikufuna kuti ndiyimbe ijayi mphindi chabe,mwachete kwenikweni mwa kupembedza.

Khalani ndi njira Yanu, Ambuye!Khalani ndi njira Yanu!Gwirani chomwe ndiriMnjira ya mtheradi!Ndiumbeni ndipangeniMwa kufuna Kwanu,Pamene ndiyembekeza,Wodzipereka mwa chete.

Tonse palimodzi tsopano, mwa njira ya kupembedza.

Khalani ndi njira Yanu,

Tsopano dziperekeni nokha ku nyimbo imeneyo, ndinyimbo imeneyo, kwa Mulungu.

Khalani ndi njira Yanu!Gwirani chomwe ndiriMnjira ya mtheradi!Ndiumbeni ndipangeniMwa kufuna Kwanu,Pamene ndiyembekeza,Wodzipereka mwa chete.

111 Mwachete tsopano, mwa kupembedza tsopano. Musatimuziyang’ana pozungulira. Ingoyang’anani kwa Mulungu.

Khalani ndi njira Yanu, (Tanthauzani izokwenikweni.)

Khalani ndi njira Yanu!Ndinu Wowumba;Ndine dongo.Ndiumbeni ndipangeniMwa kufuna Kwanu,Pamene ndiyembekeza,Wodzipereka mwa chete.

Page 21: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 21

112 Ine ndikukhulupirira kuti izo zikanakhala zabwinokwenikweni. Inu mumakukonda kupembedza? [Osonkhana ati,“Ameni.”_Mkonzi.] Uthenga watha tsopano. Tiyenitizingopembedza, miniti, ndi mitu yathu itaweramitsidwa,nyimbo iyo kachiwiri. Tanthauzani izo kuchokera mu mtimawanu.

Khalani ndi Yanu^Khalani ndi njira Yanu!Ndinu Wowumba;Ndine dongo,Ndiumbeni ndipangeniMwa kufuna Kwanu,Pamene ndiyembekeza,Wodzipereka mwa chete.

113 Ambuye, perekani izi. Mulole mmodzi aliyense, kuchokerapa ana aang’ono awa mpaka kwa mwamuna wamkulu kwambirindi mkazi mu Kukhalapo Kwauzimu, mulole Mzimu Woyerapakali pano ugwire ntchito pa chikhulupiriro chawo ndipouchotsepo kukaikira kwawo konse, kulephera kwawo konsekwakung’ono, ndipo mulole iwo kuti awumbidwe monga mwachifuniro Chanu. Pamene iwo ali pa gudumu Lanu lalikulu lakuwumbira, ife tikugoneka miyoyo yathu kuti idalitsidwe,iwumbidwenso. Perekani izo, O Mulungu, mu Dzina la Yesu,Mwana Wanu. Ameni.

114 Ine ndikungozikonda izi. Sichoncho inu? [Osonkhana ati,“Ameni.”_Mkonzi.] Mwachete kokha kumamverera MzimuWoyera. O, utatha Uthenga wolimba, ndiyeno kukoma kujakwa Mzimu Woyera! Iwo umabwera ndi Mawu. Ine ndikutindiyimbe ndime ya iyo, kapena kuiyesa iyo.

Ukuwukha magazi, inde, ukuwukha magazi,Uthenga wa Mzimu Woyera, ukuwukha

magazi,Magazi a ophunzira ofera Choonadi,Uthenga wa Mzimu Woyera Ulikuwukha

magazi.

Woyamba kufera dongosolo la MzimuWoyera,

Anali Yohane M’batizi, anafa monga munthu;Ndiye anadza Ambuye Yesu, anampachika

Iye,Analalikira kuti Mzimu udzapulumutsa anthu.

Kunali Petro ndi Paulo, ndi Yohanewaumulungu,

Anapereka miyoyo kuti Uthenga uwu uwale;Anasakaniza magazi, monga aneneri akale,Kuti Mawu owona a Mulungu anenedwe

moona.

Page 22: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

22 MAWU OLANKHULIDWA

Ndiye anamugenda Stefano, anatsutsatchimo,

Anawakwiyitsa iwo, anamuphwanya mutu;Koma anafa mu Mzimu, napereka mzimu,Anapita kwa enawo, opereka moyo.

Miyoyo pansi pa guwa, ikulira, “Mpaka liti?”Kuti Ambuye alange ochita zoyipa;Koma kukhalanso ena opereka magaziKwa Uthenga wa Mzimu Woyera ndi mtsinje

Wake wofiira.

Tonse limodzi tsopano.

Ukuwukha magazi, inde, ukuwukha magazi,Uthenga wa Mzimu Woyera, Ulikuwukha

magazi,Magazi a ophunzira ofera Choonadi,Uthenga wa Mzimu Woyera Ulikuwukha

magazi.

115 Kodi iwo anali ndani? Amuna amene Mulunguanawaphunzitsa ndipo anawaitana. [Malo osajambulidwa patepi_Mkonzi.] Angakhoze bwanji Mulungu kumugwiritsantchito wamantha kuti aike Mawu ake mmenemo? Iye ndiwoopa. Ndicho chifukwa iwo sakudziwa kanthu za Iwo.Amuna amene sali owopa, amene Mulungu wawadula ndiMzimu Woyera, Mulungu akukhala mkatimo. Iye akanangotiasindikize mwamsanga magazi ake ngati panalibe, umboniwake ndi magazi ake; samafuna kusamala. Ndi Khristu yemweakumukhalira moyo. “Pakuti ine kuti ndikhale moyo ndiKhristu, ndipo kuti ndife ndi phindu.” Ndi momwe iwoankamverera za izo. Ameni.

116 Tsopano ndi nthawi ya mzere wa pemphero. Ndipo ndimzere wa pemphero wolawirira, pafupi twente pasiti eyiti.itapitirira 8.00. Koma ife tikufuna kuti tiwapempherere anthu.Ndipo ine ndikufuna inu tsopano, ichi^Kulalikira konsekumene ife tikanakhoza kuchita sikukanati_osati ufanizitsendi Mawu amodzi oyankhulidwa ochokera kwa MulunguMwiniwake.

117 Tsopano kuti tiyambe mzere wa pemphero, umene, ifetinalonjeza kuti tiwapempherere onse. Icho ife tichita,Mulungu akalola. Ife, usiku uliwonse, takhala tikuperekamakadi a pemphero. Ndi kunena, mu izi, kuti^Usikuuliwonse ife tikuyitana gulu kuchokera apo, ku kuzindikira zamumtima. Koma anthu, ndiye, ena a iwo adzakhala akuchokausiku umenewo. Ife tikanakhala ndi msonkhano wawukulu,ndipo Mzimu ukanati uzigwa, ndipo anthu akanati azichoka.Ndipo usiku wotsatira ife tikanati tiperekepo owonjezera.

118 Ndipo ngati ine sindiri kulakwitsa, kodi ine sindirikuyang’ana pa Fannie Wilson ataima kumbuyo uko? [Mlongo

Page 23: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 23

Wilson ati, “Ndiko kulondola.”_Mkonzi.] Ine ndikukumbukirandikumutenga mkazi uyo, pafupi khumi ndi zisanu ndiziwiri^O, kupitirira apo pafupi makumi awiri-^[“1932.”]1932, akufa, ndi TB, ndipo dotolo wa mzinda uno analiatamulephera iye. Ndipo iye anali akutaya magazi mpakamabulangeti ndi chirichonse zinali kukhala zitanyowa ndimagazi. Mwamuna wake ndi mwana wake wamkazi anabwerandipo anadzanditenga ine, mmawa wina. Tinapita kumenekondipo tinakaitanira pa iye, Dzina la Ambuye Yesu. Ndipopafupi masiku angapo kenako, mu nthawi yozizira yachirimwe, ine ndinamubatiza iye mu Dzina la Ambuye Yesu,ku mtsinje. Ndipo iye anabwera ndi msewu, kumbuyo kwangolo yachikale ya ng’ombe, wonyowa momwe iye akanakhozakukhala ali. Iye akanali moyo panobe usikuuno, chifukwaKhristu anachita izo. Nthawi yoyamba imene inendamuwonapo iye mu zaka zambiri. Ndikuyang’anapozungulira pa omvetsera, kuziwona izo.

119 Mulungu akanali wamoyo. Ndiko kulondola. Ndipo Iyeanati, “Chifukwa Ine ndiri moyo, inu mukhoza kukhala moyonanunso.”

120 Tsopano ine ndikanafuna kuti, kungoti ndikhale ngatindiyike kwa inu chimene ichi chiri, chifukwa, ngati inesinditero, ndiye inu mukhoza kuchokapo ndi kukati,“Chabwino, ine sindikuzimvetsa izo.”

121 Tsopano, makani anga ndi awa, kuti, “Yesu Khristuakanali yemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse.” Tsopano,ngati Iye akanali yemweyo, Iye ayenera kukhala yemweyo mumfundo iliyonse, yemweyo mu_mu mphamvu, yemweyo munyonga, yemweyo mu chirichonse chimene Iye anali.

122 Ndipo akanali pansi pano, uko kunali Agriki ena, nthawiyina, omwe anadza ndipo anati, “Mabwana, ife tikanafunakumuwona Yesu.”

123 Ndipo ine ndikukhulupirira kuti icho ndi chokhumba chamunthu aliyense kapena mkazi yemwe anayamba wamvapo zaYesu, amafuna kuti amuwone Iye. Ndipo ngati Iye asaliyemweyo, ndiye ife sitingakhoze kumuwona Iye. Koma ngatiIye ali yemweyo, ife tikhoza kumuwona Iye, kapena Iyeanatiuza chinachake cholakwika. “Komabe kanthawipang’ono, ndipo dziko silindiwona Ine kenanso, komabe inumudzandiwona Ine, pakuti Ine,” puronauni yaumwini, “Inendidzakhala ndi inu, ngakhale mkati mwa inu mpaka kumathero a m’badwo.” Ndiyeno Yesu analonjeza kuti azikhalamu Mpingo Wake, kumachita zinthu zomwezo zimene Iye analikuzichita apo, mpaka m’badwo uthe. Tsopano Iye anati,“Kanthawi pang’ono,” dziko silimamuwona Iye kenanso.Chabwino, ndiye, ife tikanati tizimuwona chotani Iye? Ifetikanamachita kumauwona Mzimu Wake, ngati Iye ali mkati

Page 24: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

24 MAWU OLANKHULIDWA

mwa ife, ndipo Mzimu umenewo ukanamati uzichita mofananamomwe Iye ankachitira apo, kapena Iwo sukanati ukhaleMzimu womwewo.

124 “Ine ndine Mpesa, inu ndinu nthambi.” Ndipo ngati ifetikubala^Ngati nthambi ili mu Mpesa, nthambi izibalamtundu wa chipatso chimene Mpesa umapereka kwa iwo.Chabwino, Mpesa woyamba umene ukutulukiraapo^Nthambi yoyamba inachokera mu Mpesa inali nthambiya chipentekoste; masomphenya, zimphamvu, machiritso,ubatizo wa Mzimu Woyera, zizindikiro zazikulu, ndizodabwitsa. Nthambi yotsatira ikanayenera kuti ikhale yamtundu wofanana wa nthambi. Kupitirira mmusi mpaka kumapeto, iyo iziyenera kuti ikhale yofanana. Ndicho chimeneYesu ananena.

125 Tsopano, tiyeni tiwone chimene Iye anali dzulo. Ngati ifetingakhoze kupeza chimene Iye anali dzulo^Tsopano inendikutenga mwa chidule, chifukwa cha nthawi; ndatindipereke pafupi maminiti asanu a malangizo. Ndipo ngati ifetingakhoze kuwona chimene Iye anali dzulo, ndiye ifetingakhoze kuwona chimene Iye ali lero, ndipo akhala alikwanthawizonse. Kodi izo ndi zosakondera mokwanira?[Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.]

126 Tsopano, pamene Iye anali kuno pa dziko lapansi, Iyeanabwera ngati Mesiya, anabatizidwa ndi Yohane M’batizi;anali asanachite ntchito ina apabe. Ndipo Iye analowa utumikiWake woyambirira. Kodi Iye anatumizidwa kwa ndani?Ayuda.

127 Tsopano, ife tikuzindikira kuti pali mafuko atatu okha aanthu mu dziko, ndiwo: Ayuda, Amitundu, ndi Asamaria;amene ali anthu a Hamu, Shemu, ndi Yafeti. Ayuda,Amitundu, ndi Asamaria.

128 Inu mukukumbukira? Petro anaitanira pa iwo, ndimafungulo aku Ufumu, pa Tsiku la Pentekoste, kwa Ayuda.“Lapani, mmodzi aliyense wa inu, ndipo mukhale obatizidwamu Dzina la Yesu Khristu.”

129 Filipo anapita uko ndipo anakalalikira kwa Asamaria. Iwoonse anakhulupirira ndipo analapa, ndipo anali atabatizidwamu Dzina la Yesu Khristu. Kungoti, Mzimu Woyera unaliusanafike pa iwo. Petro anali ndi mafungulo. Iye anabwerauko ndipo anasanjika manja pa iwo, ndipo iwo analandiraMzimu Woyera.

130 Ndiyeno Kornelio, Wamitundu, anali ndi masomphenya,kuti iye anali woti atumize ndi kukamutenga munthuwotchedwa Petro, Simoni Petro, yemwe anali kukhala munyumba ya munthu yemwe anali wofufuta zikopa. Ndipopamene Petro anabwera mpaka uko, “Petro akanalichiyankhulire Mawu awa, Mzimu Woyera unagwera pa iwo.”

Page 25: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 25

Ndiye Petro anati, “Kodi munthu angaletse madzi? Awaalandira Mzimu Woyera monga ife tinaupezera Iwo pachiyambi.” Nthambi iliyonse ikubwera apo mofanana basi.Mukuona?

131 Tsopano, pamene Yesu anakomana^Tsopano, Iyesanabwere kwa Amitundu. Ndi angati akudziwa izo? Iyeanawaletsa ophunzira Ake kuti apite kwa Amitundu alionse.Ndi angati akudziwa izo? “Musati mupite mu njira yaAmitundu, koma mupite maka kwa nkhosa zosochera zaIsraeli. Ndipo pamene inu mukupita, kalalikireni, kumati,‘Ufumu wa Kumwamba uli pafupi,’ kwa nkhosa zosochera zaIsraeli.”

132 Tsopano, ndani anali kumuyembekezera kuti Iye abweremu tsiku limenelo? Osati Amitundu; ife tinali achikunja,Angelezi Achisaxon. Ife tinali Achiroma, tikupembedza dzuwandi zina zotero. Ife sitinali tikuyembekezera Mesiya aliyense,koma Ayuda ndi Asamaria anali. Tsopano, kodi Iyeanadzilengeza chotani Iyeyekha kwa anthu amenewo omweanali akumuyembekezera Iye?

133 Tiyeni tibwerere mmbuyo tsopano ku Yohane Woyera,mutu woyamba, ndipo kwa mphindi yokha tsopano. Ndipomvetserani mwatcheru.

134 Myuda woyamba yemwe anayamba wabweretsedwa kwaIye, pamene Filipo kapena^Andrea atatembenuzidwa, ndipoanapita nakamupeza m’bale wake, Simoni Petro, iyeanamubweretsa Simoni pamaso pa Yesu. Ndipo Yesu anamuuzaiye chomwe dzina lake linali, ndi yemwe abambo ake anali. Ndiangati akudziwa izo? [Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.] Inumukuganiza kuti icho chinachita chiani kwa munthu ameneyo,yemwe akanati kenako adzakhale ndi mafungulo aku Ufumumu dzanja lake? Ndicho chimene Iye anadzitsimikizira Yekhakuti ali, Mesiya. Mwamsanga ndiye^

135 Filipo atatembenuzidwa, ndipo anapita kuti akampezeNataniele. Ndiwo mailosi makumi atatu kuzungulira phiri.Ndipo iye anabwera mpaka ku nyumba, ndipo ine ndikukhozakumumva iye akuti, “O, Akazi a Nataniele, kodi Nataniele alikuti?”

“O, iye ali uko_mu munda wa azitona.”

136 Anathamangira kunja uko mwamsanga kwenikweni,“Nataniele, kodi iwe uli kuti?” Ndipo iye anamupeza iye pansipa mtengo. Ndipo Nataniele anali akupemphera. Ndipo iyeanayembekezera mpaka iye atatsiriza kupemphera. Ndipo iyeanati, osati, “Iwe uli bwanji, Nataniele? Mbewu zikuchitabwanji?” O, iye anali ndi uthenga! Ndi momwe munthu yemwewakomana naye Yesu aliri. Iye alibe nthawi ya zopusa. Iyeanati, “Tabwera, udzamuwone Yemwe ife tamupeza, Yesuwaku Nazareti, mwana wa Yosefe!”

Page 26: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

26 MAWU OLANKHULIDWA

137 Ndipo tsopano ine ndikukhoza kumuwona Natanieleakusasa zovala zake, akuchokera pa pemphero. Iye anati,“Tsopano, Filipo, ine ndakudziwa iwe kuti ndiwe munthuwabwino, ndi munthu woonamtima. Tsopano, kodikungakhoze kukhala chinthu chabwino chirichonsechingabwere kuchokera ku Nazareti? Chabwino, iweukudziwa, ngati Mesiya akanati abwere, Iye akanabwera kuYerusalemu, kupyolera mu mpingo.” Ndi chimene anthuakuganiza lero. Mwaona? “Iye akanabwera kupyolera kuYerusalemu. A Kayafa sanalengeze konse izo pa msonkhanowathawu. Kotero, palibe mmodzi wa azamulungu wazilengezaizo. Chotero ine ndakudziwa iwe kuti ndiwe munthuwoonamtima. Kodi iwe wapita ku mathero akuya?”

“O, ayi. Iwe ubwere udzapeze chomwe chiri.”

Iye anati, “Kodi chirichonse chabwino chingakhoze^”

138 Iye anamupatsa iye yankho lopambana limene munthualiyense akanakhoza, anati, “Bwera, udzadziwonere wekha.”

139 Tsopano, pa ulendo mozungulira, ine ndikukhozakumumva Nataniele akuti^kapena Filipo akunena kwaNataniele, “Iwe ukudziwa chiyani? Iwe ukumukumbukiransodzi wachikulire uja uko yemwe sankakhoza ngakhalekulemba chiphaso chija pamene iwe unamupatsa iye zija,utagula nsomba zija kwa iye?”

“Inde. Ine ndikukhulupirira dzina lake linali Simoni.”

“Inde, ndi limenelo.”

140 “Ine ndinamubweretsa iye, tsiku lina, pamaso pa Mesiyaameneyo, ndipo mwamsanga pamene Iye anamuwona iye, Iyeanati, ‘Dzina lako ndiwe Simoni. Dzina la abambo ako ndi aYonasi.’ Ndipo ine^Sizikanati zikandidabwitse ine, kutipamene iwe uti ukafike pamaso pa Iye, Iye nkusakuuza iweyemwe iwe uli.”

Iye anati, “Aa, tsopano, dikirani miniti, osati ine.”

141 Chotero, tsiku lotsatira iwo anafika. Ndipo Yesu anali mumzere wa pemphero, mwachizolowezi, akupempherera odwala.Ndipo pamene iye akanakhoza^anabwera apo ndipoanalowa mkati mwa omvetsera. Yesu anayang’ana mmwamba,ndipo Iye anamuwona Filipo akubwera, akumubweretsamunthu kupyolera mu mpita. Ndipo Iye anayang’ana pa iye,ndipo Iye anati, “Taonani M’israeli mwa yemwe mulibechinyengo.”

142 Chimenecho Chiphunzitso chachilendo? Ameneyo analiYesu, dzulo. Uyo ndi Yesu, lero, ngati Iye ali yemweyo.

143 Ndipo munthu uyo anaima. Ine ndikukhoza kumuwonaNataniele. Filipo akumugunyuza iye, ndipo anati, “Inendinakuuza chiyani iwe? Ine ndinakuuza chiyani iwe?”

Page 27: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 27

144 Iye anati, “Rabbi,” zikutanthauza mphunzitsi, kapenachirichonse chimene ife timachitcha icho lero, inu mukudziwa.Kwenikweni, mawu olondola Achihebri, amatanthauzamphunzitsi. Anati, “Rabbi, ndi liti lomwe Inu munayambamwandiwonapo ine? Inu mwadziwa motani chirichonse za ine?Ine sindinayambe ndakuwonani Inu mu moyo wanga. Inumwadziwa motani kuti ine ndine M’israeli? Inu mwadziwamotani kuti ine ndine wolungama, ndi woonamtima, ndiwonena zoona? Inu simunayambe mwandiwonapo ine, mumoyo Wanu. Inu mwandidziwa motani ine?”

145 Iye anati, “Filipo asanakuitane iwe, pamene iwe unalipansi pa mtengo, Ine ndinakuona iwe,” mailosi makumi atatukuzungulira phiri, dzana lake. Ndi maso otani!

146 Tsopano kodi iye ananena chiyani? Iye anati, “Rabbi, Inundinu Mwana wa Mulungu. Inu ndinu Mfumu ya Israeli.”Ngati Ayuda anachizindikira icho^Tsopano dikirani. Uyoanali Myuda wosankhidwa. Ndi angati amakhulupirira mukusankhidwa? O, alipo anthu ambiri amene sadzalandira konseizo. Mukuona? Baibulo linanena chomwecho. Koma munthuameneyo anali ndi Mzimu wa Mulungu mwa iye. Ndipo iyeanavomereza izo, anati, “Rabbi, Ndinu Mwana wa Mulungu.Ndinu Mfumu ya Israeli.”

147 Koma kumeneko kunaima wazamulungu wa tsikulimenelo, ansembe ndi aphunzitsi aakulu, akumvetsera kwaIye. Ndipo inu mukudziwa chimene iwo ananena? Iwo anati,“Iye ndi wam’bwebwe. Iye ali ndi mzimu wa Belezebule paIye.” Yesu^Iwo sanali kuyankhula izo, mokweza. Ayi, ayi.

148 Koma Yesu anapotoloka ndipo anayang’ana pa iwo. Iyeanati, “Inu mukhoza kunditcha Ine izo ndi kudutsa nazo izo.Koma ili kubwera nthawi pamene Mzimu Woyera utiudzabwere, ndipo pamene inu muyankhula mawu amodzimomutsutsa Iye akuchita chinthu chomwechi, izosizidzakhululukidwa konse mu dziko lino kapena dziko lirinkudza.”

149 Chotero ndiye kodi ife tikuchita ndi chiyani? Awo analiAyuda. Ayuda enieni ndi owonamtima anamukhulupirira Iyekuti anali Mesiya.

150 Aphunzitsi ndi azamulungu, kodi iwo anali ndani? Mbewuya serpenti, monga ife tadutsiramo. Iye anati, “Inu ndinu aatate wanu, Mdierekezi.” Komabe, iwo anali ophunzira,anzeru, amuna oyera. Iwo sankakhoza kusunthakaphesi^Oyera. Iwo sankakhoza kuswa Sabata. Iwosankakhoza kudya nyama. Iwo anali amuna oyera, koma iwoanalephera kuti awone. Mukuona, iwo anali ataphunzitsidwandi anthu.

Mulungu amaphunzitsa amuna Ake, molimba. Ndikokulondola. Amuna oitanidwa ndi Mulungu!

Page 28: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

28 MAWU OLANKHULIDWA

151 Ndiye tsiku lina Iye_Akanati^Ndizo zomwe Ayudaankaganiza. Ndi momwe Iye anadzipangitsa kudziwikaIyeyekha kwa Ayuda. Ndi angati akudziwa kuti ndilo Lemba?[Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.] Chabwino. Tsopano, ngatiIye anadzipangitsa kudziwika Iyeyekha kwa Ayuda, ameneyoanali Yesu dzulo ndi Ayuda.

152 Tsopano inu mukuti, “Asamaria anali akuyembekezerakuti Iye abwere.” Inde, iwo anali, koma osati Amitundu.Asamaria okha.

153 Ndipo pamene Iye anakomana ndi Asamaria koyamba, Iyeankasowa kuti adzere ku Samaria. Ndipo Iye anaima, ndipoanawatuma ophunzira Ake, apite akafune chakudya, pafupithwelofu koloko. Iye anakhala pansi pa chitsime. Apopanatulukira mkazi, anayamba^Tsopano, ife tikudziwa iye,mu dziko ili, kuti anali mkazi wa mbiri yoipa, dona wamumsewu, inu mukudziwa, wachiwerewere. Ndipo chotero iyeanatulukira ndipo anayamba kutsitsira chidebe pansi muchitsime, kuti atungepo madzi. Ndipo iye anamva Liwu likuti,“Mkazi, ndibweretsere Ine akumwa.” Ndipo iye anayang’anapozungulira ndipo apo panakhala Myuda wa usinkhu wapakati.

154 Iye anali wa makumi atatu okha ndi chinachake, komaBaibulo linati Iye ankawoneka wa makumi asanu. Iwo anati,“Ndiwe Mwamuna wosapitirira usinkhu wa zaka makumiasanu, ndipo ukuti Iwe ‘unamuwona Abrahamu’?”

155 Iye anati, “Asanakhalepo Abrahamu, Ine ndine.”Mukuona? Ayenera kuti ankawoneka wachikulire chifukwacha ntchito Yake, thupi Lake laumunthu.

156 Ndipo iye anayang’ana apo. Iye anadziwa kuti Iye analiMyuda. Iye anati, “Bwana, si mwambo wake kuti inu Myudamuwapemphe Asamaria zinthu zoterozo monga izo. Ife tiribechochitirana chirichonse wina ndi mzake.”

157 Iye anati, “Mkazi, ngati iwe ukanadziwa Yemwe iwe unalikuyankhula naye, iwe ukanandipempha Ine akumwa. NdipoIne ndikanakubweretsera iwe, ndikanakupatsa iwe madziamene sukanati uzibwera kuno kuti udzatunge.” Kodi Iyeanali akuchita chiyani? Kuwukhudza mzimu wake. Mukuona?Penyani, Iye akuti adzilengeze Iyeyekha kwa Asamaria,tsopano.

158 Ndipo iye anati, “Bwanji, Inu mumati, ‘Kumakapembedzaku Yerusalemu.’ Ife timati, ‘Mu phiri ili.’ ”

159 Iye anati, “Nthawi ili nkudza, ndipo tsopano ili, pameneinu simudzatero, mu phiri ili kapena ku Yerusalemu,kumupembedza Mulungu, koma mu Mzimu ndi Choonadi.Atate akufuna oterowo.”

160 Kodi Iye anali akuchita chiyani? Kuwugwira mzimu wake.Ndipo patapita kanthawi, pamene Iye anapeza pamene vuto

Page 29: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 29

lake linali^Ndi angati akudziwa chimene vuto lake linali?Iye anali ndi amuna asanu, ndipo iye anali akukhala ndiwachisanu ndi chimodzi. Kotero, Iye anati, “Mkazi, pitaukamutenge mwamuna wako ndipo mubwere kuno.”

Iye anati, “Ine ndiribe mwamuna aliyense.”

161 Anati, “Ndiko kulondola. Iwe uli^unali nawo asanu,ndipo mmodzi yemwe iwe tsopano ukukhala naye si wako.”

162 Iye anaima ndipo anayang’ana pa Iye. Tsopano, iye sanati,“Ndinu Belezebule, bwana. Inu ndi wam’bwebwe.” Iyeankadziwa mochuluka za Mulungu kuposa theka la alaliki akuJeffersonville, ndiko kulondola, pokhala wachiwerewere. Iyeanati, “Bwana, ine ndadziwa kuti Inu ndinu mneneri.”

163 Penyani, “mneneri.” Ndipo ngati inu mungawayendetsemawu amenewo chammbuyo, inu muwapeza iwo, Mneneriyemwe Mose anati akanati adzabwere, mukuona, “Ambuye,Mulungu wanu, adzadzutsa mneneri wonga ine.”

164 Iye anati, “Ine ndazindikira kuti Inu ndinu mneneri.” Iyeanadziwa kuti Iye sanali kuzidziwa izo mulimonse;sakanakhoza kuzidziwa izo. Anati, “Ine ndazindikira kuti Inundinu mneneri.” Tsopano mvetserani pano, “Ife, Asamaria,”osati Ayuda tsopano. Asamaria, “Ife tikudziwa, pameneMesiya abwera, Iye adzatiuza ife zinthu izi.” Mukuona mtunduwa chizindikiro iwo anali kuchiyembekezera? Chizindikiro chaMesiya. “Pamene Mesiya abwera, Iye adzatiuza ife zinthu izi,koma Inu ndinu yani?”

Iye anati, “Ine ndine Iye, yemwe akuyankhula ndi iwe.”

165 Ndipo iye anagwetsa chidebe chake chamadzi, ndipoanathamangira ku mzinda, ndipo anati, “Bwerani,mudzamuwone Mwamuna yemwe wandiuza ine zinthu zomweine ndachita. Kodi ameneyu si Mesiya?”

166 Ngati icho chinali chizindikiro cha Mesiya pamenepo, ichochiyenera kukhala chizindikiro cha Mesiya lero. Ngati Iyeali^Tsopano, kumbukirani, palibe nthawi imodzi pamenechozizwitsa icho chinayamba chachitidwapo pamaso paAmitundu. Izo zinali zoletsedwa. Chifukwa? Amitundu analindi zaka zikwi ziwiri za mwachimpingo.

167 Koma tsopano kutha kwa m’badwo wa Amitundu kulipano. Ndipo Russia, chikominisi, chalozetsa bomba kumenecha kwa inu, kuti alithetse ilo, naponso. Musati muzidandaula,izo zikubwera. Baibulo linanena chomwecho. Ilo lidzakhalakuno ndi dzina lanu litalembedwa pa ilo, ndipo ilolidzasandulika phulusa mu nthawi ya mphindi imodzi, fukolonse. Ilo lidzakhala litathetsedwa kwathunthu. Zindikirani,uyo ndi Mulungu akuchita izo. Ine ndikudziwa kuti iwo aliufumu waufulu, iwo ndi gulu la achikunja. Koma kodiMulungu sanadzutse mafuko achikunja kuti amuwongole

Page 30: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

30 MAWU OLANKHULIDWA

Israeli mu masiku apitawo? Baibulo limanena kuti Russia ndichikominisi zikusewera kumene mmanja a Mulungu, kutiathetse anthu mwamtheradi pa dziko lapansi.

168 Koma izo zisanati zichitike, Mkwatulo ukubwera ndikudzautengera Mpingo Kwawo izo zisanafike pochitika. Ndipongati izo zayandikira pafupi chotero, Mkwatulo uli pafupichotani? Pafupiko kuposa izo. Chotero inu mukuona chifukwaife tiri^chifukwa ine ndikulalikira momwe inendikuchitiramu, pamene ine ndikulimbikira molimba mongaine ndingathere; pamene Mulungu akuchita chirichonsechimene Iye angakhoze kuchita, kuti akanikizire izo mwaOsankhidwa, kuti akokere Mbewu ya mkazi kunja, kutimbewu ya serpenti ikhoze kutenga chilango. Ndiko kulondolandendende. Ndizo zimene Iye analonjeza kuti adzachita.

169 Tsopano, ngati Yesu anadzilengeza Iyeyekha pamaso paMyuda ndi pamaso pa Msamaria, mwa zizindikiro zimenezo,ndipo akatilola ife kuti tizipita wopanda kulengezachizindikiro chomwecho kwa ife, Iye ali wosalungama; ngatiIye atisiya ife kuti tidutse nazo, mwa kuti, “Ndife Amethodisti.Ndife Abaptisti. Ndife Akatolika. Ndife Apresbateria.” Ayi,bwana, Iye akatilola ife kuti tidutse nazo ndi zamulunguzozizira.

170 Iye ayenera kuti abwere ndi zizindikiro, zodabwitsa, basimonga Iye anachitira mu malo oyamba, ngati Iye ali yemweyodzulo, lero, ndi kwanthawizonse. Ife tafika pa tsiku limenelo.Ife tiri pano tsopano. Mwa Baibulo, mwa mboni, mwa Mzimu,mwa sayansi, chirichonse chikutsimikizira kuti liri pano. O,ine^O, ine ndikukhumba ine ndikanakhala ndi mphamvukuti ndikankhire izo mwa anthu, kuti ndiwalole iwo kuziwonaizo.

171 Inu anthu kuno mu Jeffersonville ndinu anthu anga. Inendaleledwa ndi inu. Ndipo ine_ine ndimakukondani inu.Musati_musati mundiganizire ine kuti ndine wotentheka.Kodi inu mukuganiza zoneneratu izi ziri? Tayang’ananimmbuyo ku kusefukira kwa ‘37, inu anthu, pamene inumunkaseka pomwe pano pa mpingo. Ndipo ine ndinati, “Iwoadzakhala mapazi makumi awiri ndi awiri pa Spring Street,”miyezi isanu ndi umodzi izo zisanachitike. Ndiuzeni ine nthawiimodzi pamene chirichonse chinayamba chanenedwapo, chaPAKUTI ATERO AMBUYE, chimene sichinali ndendendeChoonadi. Ndiuzeni ine chinthu chimodzi chimene chinayambachanenedwa. Palibe! Ndi Choonadi, ndipo Icho chatsalachikadali Choonadi, ndipo Icho nthawizonse chidzakhala chiriChoonadi.

172 Tsopano ife sitingakhoze kubweretsa^Ine ndikulingaliraalipo zana kapena anthu opitirira pano oti apemphereredwe.Ife sitingakhoze kuwabweretsa iwo onse mwa kamodzi. Ife

Page 31: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 31

tiwabweretsa omwe ife tingakhoze, pa nthawi, ndiyenotiziwabweretsabe iwo mpaka ife titawabweretsa iwo onsepano. Tsopano ine ndikuti ndiyambire mu^Inendikukhulupirira. Kodi Billy Paul sanali pano? Kodi iye alikumbuyo uko? Muuzeni iye kuti abwere kuno. Ine ndikufunandiwone chiyani, ngati iye anapereka^Iwe unapereka khadiyanji? [M’bale Billy Paul ati, “Q, wani mpakahandiredi.”Mkonzi.] Ma Q, Q, Q. Khadi la pemphero Q.Yang’anani pa khadi la pemphero lanu. Ilo liri ndi Q. Wanimpaka handiredi. Chabwino. Ife sitingakhoze kuwabweretsaiwo onse pa nthawi imodzi, koma ife tikhoza kungobweretsapang’ono pokha pa nthawi, mpaka ife titakhoza kuwabweretsaiwo onse pamwamba pano. Ife tikufuna kuti iwo kutiazibwera, mmodzi ndi mmodzi, mpaka iwo onseatapemphereredwa.

173 Tsopano penyani. Ine ndikufuna aliyense, mkati ndi kunja,kuti aganize za izi. Ndipo potseka pa msonkhano uno, inendikuwupereka mpingo uno kwa m’busa, M’bale Neville,kukuperekani inu kwa iye, ndi iye kwa Mulungu. M’baleNeville pano. Ine ndikukuitanani nonse inu kuti mubwerenso.M’bale Neville ndi msirikali wamphamvu. Iye ndi wantchitoweniweni wa Khristu. Mlaliki wa Chimethodisti poyambapo,ine ndikukhulupirira, wophunzira wochokera ku Asbury,ndipo iye anali ataphunzitsidwa mu zamulungu zonse,seminale ya zamulungu, ndi kujayira kwa zomwe iwoamaphunzitsa. Koma, tsiku limodzi, iye anafika pa malopamene iye anadziwa kuti iye ankayenera kuti akhale ndichinachake chosiyana, ndipo iye anawoloka mzere. Iye ndim’busa pano, mwamuna wodzazidwa ndi Mzimu, mlalikiweniweni, wazamulungu weniweni. Ndipo inendikukupemphani inu, anthu a mzinda uno, ndi mu chigawochino, ngati inu mulibe mpingo, ndipo inu mukufuna kutimuzimvera Uthenga weniweni, muzibwera kudzamumveraM’bale Neville. Iye amaimira Chinthu chomwecho chimene inendimachita. Mwamtheradi, msirikali weniweni wamphamvu.Ife tonse, pano, timamukonda M’bale Neville. Iye wakhala alipano ndi ife nthawi yaitali, ndipo ife timamukonda iye.

174 Tsopano ngati Yesu Khristu, mwa Mzimu, ati abwererekuno usikuuno ndi kudzachita zinthu zomwezo zimene Iyeanachita pamene Iye anali pano pa dziko lapansi, kwa Myudandi Msamaria, Iye achita chinthu chomwecho kwa inuAmitundu, ndi angati a inu muti munene, “Inendimukhulupirira Iye ndi mtima wanga wonse ndipondikuzilandira izo pomwe pano”? Sindikusamala mpingowomwe inu muli a iwo. Izo ziribe^

175 Inu mukuti, “Kodi inu mukufuna kuti ine ndisiye kumapitaku mpingo wa Methodisti?” Ayi, bwana. “Baptisti?” Ayi,bwana.

Page 32: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

32 MAWU OLANKHULIDWA

176 Inu muzipita kulikonse kumene inu mukukufunakumatero, pakuti Mulungu ali nawo ana mu umodzi uliwonsewa mipingo imeneyo. Ndithudi, Iye ali nawo. Ndipo inu,mwinamwake, ndinu mmodzi wa iwo. Ndipo inendikukukondani inu mofanana basi monga inu mukanakhalamembala wa Branham Tabernacle. Izo sizimapangakachidutswa kamodzi ka kusiyana kwa ine. Inu mukudziwaizo mwa utumiki wanga, kulikonse. Ine ndikukhulupiriraMulungu amawakonda ana Ake, ziribe kanthu mtundu wanjiwa chizindikiro chomwe iwo akugwirapo. Ndi chimene inumuli mu mtima mwanu. Koma ife tikungokuitanirani inu kuchiyanjano. Ndinu olandiridwa kuti mubwere.

177 Tsopano, aliyense amadziwa, ndipo inu anthu akuJeffersonville mukudziwa, pambuyo pa zinthu zambiri zonsezimene zanenedwa ndi kuchitidwa, ndi kunenedweratu,chimodzi chirichonse cha izo kufika pakuchitika mwangwirobasi^Ndi angati kuno mu Jeffersonville akudziwa kuti izondi choonadi? Kwezani mmwamba manja anu amenemukudziwa kuzungulira kuno tsopano. Tsopano, kwa inuanthu akunja kwa mzindawu, inu mukuona chimene inendikutanthauza? Ndi angati akunja kwa mzindawu ameneanayamba akhalapo mu misonkhano yanga ndipo anawonakuti izo zimachitika chimodzimodzi basi monga Iwoamanenera? Kwezani manja anu, kwa anthu aku Jeffersonville.Mukuona? Baibulo linati, “Pa kamwa pa mboni ziwiri kapenazitatu mulole mawu aliwonse akhale okhazikika.” Kuzunguliramdziko izo zakhala ziri. Ndiye ife tikuyembekezera chiyani?Ife tiri nacho chirichonse mmanja athu momwe, ndi AmbuyeYesu. “Iye watipatsa ife zinthu zonse mwaulele.”

178 Tsopano ife tiyamba mzere wa pemphero. Ndipo ngati YesuKhristu ati achite pano usikuuno^

179 Tsopano, ndi angati a inu mukudziwa za chithunzi chaAmbuye Yesu, Kuwala kuja? Nonse a inu mukudziwa za Icho,mwakuchitika. Icho chiri mu Washington, D.C.,chinajambulidwa ndi munthu wopambana yemwe EdgarHoover anali naye mu zaka pang’ono zapitazi, George J. Lacy,mpukutu wa zidindo za zala. Ife tiri nako_kusaina kwake kulipa pepala kumene. Icho, makamaka^Iye anati iye penaankaganiza kuti kunali kuwerenga maganizo, ine ndinalikuwerenga maganizo a anthu. Iye anati, “Koma, BamboBranham, diso la makina la kamela iyo silingakhoze kutengakuwerenga maganizo.” Anati, “Kuwala kunakhudza disolo.”Ndipo ife tiri nazo izo zitalembedwa pa pepala, zikupita kunjalimodzi ndi chithunzi, Kuwala kunakhudza disolo.

180 Ndi angati akanali moyo, pamene Iko kunayambakuwonekera pamaso pa anthu kumusi kuno pa mtsinje,pamene ine ndinali kuwabatiza iwo mazana kumusi kuja tsikulija? Mu nyumbayi, kwezani mmwamba dzanja lanu. Apo pali

Page 33: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 33

manja atatu kapena anai, akadali moyo, ochokera ku zakazapitazo, kumusi kuno pa mtsinje pamene Iko kunabwerapansi, ndipo Uthenga wa Ambuye unabwera. Mofananakumene basi! Kodi Iko kunachita chimene Iko kunanena uko?Kuti, utumiki umene ine ndikanati ndikhale ndikulalikira,ukanati udzayambitse chitsitsimutso chozungulira mdziko,kutangotsala pang’ono Kudza kwachiwiri kwa Khristu.Penyani chimene Iko kwachita. Mwaona? Mmenemomunatuluka, kuchokera umo, Oral Roberts ndi ena onse awa.Mwaona? Ndipo kuzungulira dziko izo zapita, fuko lirilonse,anthu aliwonse, chinenero chirichonse. Moto wa chitsitsimutsoukuyaka, misonkhano yayikulu ya machiritso. Mwaona?

181 Tsopano, khalani okonzeka. Mkati, kunja, kulikonse inumuli, mulandireni Khristu. Mutero inu, usikuuno?

182 Tsopano, kuchokera pano mpakana, ine ndikudziperekandekha kwa Ambuye Yesu, kuti ine ndikakhoze kukwanitsakudzipereka ndekha kwa Mzimu, kuti ndizingomkuza YesuKhristu yekha; osati inemwini, koma Yesu Khristu; kuti anthuawa, anthu anga, abwenzi anga, mkati ndi kunja kwa mzinda,akakhoze kudziwa kuti Uthenga umene ine ndaulalikirauli^mwamtheradi Choonadi. Ndipo Khristu ali pano kutiawutsimikizire Iwo kuti uli Choonadi, mwa Mawu Ake ndiMzimu Wake.

183 Ife tichita kumawaitana iwo mmodzi pa nthawi. Choteroife tikhala^Ife tiyambira ndi nambala wani, Q nambalawani. Ndi ndani ali nayo iyo? Ngati_ngati inu simungakhozekuwuka tsopano, akulu adzakunyamulani inu. Ife tikufunakuti timutenge mmodzi aliyense wa inu. Q nambala wani.M’bale Hickerson, Billy Paul^Kapena, dikirani, Doc akutiamuthandizire iye pano. Q nambala wani, kodi inumungakwezere mmwamba dzanja lanu, yense yemwe ali nayoiyo. Kodi inu mukutsimikiza kuti iyo inali Q? Kapena,chabwino, o, ine ndikupepesa. Chabwino. Bwerani komwekuno. Msonyezeni iye kachitidwe kache, kudzera mu kampitauko. Q nambala wani. Chabwino.

184 Nambala thuu, kwezani dzanja lanu, chonde. Chabwino,dona wakhala kumbuyo komwe mkati muno. Chabwino, dona,bwerani. Pangani njira mpaka cha kuno; ngati inu nonsemungati mumulole iye. Anyamata uko akuthandizani inu,othandizira ndi ena otero. Q nambala firii, kwezani mmwambadzanja lanu. Nambala firii. Kodi mungakweze dzanja lanu,yense yemwe ali ndi Q nambala firii. Onani ngati dona uyuyemwe akupita apayu, ngati iye ali nalo khadi. Inu_inu mulibeiyo? [Mlongo ati, “M’bale Branham, ine ndinapempha khadi.Koma ine ndinamuwona mzanga wa ine, yemwe anaima ndimnyamata wodwala.”_Mkonzi.] Inu_inu simungakhozekuchita izo. [“Simungakhoze?”] Ayi. Inu muyenera kuigwiraiyo ndi kumvetsera kwa malangizo. Ife timutenga mwanayo,

Page 34: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

34 MAWU OLANKHULIDWA

mulimonse. Mukuona? Inu muzingobwera pamene nambalayanu yaitanidwa. Mwanayo akhoza kubwera pamene iyoyaitanidwa. Mukuona? Ndi zabwino.

185 Nambala wani, thuu. Ndi ndani yemwe ali nayo nambalafirii? Kwezani mmwamba dzanja lanu. Nambala firii. Nambalafolo.

186 Tsopano, ndizo zokondeka mwamphamvu kwa inu,mlongo, yense yemwe iye anali, dona uja yemwe amafuna kutiachite izo. Mukuona? Koma, onani, ngati_ngati nambala yawoyaitanidwa, iwo azibwera basi^Ngati iwo sanaitanidwe, ifetiwatenga iwo, mulimonse. Mukuona? Ife tikukufunani inu mumalo anu basi, kotero inu mukhoza kukhala ndi malo anu,inunso, inu mukuona. Mukuona? Chabwino.

187 Nambala firii. Nambala folo. Nambala faifi. Q nambalafaifi, kwezani mmwamba lanu^Kumbuyo komwe, mkaziwamng’ono. Nambala sikisi. Chabwino, mnyamata wamng’ono.Nambala seveni. Mwamuna komwe kuno. Nambala eyiti.

188 Ife tiyenera kuti tichite izi. Inu mukuona, inu simungakhozekuchita izo; mumangofika pongodzazana monse, inu mukati,“Munthu aliyense akufuna kuti apemphereredwe.”

189 Ndiroleni ine ndikusonyezeni inu chinachake, ngati inumukufuna kuti muwone chifukwa chimene ife timachitakuwafolela iwo. Aliyense mkati muno yemwe akanafuna kutiabwere ndi kuti adzapemphereredwe, kwezani mmwambamanja anu, munthu aliyense, ziribe kanthu yemwe inu muli.Taonani apo. Ndani yemwe ati abwere choyamba? Mukuona?Payenera kukhala winawake.

190 Billy amabwera kuno, amawatenga makadi awa, ndipoamawasakaniza iwo onse pamaso pa inu, ndipo iyeamamupatsa aliyense khadi la pemphero yemwe akufunaimodzi. Inu mukhoza kutenga yachisanu, yachisanu ndichimodzi, ndipo nthawizina ife timayambira penapake. Ndipoizo sizimapanga kusiyana kulikonse pamene ife^Ndiyenoiwo kunjako mwa omvera amachizidwa kwenikweni asanateroawa a pa nsanja, nthawizina. Ndi angati akudziwa izo, onsealendo ndi^Chabwino, zedi, ziribe kanthu kochita ndi izo.

191 Nambala sikisi, mmodzi ameneyo wabwera? Nambalaseveni. Nambala eyiti. Ndi ndani yemwe ali ndi khadi lapemphero eyiti? Takhala nayo kale iyo? Nambala naini.

192 Eyiti, nambala eyiti, ife tikufuna inu kuti muitenge iyotsopano. Mwina winawake kunjako. Ngati iwo ali, winawakeakweze dzanja lawo, kapena chinachake, winawake kunjako,yemwe sakanakhoza kuti alowe mkati. Nambala eyiti. M’baleCollins, kodi alipo aliyense kumbuyo uko, khadi la pempheronambala eyiti, yemwe akuyesera kuti alowe mkati? Chabwino,khadi la pemphero nambala eyiti. Chabwino.

Page 35: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 35

193 Nambala naini. Khadi la pemphero naini, kwezanimmwamba dzanja lanu. Mwina iwo anapita panja,sakanakhoza kulowa mkatimu. Ngati iwo ati abwere muno,ayikeni iwo mu mzere.

194 Nambala teni, kwezani mmwamba dzanja lanu. Mwamunakutali uko mmbuyo. Bwerani, bwana. Wokondwa kukuwonaniinu mukuitanidwira mkati. Inu munali mutaima kumbuyo uko,miyendo itachita zanzi. Nambala teni.

195 Nambala leveni. Kwezani mmwamba dzanja lanu, yenseyemwe ali ndi khadi la pemphero Q nambala leveni. Chabwino,leveni.

Thwelofu, Q nambala thwelofu. Njira^Chabwino,thwelofu.

196 Satini. Satini. Ingokwezani mmwamba dzanja lanu,chonde, kuti ine ndikhoze kuliwona. Khadi la pemphero satini,Q satini. Fortini. Fortini. Fifitini. Kodi unapereka makadiangati, Billy, zana? Satini, fortini, ndi fifitini, akusowa. Khadila pemphero satini, fortini, ndi fifitini, kodi inu muli pano?Fifitini, sikisitini, seventini, eyitini, naintini, twente.

197 Q poyamba, ndiye kuti titenge J, ndiyeno nkumangopitirirammusi pa mzere. Ine ndikuganiza iwo akuyesera kuti atsirizeawa, poyamba, mwaona. Ife tikatha kuwaitana iwo, ife tifikakwa enawo basi pamene titi tizibwera. Mukuti chiyani?[M’bale akuyankhula_Mkonzi.] Ndi choncho. Inu mukuona, ifetinapereka makadi uko, mmawa uno, ndipo anthusanabwerere, mwinamwake. Mukuona? Chabwino.

198 Tiyeni tiyambire pamenepo pang’ono. Motani^Inu mulipafupi kukwanitsa mzere wanu uko tsopano? Chabwino.Tsopano, ndi ndani yemwe ali nayo fifitini, sikisitini, seventini,eyitini, naintini, ndi twente, mu ma Q? Twente wani, twente-thuu, twente-firii, twente-folo, twente-faifi. Tsopanoingokhalani muli ok onzeka, basi mwamsanga izi zikakhalazitatha. Ife tiri ndi mzere wodzaza pano tsopano. Ndiyeno ifetibwera mpaka kwa iwo, kupita mopitirira mpaka pansi pamzere, ndiye nkulumphira mpaka mu makadi onsewo, ma J,pamene ife tinalekezerapo, ndi mmusi momwe mpaka ife tifikepa mapeto a iwo nkutha.

199 Tsopano ingokhalani molemekeza kwenikweni kwamphindi pang’ono. Tsopano, ine ndikukhumba ife tikanakhalandi malo okhalamo. Ine ndikukhumba pakanakhala pali njiraina yomwe ine ndikanati ndizichitira izo, koma ife tiribe iyo.Koma, tsopano, ine ndikufuna kuti inu mungokhalamwakulemekeza. Tsopano, kukanali molawirirabe. Ilimaminiti khumi isanakwane naini. Msonkhano ukhala utatha,theka lina la ora. Chotero, uku ndi kutsekera kwa msonkhano,ndipo chotero tsopano khalani molemekeza kwenikweni.Khalani chete kwenikweni. Musati muziyendayenda.

Page 36: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

36 MAWU OLANKHULIDWA

200 Ndipo ndi angati mkati muno amene alibe khadi lapemphero, ndipo komabe inu mukufuna kutimupemphereredwe? Kwezani mmwamba dzanja lanu.Chabwino, iwo angokhala paliponse. Tsopano, ngati inumulibe khadi la pemphero, ine ndikufuna kuti ndikupatseniinu Lemba lina.

201 Nthawi ina Ambuye wathu anali akupita kutiakamuwukitse msungwana wamng’ono, wakufa, yemwe analiasanafe apobe, mwana wamkazi wa Zakeyu. Ndipo mkazianati mu mtima mwake, “Ine ndikumukhulupirira Iye kuti ndiMunthu woyera. Ine ndikumukhulupirira Iye kuti ndi Mesiya.”Ndipo iye anali ndi vuto la magazi kwa zaka zambiri. Ndipoiye anazembera mu unyinji ndipo anakagwira chovala Chake.Munayamba mwawerengapo nkhaniyo?

Ndipo Yesu anaima, anati, “Ndani wandigwira Ine?”

202 Ndipo Petro anamudzudzula Iye. Iye anati, “Chabwino,onse a iwo akukugwirani Inu. Ndipo bwanji Inu mukuti,‘Ndani wandigwira Ine?’”

203 Iye anati, “Ine ndafooka. Ukoma, mphamvu, zachoka mwaIne.” Mukuona chimene izo zimachita kwa iwe, masomphenya?“Ine ndafooka. Mphamvu zachoka mwa Ine.”

204 Ndipo Iye anayang’ana pozungulira, pa omvera, mpaka Iyeanamupeza mkazi. Iye anachita mantha. Iye ankaganiza kutiiye anali atachita chinachake cholakwika. Koma Iyeanayang’ana pa iye, ndipo Iye anamuuza iye za kutaya kwakekwa magazi, ndipo anati, “Chikhulupiriro chakochakupulumutsa iwe.” Ndi angati akudziwa izo kuti ndiChoonadi? [Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.]

205 Tsopano, kwa inu masikolala a Baibulo, kodi Baibulo limati,kuti, “Yesu Khristu pakali pano ndi Wansembe Wamkulu,Wansembe wathu Wamkulu, yemwe angakhoze kugwiridwa ndikumverera kwa zowawa zathu”? Ndi angati akudziwa izo?[Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.] Chabwino, ngati Iye aliWansembe Wamkulu tsopano yemwe angakhoze kugwiridwandi kumverera kwa zowawa zathu, Iye akanakhoza kuchitamotani, ngati Iye ali yemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse?Iye akanayenera kuti achite mwanjira yomweyo momwe Iyeankachitira pamenepo. Kodi uko ndi kulondola? [“Ameni.”]

206 Chabwino, tsopano, Iye alibe thupi logwirika tsopano,pakuti ilo liri ku dzanja lamanja la Mulungu. Koma Iye alinawo matupi athu amene Iye amagwiriramo ntchito, ndipo ndiMzimu Wake ukugwira ntchito kupyolera mwa ife, monga Iyeanati iwo unali. “Ine ndidzakhala ndi inu, mkati mwa inu;ntchito zimene Ine ndikuzichita, mudzachita inunso.Zochuluka kuposa izi inunso mudzazichita, zochuluka, pakutiIne ndikupita kwa Atate.” Iye akanati adzaime mu malo athu.Mwaona? Koma Iye akanati azitidzoza ife ndi Mzimu.

Page 37: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 37

207 Tsopano, inu kunja uko mwa omvera, inu mungoyang’anacha kuno. Ndipo musati muzingoyang’ana pa ine mongaM’bale Branham. Inu muzingoti, “Ambuye Yesu, NdinuWansembe Wamkulu, ndipo Inu muli mu nyumba muno. Ndipoine ndikufuna kuti ndikugwireni Inu ndi zowawa zanga,kukuuzani Inu, ine ndikudwala. Ndipo Inu mutsimikizire izondi ine, ndipo mungomulola M’bale Branham kuti atembenukeapo monga, ndi Mzimu Wanu, ndipo andiuze ine monga Inumunamuuzira mkazi uja. Izo zikhazikitsa icho.” Inendikupikisana nacho chikhulupiriro chanu, mu Dzina laAmbuye, kuti muchite izo. Tsopano penyani ngati izo zirizolondola kapena ayi. Inu mumufunse Mulungu izo, ndipomuwone ngati izo ziti zichitike basi mwanjira imeneyo.Tsopano ingokhalani molemekeza kwenikweni.

208 Tsopano inu mukhoza kubweretsa odwala anu. Kapena,kodi munthuyo anali uyu? Chabwino. Chinthu choyamba mumzere, gawo ili la mzere^

209 Alipo anthu ochuluka muno. Ife timayesera kuwasiyaanthu kutali, anthu aku Jeffersonville; kungowalola anthu akunja kwa mzinda, kulimbanira kuti alowe muno. Chifukwa,mu mzere wa mtundu uwu, ngati anthuwo anali ochokerakuno, kuzungulira Jeffersonville, iwo akanakhoza kunena,“Bwanji, M’bale Branham amawadziwa anthu amenewo. Zedi,ndi chimene izo ziri.” Koma, ndithudi, iwo sanayambeakhalapo mu Afrika, ndi India, ndi Asia, ndi Ulaya, ndi konsekuzungulira dziko, mu malo ena. Koma ine sindikudziwa izo.

210 Ine ndikukhulupirira, anthu onse awa mu mzere uwu apatsopano, akuwoneka kwa ine ngati iwo ali alendo kwa ine.Kodi inu nonse ndinu alendo kwa ine? Ingokwezani mmwambamanja anu ngati inu muli. Chabwino. Ndizo zabwino. Ndiangati kunjako kwa omvetsera ali alendo kwa ine, kapena inumukudziwa kuti ine sindikudziwa chomwe chavuta ndi inu?Basi munthu aliyense, ziribe kanthu yemwe iye ali. Zedi, inusimuli, mwaona. Koma Iye amatero. Tsopano, ine sindikunenakuti Iye atero. Koma ngati Iye ati atero, ndiye izo zimupangitsaIye kukhalapo pomwe pano.

211 Tsopano, bambo uyu pano, ine ndikukhulupirira,anakweza dzanja lake, kuti iye ndi ine tinali alendo kwa winandi mzake. Ife ndife alendo. [M’bale ati,“Kulondola.”_Mkonzi.] Ine sindinayambe ndamuwonapobamboyu mu moyo wanga. Ine ndiri^ [“Ine sindinayambendakuwonanipo inu.”] Iye sanayambe wandiwonapo ine mumoyo wake mpaka tsopano pakali pano. Ife tabwera mnyumbamuno, ndipo ife taonana wina ndi mzake tsopano kwa nthawiyathu yoyamba.

212 Tsopano, pano pali chithunzi changwiro cha Filipo kupita,kukamutenga Nataniele, ndipo Nataniele nkubwera pamaso pa

Page 38: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

38 MAWU OLANKHULIDWA

Yesu. Tsopano, osati kuti iyeyo ndi Nataniele, kapena ineyoYesu. Tsopano, musati muziganiza izo. Koma zaka zotsatira,mwa lonjezo limene linapangidwa pamenepo. Ndipo pano paliamuna awiri amene sanayambe akomanapo mu moyo, basimonga amuna awiri aja anali pamenepo. Ndipo ngati Yesuakanali yemweyo, iye akhoza kudzipereka mzimu wake kuchikhulupiriro, ndipo ine ndikhoza kudzipereka mzimu wangaku chikhulupiriro, kwa Khristu, mwa mphatso Yauzimu yaMzimu Woyera, ndipo tikhoza kuchita chozizwitsachomwecho. Ndi kulondola uko? [Osonkhana ati,“Ameni.”_Mkonzi.] Ndipo ndi chauzimu. Mukuti, “Ndichozizwitsa?” Chabwino, ine ndingadziwe motani izo, ngati inesindinayambe ndamuwona iye? Manja anga ndi awa. Ifesitinayambe takomanapo kale. Ife, pano ife taima, kwa nthawiyoyamba. Mulungu akumudziwa iye; ine sindiri.

213 Tsopano, kumbukirani, khalani mukundipempherera ine.Tsopano nthawizina mu izi_mu nthawi izi, Mzimuumakudzoza, ndipo wakhala ukuchita izo mochulukakwambiri tsopano, mpaka zikukhala ngati^Chabwino,ine_ine ndikungofuna kuti inu mukhale mwabata. Mukhalemolemekeza kwenikweni. Penyani. Mukhale mu pemphero.

214 Tsopano, ine ndikungofuna inu, bwana, pokhalaosakudziwani inu, koma inu muli pano pa chifukwa chinachimene ine sindiri kuchidziwa. Koma chirichonse chimeneicho chiri, ndipo Ambuye Yesu akalola kundiuza ine chimeneinu mukufuna kwa Iye, popanda inu kundiuza ine, izozingamupange Iye basi chimene ine ndinati Iye anali, yemweyodzulo, lero, ndi kwanthawizonse. Inu mukukhulupirira izo?[M’bale ati, “Zedi.”_Mkonzi.] Chabwino. Iye akukhulupiriraizo. Ndipo tsopano omvetsera akukhulupirira izo. NdipoAmbuye anena kuti Iye akanati adzachite izo, mu BaibuloLake.

215 Tsopano, apa ndi pamene ine ndimapezeka mwinandikunena Choonadi ndi Baibulo la Mulungu, kapena Baibulolalonjeza chinachake chimene Ilo silingakhoze kuchiyimirakumbuyo, kapena ndine wachinyengo; chimodzi kapenachimzake. Mukuona? Ndiko kulondola. Muwone pamene iweumadziyika wekha. Ine ndazichita izo pamaso pa ambiri mbiri,zikwi za anthu, otsutsa ndi onse. Koma ine ndikudziwa kutiIye amalonjeza, ndipo Iye amasunga lonjezo Lake.

216 Ine ndikuwona Izo zikuyamba pakali pano tsopano. Inendikuwona anthu pokuzungulira iwe, pa nsanja, ndi kunjakwa msonkhano, ife tinalibe aliyense pozungulira. Mukuona?Alipo anthu odwala pano. Mwamsanga pamene Iwoukuyamba, iwe ukhoza kuwumverera Iwo. Iwo ndi MzimuWoyera. Khalani molemekeza kwenikweni tsopano,molemekeza basi tsopano, momwe ife tingakhozekuyankhulira. Inde, bwana. Ambuye Yesu amatikonda tonse

Page 39: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 39

ife, pakuti ndife amuna awiri amene Iye anawafera. Ndiponthawi yathu yoyamba kukomana. Ngati inu muli osowa,Mulungu ali wokhoza kupereka pa chosowa chimenecho,chifukwa Iye analonjeza kuti Iye akanadzatero.

217 Koma tsopano, bamboyu, ngati ali woona mu mtima wake,iye akuzindikira kuti chinachake chiri kuchitika. Iyesangakhoze kungoganiza ndendende chimene icho chiri. KomaMngelo uja yemwe inu mumamuwona pa chithunzi, akubwerapafupi ndi pafupi kwa bamboyu, ndipo iye akuzimirira kutalindi ine. Ndipo bamboyu akuvutika ndi vuto la mtima, ndipoiye ali ndi matenda a shuga. Ndiko kulondola. Ndizo PAKUTIUKUTERO MZIMU. Ngati izo nzoona, kwezani mmwambadzanja lanu.

218 Tsopano, ngati ine sindinayambe ndakuwonani inu, inendikanadziwa motani chirichonse chokhudza inu? Njira yina,njira yomweyo imene Iye anadziwira kumeneko. Ndi kulondolauko? [M’bale ati, “Ndiko kulondola.”_Mkonzi.] Kodiomvetsera akukhulupirira izo? [Osonkhana ati, “Ameni.”]

219 Tsopano, bwanji_bwanji osati tingotenga nthawi yathu,pang’ono pokha basi, chotero kuti inu muwone kuti sikunalikungopeka chinachake. Tiyeni titenge chinthu chinachake,ndipo tiyeni tingowona ngati Mzimu Woyera ukanati uwululechinthu chinachake kwa ife. Tiyeni tingoyankhula kwa bambowaima apoyo, miniti yokha. Mwinamwake pali chinthuchinachake mu moyo wake, mwinamwake chinthu chinachakecholakwika ndi iye. Ine sindiri kudziwa.

220 Ine sindiri kudziwa kwenikweni chimene ine ndinanena.Ine ndikasowa kuti ndikachiwone icho pa zojambulidwa kuno,chifukwa, mukuona, ndi masomphenya, iwe umaona pameneiye anali ali. Inde, ine ndikuziwona izo tsopano. Ndichinachake chokhudza magazi ake. Ndi shuga. Eya, ndimatenda a shuga. Iye ali ndi matenda a shuga, ndipo izozayambitsa vuto la mtima, chimene chayambitsa mtimawamanjenje. Iye wakhala ndi izo kwa nthawi ndithu. Ndipoiye si wochokera ku mzinda uno. Koma iye ndi wochokera kuIndiana, akuchokera ku malo pafupi ndi malo otchedwa mongaBorden. Inu^Ine ndikuona Borden. Ndinu ochokera kuBorden. Ndizo PAKUTI ATERO AMBUYE. Ndi zimenezo.

Ndipo pali chinachake cholakwika mu moyo wanu.

221 Pano pali chinthu china. Ine ndikuona mkazi akuwonekerapano mu masomphenya, chifukwa inu muli mu^Ndi akazianu, ndipo iye akusowa machiritso ena. Ndipo iye akuvutikandi mtundu wina wa kukhosomola. Ndi mphumu, iye ali nayo.

222 Ndipo inu muli ndi chinthu china cholakwika mu moyowanu, chimene inu mwakhala mukuyesera kuti muchichite.Mwa chikhulupiriro, ndinu wa Chipentekoste, chifukwa, inu,ndikukuwonani inu pa msonkhano wa Chipentekoste kumene

Page 40: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

40 MAWU OLANKHULIDWA

iwo akufuula ndi kuwomba manja awo. Ndipo inu mukuyeserakusiya^Inu mumasuta. Ndicho chimene inu mukuyesera kutimuchisiye, kusuta ndudu. Ndiko kulondola ndendende. NdizoPAKUTI ATERO AMBUYE. Ndicho choonadi. Sichoncho izo?Zedi, izo ziri. Mukuona? Kodi inu mukukhulupirira kuti Iye alipano tsopano, alipo? Kodi ndinu wokonzeka kuti mulandiremachiritso anu?

Tiyeni tiweramitse mitu yathu.

223 Ambuye Mulungu, Yemwe munamudzutsa Yesu KhristuYemwe ali pano tsopano, bambo uyu, Ambuye, yemwe ali panokufuna madalitso a Mulungu kuti akhale pa iye, ifetikupemphera kuti Inu mumupatse iye chokhumba cha mtimawake, mu Dzina la Yesu Khristu. Ameni.

224 Bwererani kwanu, mukazipeze izo basi momwe inumwakhulupirira. Ndi momwe izo ziti zikakhalire. Mulunguakudalitseni inu.

225 Kodi inu mukukhulupirira? [Osonkhana ati,“Ameni.”_Mkonzi.] Mulungu Wamphamvuzonse, Yemweanalemba Baibulo ili, Yemwe Mzimu wake ulipo, akudziwakuti ine sindinayambe ndamuwonapo bamboyu mu moyowanga, mwachidziwikire, mpaka miniti iyi yomwe. Koma, inendikudziwa chinthu chimodzi, Mzimu Woyera uli pomwe pano.Ine sindiri kudziwa chimene Iye ati achite, koma inendikudziwa kuti Iye ali pano.

226 Kodi ndi uyu donayo? Chabwino. Kodi ndife alendo kwawina ndi mzake? Chabwino, inu_inu_inu munandiwona ineku misonkhano, koma ine sindikukudziwani inu. [Mlongo ati,“Ayi. Ayi.”_Mkonzi.] Ndiko kulondola. Chabwino. Ndiye,muli pano pa cholinga china.

227 Tsopano, mkaziyo akhoza kukhala pano^Iye akhozakukhala Mkhristu; iye akhoza kusakhala. Iye akhoza kukhalawotsutsa. Ngati iye ali, ingopenyani chimene chiti chichitike.Mukuona? Ndipo ine sindikudziwa chimene iye wadzera.

228 Mayi anga akhala penapake mu nyumba muno, mkaziwachikulire. Kodi inu mungaganize kuti ine ndingayesere kutindimupweteke munthu wosawuka ameneyo? Inu mukuganizakuti ndingabwere kwa iye ngati wachinyengo? Ine ndithudisindikanatero. Ine kunali bwino kungochoka pa nsanja panondi kupita kwathu; ine ndalalikira kale Uthenga. Koma izozonse si zimene zimapita ndi Uthenga. Khristu ali yemweyodzulo, lero, ndi kwa nthawizonse. Sindikusamala chomwedziko likunena za izo. Ife tiyenera kuima ndi izo, mulimonse.Mulungu anati tizichita izi.

229 Pokhala osakudziwani inu; ndipo, ndithudi, inu mwakhalamu msonkhano, mwinamwake mmene muli mazana ndimazana a anthu, ine ndiribe njira ya kukudziwirani inu. Koma

Page 41: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 41

pano pali chithunzi tsopano cha Yohane Woyera 4, mwamunandi mkazi, kukomana kwa nthawi yoyamba. Ambuye wathundi mkazi waku Samaria akukomana kachiwiri. Tsopano iwoanayankhula. Iye anawukhudza mzimu wake, anadziwachimene chinali cholakwika ndi iye, ndipo anamuuza iye,ndipo iye anamuzindikira Iye kuti anali Mesiya. Kodi inumungachite chinthu chomwecho? Inu mungatero.

230 Kodi omvetsera angachite chinthu chomwecho, mkazialiyense kunja uko? [Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.]Mulole Mulungu apereke izi. Inde.

231 Mkaziyu akuvutika ndi_chikhalidwe cha manjenje. Iyewakhala nazo izo kwa nthawi yaitali, zaka zambiri mmbuyo.Ine ndikukhoza kumuwona iye panobe ali mkazi wamng’ono.Koma icho si chinthu chachikulu chimene iye akufuna kuti inendichipempherere. Ndi nyamakazi imene yamulumalitsa iye.Ndi chimene inu mukufuna ine kuti ndichipempherere.

Tsopano kodi inu mukukhulupirira? [Osonkhana ati,“Ameni.”_Mkonzi.]

232 Tiyeni tiyankhule kwa iye mopitiriza pang’ono. MuloleMzimu Woyera upereke izi. Mkaziyu alimakamaka_wamayankhulidwe akwina. Dzina lake ndiHanson. Ndi zoona. Wachi Norway kapena wachi Swedish, iye.Sindinu wochokera ku mzinda uno. Ndinu ochokera ku malootchedwa Canton. Ndipo uko ndi ku dziko lalikulu kumenekuli tirigu wambiri. Ndipo ndi ku Minnesota. Ndi kumene inumukuchokera. Izo nzoona. Tsopano bwererani kwanu; inumwachiritsidwa. Yesu Khristu wakupangani inu wabwino.Kawauzeni anthu zinthu zabwino zimene Ambuye achita kwainu.

233 Ine ndiri kulingalira kuti ife tiri alendo kwa wina ndimzake. [Mlongo ati, “Inde. Ine ndakhala ndiri mu misonkhano,koma inu simuli kundidziwa ine.”_Mkonzi.] Inesindikukudziwani inu. Ayi, mayi. Koma Ambuyeakukudziwani inu. Inu muli pano pa cholinga china. Ine sindirikuchidziwa. Koma ngati Ambuye Yesu ati awulule kwa inechimene inu mwadzera pano, inu mudziwa ngati izo zirichoonadi. Ngati ine ndikanabwera pano ndi kudzati, “Inumukudwala, mkazi.” Zedi, inu muli kuima pa mzere wapemphero, izo zikusonyeza^[Malo osajambulidwa pa tepi.]

234 Kupimidwa kwanu kukusonyeza kuti inu muli ndichinachake cholakwika ndi chiwindi. Iye anati izo zinalikuwuma kwa chiwindi. Ndiko kulondola. Ndingoyankhulakwa iye miniti. Basi^Kodi inu mukukhulupirira kutiAmbuye Yesu, yemwe anayankhula kwa mkazi pa chitsime, aliyemweyo lero? [Mlongo ati, “Inde.”_Mkonzi.] Inu mukutero?Muli, mukuwoneka ngati muli ndi mzimu wabwino. Sindinu

Page 42: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

42 MAWU OLANKHULIDWA

wochokera kuno. Inu mukuchokera kummawa, mukuchokeraku Ohio. Ndiko kulondola. Dayton, Ohio, kubwera kuno.[“Ndiko kulondola.”] Ndiko kulondola. Ine ndikuona^

235 Inu mukumupempherera winawake. Uyo ndi mnyamata.Iye ali ndi vuto la mtima. Iye ali ndi zironda, nayenso,mnyamata wokhala ngati wamanjenje. Ndiko kulondola.Ndipo inu mukupempherera moyo wake, chifukwa iye ndiwosapulumutsidwa. Ndizo PAKUTI ATERO AMBUYE. Izo ndizoona. Sichoncho izo? [“Mwana wanga.”] Inu mwachiritsidwa.Bwererani. Kamuuzeni iye, akhale wolimba mtima bwino.Yesu Khristu^

236 Sindiri kukudziwani inu, dona, sindiri kukudziwani inu.Mulungu akukudziwani inu. Ngati Mulungu ati andiuze inelomwe liri vuto lanu, inu mundikhulupirira ine kuti ndinewantchito Wake? Ndikutsimikiziritsa Iyeyekha. Mukuona,chimene ine ndikufuna kuti ndichite ndi kuwatenga anthuawa, amene akubwera mu mzere wa pemphero, kuti awonekuti Iye ali pano.

237 Chinachake chinachitika mu msonkhano. Pali akazi awiriaima apowo atavala, onse, magalasi. Winawake wamugwiraIye, ndi kumverera kwa zowawa zawo. Ine ndikukhozakungomuwona mkaziyo, chimene^Vuto lanu la khutu, ilolapita tsopano. Tayang’anani pa donayo, momwe iyeakuwonekera mochuluka monga uyu apa. Iwo anali ataimaapo. Ine ndimakhoza kuwaona iwo. Koma mmodzi analiakuchita izi; ndipo panalibe kanthu kotero kwa mmodzi uyu.238 Chifukwa cha izo chiri, mkazi uyu akuimira munthuwinawake. Ndiko kulondola. Ndipo mkazi uyo ndiwoyandikana naye wanu. Ndipo iye ali ndi nyamakazi. Ndipoinu mukumuimira iye. Ndipo ine ndikukuwonani inumukumupempherera iye, chifukwa iye ndi wosapulumutsidwa.Ndipo inu mukumupempherera iye. Ndicho chinthuchamphamvu. Kaikeni mpango uwo pa iye, umene inu mulinawo mdzanja lanu. Kamuuzeni iye kuti asati akaikire, ndikuti akapereke moyo wake kwa Khristu, ndipo nyamakaziyake imuchokera iye.

239 [Malo osajambulidwa pa tepi_Mkonzi.]^mukumulirira,mlongo? Inu mukumukhulupirira Mulungu? Inumukukhulupirira ine kuti ndine wantchito Wake? Inumukukhulupirira kuti Mulungu akhoza kundiuza ine chimeneinu muli kulirira, ndi chimene chokhumba chanu chiri? Ngatiinu mukukhulupirira izo, kwezani mmwamba dzanja lanu.Kodi inu mukukhulupirira kuti chotupa icho chimusiya iye?Ngati inu muti mukhulupirire izo, icho chipita. Ingokhalaninacho chikhulupiriro. Musati mukaikire basi.

240 Inu muli bwanji? Ndikuganiza ndife alendo kwa wina ndimzake. Ambuye Yesu akutidziwa tonse ife. Ndinu mkazi

Page 43: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 43

wamng’ono wamphamvu. Koma inu simuli pano chifukwa chainumwini. Ine ndikuwona chipatala chikutulukira, kama. Ndiamayi anu amene inu mukuwapempherera, ndipo iye ali ndimthunzi wa imfa. Iye akuvutika ndi ndulu, zotupa. Ndipo iyeali ndi khansala, naponso, mthunzi wakuda wa khansala.Tengani mpango umenewo, umene inu mukulirilapo,mukawuyike iwo pa iye. Ndipo mukaitanire pa Dzina laAmbuye, ndipo musati mukaikire. Ngati inu simukaikira,Mulungu akamuchotsapo iye apo ndi kumukhalitsa bwino iye.Musati mukaikire tsopano. Pitani mu Dzina la Ambuye, ndipokakhulupirireni.

241 Kodi inu mukukhutitsidwa kuti Khristu alimoyo?[Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.]

242 [M’bale Branham akuimikira_Mkonzi.] Pali chinachakecholondola^O, ndi mkazi wakhala kumbuyo komwe kuseriuko, mu mpando uwo. Iye akuvutika ndi mitu. Ndipo iyewakhala akupemphera kwa Ambuye, uko, akuyesera kutiazimusamalira mwana uyo. Iye anakumvani inu, mlongo. Izozonse zatha tsopano. Ingoimirirani pa mapazi anu, kutimumupatse Mulungu matamando chifukwa cha izo, dona.Ingomupatsani Mulungu matamando chifukwa cha izo.Mukuona?

243 Kodi iye anagwira chiyani? Iye sanandigwire ine konse.Koma iye anamugwira Wansembe Wamkulu uja. Ine sindirikumudziwa mkaziyu. Ine sindinayambe ndamuwonapo iye, mumoyo wanga. Koma Mulungu wamuchiza iye apo basi. Kodi izozikumupanga Yesu yemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse?[Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.] Zedi, izo zikutero. Ngatiinu mungakhoze kukhulupirira! Zinthu zonse ndi zotheka kwaiwo amene akhulupirira.

244 Iwo ukugunda omvetsera, munthu wina akupemphera.Mwaona, izo zimatengera pamene mphamvu ikuchulukira,kumene kuli Mzimu. Ine ndikhoza kutsatira kokha ndi kunenamonga Iye akunenera; ine sindimadziwa. O, ndi mkazi yemwewavala magalasi ake, akulira. Chifukwa chimene iye analikulira, chifukwa Mzimu uli pa iye. Apo Iwo uli. Vuto lamatumbo lija limene inu mwakhala mukuvutika nalo; khalanindi chikhulupiriro, izo zikusiyani inu ndipo sizidzabwererakonse. Ine sindikumudziwa mkaziyo. Ine sindinayambendamuwonapo iye. Iye sanandikhudze ine konse. Iyewamukhudza Wansembe Wamkulu.

Ngati inu mungakhoze kukhulupirira!

245 Iwo unamugunda mkazi wina. Ine ndikufuna wina aliyenseyemwe akufuna kutero, yang’anani kuno. Tayang’anani pamkazi akulirayu; tayang’anani pa mkazi winayo yemwewakhala bwinobwino; tayang’anani pa mkazi winayowapafupi ndi iye, akulira. Iye anali ndi vuto la mtima, dona

Page 44: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

44 MAWU OLANKHULIDWA

wamng’ono wakhala pomwepoyo, akuyang’ana pa ine ndilanu^Eya. Ndiko kulondola. Inu munali ndi vuto la mtima.Sichoncho inu? Ilo lakuchokerani inu. Chikhulupiriro chanuchinayatsa moto ndi Mulungu, ndipo inu munamugwira Iye.

O, izi ndi zodabwitsa!

[M’bale Branham akuimikira kwa mphindi makumi awirindi zisanu_Mkonzi.]

246 Muikumuwona dona wakhala apo pomweyo ndi mutuwake chowerama, akupemphera? Mkazi wa mutu wa imvi,mlendo kwa ine, atakhala apo. Inde. Inu munatembenukamozungulira, kumayang’ana pa uyo. Iye ali ndi vuto la ndulu.Iye wakhala akupemphera kuti Mulungu achichotse icho kwaiye. Ndipo inu munali kupemphera pamenepo, “Ambuye,muloleni iye andiyitane ine.” Ndiko kulondola. Ngati ndikokulondola, kwezani mmwamba dzanja lanu. Ine ndinadziwabwanji pemphero lanu? Izo zachoka kwa inu. Chikhulupirirochanu chakuchizani inu. Pitani kwanu ndipo mukakhalebwino.

247 Kodi inu mukukhulupirira? Ngati inu mungakhozekukhulupirira, zinthu zonse ndi zotheka. Koma inu muyenerakuti mukhulupirire.

248 Ukusunthabe mu boma limenelo, la yemwe wakhala mkatimmenemo. Pomwe pano, wachiwiri kuchokera kumapeto,kuthamanga kwambiri kwa magazi. Ngati inu mutimukhulupirire ndi mtima wanu wonse, mlongo, izo zatha. Kodiinu mukumukhulupirira Mulungu, kumutenga Iye pa MawuAke? Chabwino. Kwezani dzanja lanu mmwamba. Ndichochimene inu munali kuchipempherera, “Ambuye, muloleni iyeandiyitane ine potsatira, ndi kuthamanga kwambiri kwamagazi uku.” Ine ndine mlendo kwa inu. Ngati izo zirizolondola, gwedezani dzanja lanu. Chabwino. Izo zachoka kwainu. Pitani kwanu ndipo kakhaleni bwino.

249 Inu mukuona chimene icho chiri? Ndi chikhulupiriro.Ndipo ngati inu mungakhoze kuzikhulupirira izo! Kodi inumukukhulupirira? [Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.] Onani,anthu awo kunja uko, opanda makadi apemphero kapenakanthu. Kodi inu muli okonzeka kuti mukhulupirire? Kodiumo ndi momwe Ambuye Yesu ankachitira pamene Iye analipa dziko lapansi?

250 Pano, kodi uyu_kodi ndi mmodzi uyu, bambo akubwera?Chabwino. Inu simukudziwa chimene izo zimachita kwa inunonse. Kwa Branham Tabernacle, tsopano tangoyang’ana kunopamwamba manja. Mwaona? Inu mukudziwa ine sindimachitachotero. Ndi chiyani icho? Mzimu wa Ambuye. Iwo ukudzoza.

251 Anthu ambiri samamvetsa chomwe kudzozakumatanthauza. Iwo amaganiza kuti iko kumatanthauza

Page 45: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 45

kufuula. Icho ndi chisangalalo. Mphamvu imabwera moopsya.Mukuona? Icho ndi chisangalalo cha Ambuye. Iyi ndiMphamvu ya Ambuye; kumuchiza iye, kumupanga iyewabwino. Penyani chimene Iye anachita kwa msungwanawamng’ono atakhala usiku wina, wolumala; kwa munthuwakhungu; kwa ena, kupyola paliponse.

252 Inu muli bwanji, bwana? Ine ndikulingalira ndife alendokwa wina ndi mzake. Ife sitiri kudziwana wina ndi mzake. Inesindikukudziwani inu, ndipo inu simuli kundidziwa ine. Ngatiizo ziri zolondola, kwezani mmwamba dzanja lanu. Chabwino,nthawi yathu yoyamba kukomana. Molemekeza tsopano. Panopali mwamuna, ndipo iye ndi ine^wamng’ono kwambirikuposa ine, ndi manja athu ali mmwamba, kwa wina ndimzake, pamaso pa Mulungu, kuti iyi ndi nthawi yathuyoyamba kukomana. Yesu akumudziwa bamboyu. Ndipopayenera kukhala pali chinachake cholakwika; iye kuimapamenepo. Ine sindikuchidziwa.

253 Koma ngati ine ndanena choonadi, chimene Mulunguwatsimikizira mwa mboni zochuluka, kuti ine ndakuuzani inuchoonadi, kuti, “ndi mikwingwirima Yake inumunachiritsidwa.” Iyo ndi tensi yakale. Inu muyenera kupezachikhulupiriro cholimba icho, kuti mukwere pamwamba pazinthu izi.

254 Tayang’anani pa khansala ikuchoka pano usikuuno!Tsopano inu mungopenya maumboni amene akubwerakuchokera pamenepo, mithunzi yakuda ya imfa iyo. Dokotalawanu wokondeka akhoza kuyesa, zonse zimene iye akanakhozakuchita, kuti apulumutse moyo wanu. Koma pamene Mulunguanena chirichonse, ndi zimenezo. Ndipo izo sizinali ine. Inendiribe kanthu kochita ndi izo.

255 Tsopano alipo pafupi mazana awiri pano otiapemphereredwe. Ine ndikufuna kuti ndipume miniti yokhatsopano. Ndiyeno ife tidzangoyamba kumawapemphereraanthu, kuwabweretsa iwo pano; osati kuwadutsitsa iwokupyola mu mzere, koma nditaima pano kumawapemphereraiwo. Ine ndikufuna kuti ndimupempherere aliyense yemweakufuna kuti apemphereredwe.

256 Koma mwa omvetsera onse, ndi iwo amene ali pa nsanja,ine ndikufuna inu kuti muzindikire kuti Yesu Khristu ali pano.Kodi inu nonse muli kuzindikira zimenezo? [Osonkhana ati,“Ameni.”_Mkonzi.] Aliyense akuzindikira izo. [“Ameni.”]

257 Tsopano, kuti izo zikhoze kukhala zokhazikika kwanthawizonse mu malingaliro anu. Bambo uyu ndi ine, pano ndimanja athu mmwamba kwa Mulungu, nthawi yathu yoyambakukomana. Ngati Iye ati ayankhule chinsinsi cha mtima wake,monga momwe Iye anachitira kwa mkazi wa pa chitsime,kapena kwa Filipo, kapena mpaka kulikonse mpaka kupyola

Page 46: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

46 MAWU OLANKHULIDWA

mu utumiki Wake, ngati Iye ati achite izo, kodi izozitsimikizira kwa inu nonse, kuti ndi mwamtheradi Iye,Ambuye Yesu? [Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.]

258 Kodi zitero kwa inu, bwana? [M’bale ati, “Inde,bwana.”_Mkonzi.] Ine ndiribe njira, ndiribe lingaliro chomwevuto lanu liri. Ine sindikudziwa kaya ndinu wochimwakapena Mkhristu. Ine sindikanakhoza kukuuzani inu. Iyeamatero; Mulungu amatero. Koma ine sindingakhozekukuuzani inu. Koma ngati Iye ati andiuze ine^Koma inundinu Mkhristu. [“Inde.”] Chifukwa, mwamsanga pamenemzimu wanu ukugwira kudzoza kwa Mzimu uwu umene ulipa ine, iwo ukuulandira Iwo, chotero ine ndikudziwa ndinuMkhristu.

259 Ndipo inu muli pansi pa mthunzi wakuya. Ndi chinachakecholakwika ndi magazi. Ndipo inu mwakhala muli kwamadokotala. Ndipo iwo akufuna kuti apange opareshoni, ndipoopareshoni imeneyo ili, ine ndikuwamva iwo, ndipomadokotala awiri akufunsana wina ndi mzake, ndipo iwoakufuna kuti atenge chiwalo kuchokera mu thupi lanu,chimene chimatchedwa ndulu. Ndiko kulondola. [M’bale ati“Inde.”_Mkonzi.]

260 Ndipo inu simuli ochokera mu mzinda uno, koma ndinuochokera ku mzinda waukulu kumene kuli masukulu aakulu amtundu wina wa chipembedzo. Ndi ku Wheaton. Ndipo dzinalanu ndi Karl Rhodes, Rhodes, chinachake chonga KarlRhodes. Chabwino, bwana. Ngati inu muti mukhulupirire ndimtima wanu wonse, inu mukhoza kubwerera kunyumbakwanu, ndipo Mulungu akusiyirani moyo wanu. Kodi inumukukhulupirira izo? [M’bale ati, “Ine ndikukhulupiriraizo.”_Mkonzi.]

Tiyeni ife tipemphere.

261 Ambuye Yesu, ine tsopano ndikuponyera kutali choyipaichi kuchokera kwa m’bale wanga. Ndipo mu Dzina la YesuKhristu, mulole iye akhale moyo kwa ulemerero wa Mulungu.Ameni.

Mulungu akudalitseni inu, m’bale. Pa ulendo wanu,mukusangalala!

262 Ndi angati akukhulupirira tsopano ndi mtima wanuwonse? [Osonkhana Ati, “Ameni.”_Mkonzi.]

Tsopano, kodi ndiwo onse omwe ati apemphereredwe?Chabwino.

263 Chabwino, vuto lanu la nsana linakusiyani inu pamene inumunali mutakhala apo, kotero inu mukhoza kupita pa ulendowanu, ndipo muzisangalala ngati inu mukufuna kutero. Ndipomuzingopitirira, kumati, “Ndikuthokoza Ambuye wabwino!”

Page 47: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 47

264 Inu mupite mukadye chakudya chanu chamadzulo. Vutolanu la mmimba lakusiyani inu, mukubwera mu mzere, koteroinu mukhoza kupita ndi kukakhala ndi ulendo wanu, inunso.Mungokhulupirira ndi mtima wanu wonse.

265 Nyamakazi yanu sikuvutitsani inu, ngati inu mutimukhulupirire izo. Ingomapitirirani choncho, mukusangalalandi kumatamanda Mulungu, ngati inu mungatero, m’bale.Chabwino. Chabwino.

266 Kodi inu mukukhulupirira ndi mtima wanu wonse?[Osonkhana ati, “Ameni.”_Mkonzi.] Ndi angatiakumukhulupirira Mulungu? [“Ameni.”] Tsopano ine ndikutindingoponda apa mphindi yokha. `

Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu, Vol. 12 No. 4

(God-Called Man, Vol. 2 No. 27R)

Uthenga uwu wa M’bale William Marrion Branham wolalikidwa mu

Chingelezi pa Lamlungu usiku, pa Okotobala 5, 1958, ku Branham

Tabernacle mu Jeffersonville, Indiana, U.S.A., unatengedwa kuchokera pa

matepi ojambulidwa ndi maginito nudindidwa mosachotsera mawu ena mu

Chingelezi. Kumasulira uku kwa Chichewa kunadindidwa mchaka cha 1999

ndi Voice of God Recordings.

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. Box 950, Jeffersonville, Indiana 47131 U.S.A.

Page 48: MUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU Munthu …download.branham.org.s3.amazonaws.com/pdftranslations/CHA58-1005e.pdfMUNTHU WOITANIDWA NDI MULUNGU 1 Munthu Woitanidwa Ndi Mulungu ` ^Neville

Just One MOre tiMe, LOrd 1

Copyright notice

All rights reserved. This book may be printed on a home printer for personal use or to be given out, free of charge, as a tool to spread the Gospel of Jesus Christ. This book cannot be sold, reproduced on a large scale, posted on any website other than www.branham.org, stored in a retrieval system, translated into other languages, or used for soliciting funds without the express written permission of Voice Of God Recordings®.

For more information or for other available material, please contact:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org